< Yobu 6 >
1 Tsono Yobu anayankha kuti,
Epi Job te reponn:
2 “Achikhala mavuto anga anayezedwa, ndipo zipsinjo zanga zonse zikanayikidwa pa sikelo!
“O ke doulè m ta kab peze pou mete nan balans lan, ansanm ak gwo dega ki vin sou mwen yo!
3 Ndithu, zikanalemera kupambana mchenga wa ku nyanja; nʼchifukwa chake mawu anga akhala okhadzula.
Paske li ta pi lou pase sab lanmè yo. Akoz sa a, pawòl mwen yo te tèlman san règ.
4 Mivi ya Wamphamvuzonse yandibaya, thupi langa likumva ululu wa miviyo; zoopsa za Mulungu zandizinga.
Paske flèch Toupwisan an fin antre anndan m; lespri m ap bwè pwazon. Gwo laperèz Bondye a vin alinye kont mwen.
5 Kodi bulu wakuthengo amalira akakhala ndi msipu, nanga ngʼombe imalira ikakhala ndi chakudya?
Èske bourik mawon ranni sou zèb li, oswa bèf rele sou manje li?
6 Kodi chakudya chosakoma nʼkuchidya chopanda mchere, nanga choyera cha dzira chimakoma?
Èske bagay san gou kapab manje san sèl, oswa èske pati blan nan zye poul a gen gou?
7 Zakudya zimenezi sindifuna nʼkuzilawa komwe; zakudya zimenezi zimabwerera kukhosi.
Nanm mwen p ap touche yo. Yo tankou manje abominab pou mwen.
8 “Aa, ndikanalandira chimene ndikuchipempha, chikhala Mulungu anandipatsa chimene ndikuchiyembekezera,
“O ke sa m mande ta kab rive, e ke Bondye ta ban m sa m anvi wè a!
9 achikhala chinamukomera Mulungu kuti anditswanye, kulola dzanja lake kuti lindimenye ndi kundiwonongeratu!
Ke Bondye ta dakò pou kraze m nèt, ke Li ta lache men l pou retire mwen nèt!
10 Pamenepo ine ndikanakhalabe ndi chitonthozo ichi, ndikanakondwa mu ululu wanga wosalekezawu podziwa kuti sindinakane mawu a Woyerayo.
Kite sa toujou kòm konsolasyon mwen; wi, kite mwen rejwi nan doulè k ap kraze mwen, pou m pa t renye pawòl a Sila Ki Sen an.
11 “Kodi mphamvu zanga nʼzotani kuti ndizikhalabe ndi chiyembekezo? Nanga zoyembekezera zanga nʼzotani kuti ndipirirebe?
Ki jan fòs mwen ye, pou m ta tan? Epi kilès lafen mwen, ke m ta dwe sipòte?
12 Kodi ine ndili ndi mphamvu? Nanga thupi langa ndi lolimba ngati chitsulo?
Èske fòs mwen tankou wòch, o èske chè m kon bwonz?
13 Kodi ndili ndi mphamvu zodzithandizira ndekha, nanga pakuti thandizo lachotsedwa kwa ine?
Èske se pa ke nanpwen sekou anndan m, ke tout sajès fin chase lwen mwen?
14 “Munthu amene ali kakasi ayenera kukhala ndi abwenzi odzipereka, ngakhale kuti iyeyo wasiya kuopa Wamphamvuzonse.
“Paske pou nonm ki pèdi tout espwa a, li ta dwe twouve konpasyon nan zanmi li; menm a li menm ki kon pèdi lakrent Wo Pwisan an.
15 Koma abale anga ndi wosadalirika ngati mitsinje yowuma msanga, ngati mitsinje imene imathamanga.
Frè m yo te aji ak desepsyon kon yon ravin, kon flèv ravin ki vin sèch;
16 Ali ngati mitsinje ya madzi akuda nthawi ya dzinja, imene madzi ake amakhala ambiri chifukwa chakuchuluka kwa mvula,
ki vin sal tankou glas k ap fonn kote lanèj kon kache.
17 koma madziwo amasiya kuyenda nthawi yachilimwe, ndipo nthawi yotentha madziwo amawumiratu mʼmitsinjemo.
Nan sezon sèch, yo pa la; lè li cho, yo disparèt sou plas yo.
18 Anthu oyenda pa ngamira amapatukirako kufuna madzi; iwo amangoyendayenda nʼkufera mʼchipululu.
Chemen a kous pa yo tòde tout kote; yo monte rive vin anyen; yo vin disparèt.
19 Anthu oyenda pa ngamira a ku Tema amafunafuna madzi, anthu amalonda apaulendo a ku Seba amafunafuna mwa chiyembekezo.
Karavàn Théma yo te vin veye; vwayajè Séba yo te gen espwa yo.
20 Amataya mtima chifukwa ankayembekezera kupeza madzi; koma akafika kumeneko, amangokhumudwako.
Yo te desi paske yo te mete konfyans; yo te vini la, e te etone.
21 Tsono inunso mukuonetsa kuti ndinu osathandiza, mukuona chinthu choopsa kwambiri ndipo mukuchita mantha.
Anverite, koulye a se konsa ou ye; ou wè laperèz e ou vin pè.
22 Kodi ine ndinanenapo kuti, ‘Ndiperekereni kenakake, ndilipirireni dipo kuchokera pa chuma chanu,
Èske mwen te di ou: ‘Ban m yon bagay’? Oswa m te fè yon demann anba tab pou retire nan richès ou?
23 ndilanditseni mʼdzanja la mdani, ndiwomboleni mʼdzanja la munthu wankhanza?’
Oswa ‘delivre m nan men advèsè a’? Oswa ‘rachte mwen nan men opresè sila yo’?
24 “Phunzitseni, ndipo ine ndidzakhala chete; ndionetseni pomwe ndalakwitsa.
“Enstwi mwen e mwen va pe la! Montre mwen kote mwen gen tò.
25 Ndithu, mawu owona ndi opweteka! Koma mawu anu otsutsa akufuna kuonetsa chiyani?
Kèl doulè pawòl onèt sa yo genyen! Men kisa diskou ou a pwouve?
26 Kodi inu mukufuna kundidzudzula pa zimene ndikunena, ndipo mukufuna kuyesa mawu a munthu wosweka mtima ngati mphepo chabe?
Èske ou gen entansyon repwoche pawòl mwen yo, lè ou konnen se van ki mèt pawòl yo lè moun dekouraje nèt?
27 Inu mungathe kuchita maere kuti mugulitse ana amasiye ndi kumugulitsa bwenzi lanu.
Konsa, ou ta menm tire osò pou òfelen yo e fè twòk pou zanmi ou.
28 “Koma tsopano ndichitireni chifundo pamene mukundiyangʼana. Kodi ine ndingayankhule zabodza pamaso panu?
Alò, souple, gade mwen e wè si se manti m ap fè nan figi ou.
29 Fewani mtima, musachite zosalungama; ganiziraninso popeza chilungamo changa chikanalipobe.
Rete la, koulye a e pa kite enjistis fèt. Retounen kote m! Jiska prezan, ladwati mwen rete ladan an.
30 Kodi pali choyipa chilichonse pa milomo yanga? Kodi pakamwa panga sipangathe kuzindikira kanthu koyipa?
Èske gen enjistis sou lang mwen? Èske bouch mwen pa kapab distenge gou gwo malè?”