< Yobu 6 >
1 Tsono Yobu anayankha kuti,
Yoube da bu adole i,
2 “Achikhala mavuto anga anayezedwa, ndipo zipsinjo zanga zonse zikanayikidwa pa sikelo!
“Na bidi hamosu da: i dioi da dioi defesu amoga defesa ganiaba, ilia defei da hano wayabo ganodini sa: i amo defei baligi ba: la: loba. Amaiba: le, na da udigili sia: dasea, mae fofogadigima.
3 Ndithu, zikanalemera kupambana mchenga wa ku nyanja; nʼchifukwa chake mawu anga akhala okhadzula.
4 Mivi ya Wamphamvuzonse yandibaya, thupi langa likumva ululu wa miviyo; zoopsa za Mulungu zandizinga.
Gode Bagadedafa E da dadi bagohame amoga na gala: i. Dadi medosu hano da na maga: me ganodini haina daha. Gode da na beda: ma: ne, se iasu bagade nama iaha.
5 Kodi bulu wakuthengo amalira akakhala ndi msipu, nanga ngʼombe imalira ikakhala ndi chakudya?
Dougi da gisi nasea, hahawane esalebe ba: sa. Bulamagau da gisi giliga: la: i nasea, ouiya: le esalebe ba: sa.
6 Kodi chakudya chosakoma nʼkuchidya chopanda mchere, nanga choyera cha dzira chimakoma?
Be dunu da ha: i manu deme hame gala, amo manu gogolesa. Amola sio oso da: iya da hame hedasa.
7 Zakudya zimenezi sindifuna nʼkuzilawa komwe; zakudya zimenezi zimabwerera kukhosi.
Na da agoai ha: i manu hame hedai agoai ba: sa. Na da ha: i manu huluane nasea, olosa.
8 “Aa, ndikanalandira chimene ndikuchipempha, chikhala Mulungu anandipatsa chimene ndikuchiyembekezera,
Gode da abuliba: le na adole ba: su liligi hame iabela: ? E da abuliba: le na sia: ne gadosu hame adole iabela: ?
9 achikhala chinamukomera Mulungu kuti anditswanye, kulola dzanja lake kuti lindimenye ndi kundiwonongeratu!
E da na medole legemu da defea gala.
10 Pamenepo ine ndikanakhalabe ndi chitonthozo ichi, ndikanakondwa mu ululu wanga wosalekezawu podziwa kuti sindinakane mawu a Woyerayo.
Na da se bagade naba. Be E da na medole legemu na da dawa: i ganiaba, na da hahawaneba: le, soagalagadola: loba. Na dawa: , Gode da hadigidafa. Na da Ea hamoma: ne sia: i hamedafa hihi galu.
11 “Kodi mphamvu zanga nʼzotani kuti ndizikhalabe ndi chiyembekezo? Nanga zoyembekezera zanga nʼzotani kuti ndipirirebe?
Na da bu esalumu, gasa hame galebe. Na da dafawane hamoma: beyale huluane fisi dagoiba: le, abuli bu esaloma: bela: ?
12 Kodi ine ndili ndi mphamvu? Nanga thupi langa ndi lolimba ngati chitsulo?
Na da gelega hamobela: ? Na da: i hodo da balasega hamobela: ?
13 Kodi ndili ndi mphamvu zodzithandizira ndekha, nanga pakuti thandizo lachotsedwa kwa ine?
Na da nisu gaga: mu da gasa hamedafa gala. Na da fidisu dunu hamedafa gala.
14 “Munthu amene ali kakasi ayenera kukhala ndi abwenzi odzipereka, ngakhale kuti iyeyo wasiya kuopa Wamphamvuzonse.
Na da Gode Ea hou yolesi o hame yolesi, mae dawa: ma! Be amo bidi hamosu da nama doaga: beba: le, na na: iyado dunu da na hame yolesimu da defea galu.
15 Koma abale anga ndi wosadalirika ngati mitsinje yowuma msanga, ngati mitsinje imene imathamanga.
Be dilia! Na na: iyado dunu! Gibu da hame dasea, hano da hafoga: i ba: sa. Amo defele, dilia da na ogogole fawane fidisa.
16 Ali ngati mitsinje ya madzi akuda nthawi ya dzinja, imene madzi ake amakhala ambiri chifukwa chakuchuluka kwa mvula,
Anegagi oubiga, hano da anegagi ofo amola muge amoga ga: i dagoi ba: sa.
17 koma madziwo amasiya kuyenda nthawi yachilimwe, ndipo nthawi yotentha madziwo amawumiratu mʼmitsinjemo.
Be gia: i oubiga, amo liligi da hedolowane alalolesisa. Amasea, hano logo da hafoga: i dagoi ba: sa.
18 Anthu oyenda pa ngamira amapatukirako kufuna madzi; iwo amangoyendayenda nʼkufera mʼchipululu.
Sofe ahoasu dunu da hano hogobeba: le, fisi dagoi ba: sa. Ilia hafoga: i sogega doula ahoabeba: le, hedolo bogogia: sa.
19 Anthu oyenda pa ngamira a ku Tema amafunafuna madzi, anthu amalonda apaulendo a ku Seba amafunafuna mwa chiyembekezo.
20 Amataya mtima chifukwa ankayembekezera kupeza madzi; koma akafika kumeneko, amangokhumudwako.
Siba amola Dima dunu fi sofe ahoasu dunu ilia da hano hogolala, be hafoga: i hano logo fawane ba: beba: le, ilia dafawaneyale hamoma: beyale dawa: i da udigili fisi dagoi ba: sa.
21 Tsono inunso mukuonetsa kuti ndinu osathandiza, mukuona chinthu choopsa kwambiri ndipo mukuchita mantha.
Na da dili ba: sea, dilia da amo hafoga: i hano logo defele ba: sa. Dilia da nama misi hou ba: sea, beda: iba: le fofogadigili bagidu gagasi ahoa.
22 Kodi ine ndinanenapo kuti, ‘Ndiperekereni kenakake, ndilipirireni dipo kuchokera pa chuma chanu,
Na da dilima hahawane dogolegele iasu adole ba: bela: ? Na da dilima dilia na fidima: ne, eno dunuma hano suligili adole ba: bela: ?
23 ndilanditseni mʼdzanja la mdani, ndiwomboleni mʼdzanja la munthu wankhanza?’
Na da dilima na ha lai dunu na mae hasalima: ne gaga: musa: adole ba: bela: ? Hame mabu!
24 “Phunzitseni, ndipo ine ndidzakhala chete; ndionetseni pomwe ndalakwitsa.
Defea! Nama olelema! Na giadofai amo nama adoma! Na da ouiya: le, dilia sia: noga: le nabimu.
25 Ndithu, mawu owona ndi opweteka! Koma mawu anu otsutsa akufuna kuonetsa chiyani?
Dunu da moloidafa sia: nabasea, dafawaneyale dawa: mu. Be dilia da udigili gagaoui sia: fawane sia: sa.
26 Kodi inu mukufuna kundidzudzula pa zimene ndikunena, ndipo mukufuna kuyesa mawu a munthu wosweka mtima ngati mphepo chabe?
Dilia da na sia: da udigili fo agoane dawa: sa. Amaiba: le, dilia da abuliba: le na heawini da: i dioi sia: amoma adole iabela: ?
27 Inu mungathe kuchita maere kuti mugulitse ana amasiye ndi kumugulitsa bwenzi lanu.
Dilia hou da agoane gala. Dilia da udigili hawa: hamosu guluba: mano lama: ne, ululuasa. Dilia da na: iyadodafa ilia liligi wamolabeba: le, bagade gagui dunu agoai ba: sa.
28 “Koma tsopano ndichitireni chifundo pamene mukundiyangʼana. Kodi ine ndingayankhule zabodza pamaso panu?
Na odagi ba: ma! Na da hame ogogomu!
29 Fewani mtima, musachite zosalungama; ganiziraninso popeza chilungamo changa chikanalipobe.
Dilia sia: da gui dagoma! Moloihame hou yolesima! Nama se ima: ne mae fofada: ma! Na hou da moloidafa!
30 Kodi pali choyipa chilichonse pa milomo yanga? Kodi pakamwa panga sipangathe kuzindikira kanthu koyipa?
Be dilia da na da ogogosu dunuyale dawa: be. Dilia da na da wadela: i hou amola moloidafa hou amo da hisu hame dawa: yale dawa: sala: ?