< Yobu 40 >

1 Yehova anati kwa Yobu:
Te phoeiah BOEIPA loh Job te a voek tih,
2 “Kodi iwe ufuna kukangana ndi Wamphamvuzonse? Iwe amene unatsutsana ndi Mulungu umuyankhe Iyeyo!”
Tlungthang te a ho a? Cawtkung aka tluung te Pathen loh doo nawn saeh,” a ti nah.
3 Pamenepo Yobu anayankha Yehova:
Te vaengah Job loh BOEIPA te a doo tih,
4 “Ine sindili kanthu konse, kodi ndingathe kukuyankhani chiyani? Ndagwira pakamwa panga.
“Kai n'kosinah coeng he. Namah te metlam kan thuung eh? Ka kut he ka ka dongla ka puei mai coeng.
5 Ndinayankhula kamodzi, koma pano ndilibe yankho, ndinayankha kawiri, koma sindiwonjezeranso mawu ena.”
Vai ka thui vaengah ka doo voel pawt dongah pabae nen khaw ka koei mahpawh,” a ti nah.
6 Ndipo Yehova anayankha Yobu mʼkamvuluvulu kuti,
Te phoeiah BOEIPA loh Job te hlipuei khui lamloh a voek tih,
7 “Tsopano vala dzilimbe ngati mwamuna; ndikufunsa mafunso ndipo iwe undiyankhe.
Hlang bangla na pumpu te yen laeh. Nang kan dawt vaengah kai m'ming sak.
8 “Kodi iwe unganyoze chiweruzo changa cholungama? Kodi ungandidzudzule kuti iweyo ukhale wolungama?
Ka laitloeknah he na phae tang aya? Na tang hamla kai nan boe sak aya?
9 Kodi uli ndi dzanja monga la Mulungu, ndipo mawu ako angagunde ngati mphenzi monga a Mulungu?
Nang te Pathen bangla na ban om tih ol neh rhaek bangla na hum a?
10 Ngati zili choncho udzikometsere ndi ulemerero ndi kukongola, ndipo udziveke ulemu ndi ulemerero waufumu.
Hoemdamnah neh na oeknah te oi laeh lamtah mueithennah neh rhuepomnah te bai laeh.
11 Tsanula ukali wako wosefukirawo, uyangʼane aliyense wodzikuza ndipo umuchepetse,
Na thinpom thintoek te sah laeh. Thinthah boeih te so lamtah anih te kunyun sak laeh.
12 Uyangʼane aliyense wodzikweza ndipo umutsitse, uwapondereze oyipa onse pamalo pomwe alilipo.
Thinthah boeih te so lah. Anih te kunyun sak lamtah halang rhoek khaw a hmui la daep laeh.
13 Onsewo uwakwirire pamodzi mfumbi; ukulunge nkhope zawo mʼmanda.
Amih te laipi khuila det lamtah a thuh khuiah khaw a maelhmai te rhenten poi pah.
14 Ukatero Ine ndidzakuvomereza kuti dzanja lako lamanja lakupulumutsadi.
Te vaengah na bantang kut loh nang te n'khang thai tila kai loh nang kang uem van ni.
15 “Taganiza za mvuwu, imene ndinayipanga monga momwe ndinapangira iwe, ndipo imadya udzu ngati ngʼombe.
Behemoth te namah neh kan saii tih saelhung bangla sulrham ka cah coeng ke.
16 Mphamvu zake ndi zazikulu kwambiri, thupi lake ndi lanyonga kwambiri!
A thadueng te a cinghen ah, a thahuem te a bungko kah thanal dongah om coeng ke.
17 Mchira wake umayima tolotolo ngati mtengo wamkungudza; mitsempha ya ntchafu zake ndi yogwirana bwino.
A mai te lamphai thing bangla a hloih tih a phaiboeng, a phaiboeng te a tharhui loh a cut pah.
18 Mafupa ake ali ngati mapayipi amkuwa, nthiti zake zili ngati mipiringidzo yachitsulo.
A rhuh te rhohum tuicawn bangla, a songrhuh khaw thi boeng bangla om.
19 Mvuwuyo ndi yayikulu mwa zolengedwa za Mulungu, komatu mlengi wake amatha kuyiopseza ndi lupanga lake.
Anih tah Pathen kah longpuei a tongnah om tih, anih aka saii long ni a cunghang a tawn thai.
20 Imapeza chakudya chake ku mtunda ndipo nyama zakuthengo zonse zimasewera pambali pake.
Tlang kah cakkoi te anih taengla a phueih uh tih kohong mulhing boeih te pahoi luem uh.
21 Imagona pa tsinde pa zitsamba za mipeta, imabisala mʼbango ndiponso pa thawale.
Yinhnuk ah hlip hmuila capu neh nongtui dongah yalh.
22 Imaphimbika ndi mthunzi wazitsamba za mipeta; imazunguliridwa ndi misondozi ya mu mtsinje.
Anih te hlip kah a hlipkhup loh a dah tih anih te soklong tuirhi loh a vael.
23 Madzi a mu mtsinje akakokoma, sichita mantha, iyo sitekeseka, ngakhale madzi a mu Yorodani afike mʼkhosi mwake.
Tuiva loh a kawt akhaw a tamto moenih. Jordan loh a ka a hoh pa akhaw a omtoem.
24 Kodi alipo amene angathe kukola mvuwu ndi mbedza kapena kuyikola mu msampha?
Anih te a mik neh a loh tih hlaeh neh a hnarhong a toeh a?

< Yobu 40 >