< Yobu 35 >

1 Ndipo Elihu anawonjeza kunena kuti,
UElihu wasephendula wathi:
2 “Kodi mukuganiza kuti mukukhoza? Mukunena kuti, ‘Ndine wolungama pamaso pa Mulungu.’
Ukhumbula ukuthi lokhu kuqondile yini? Uthe: Ukulunga kwami kwedlula okukaNkulunkulu.
3 Komanso inu mukufunsa kuti, ‘Kodi phindu langa nʼchiyani, ndipo ndimapeza chiyani ndikapanda kuchimwa?’
Ngoba uthe kusizani kuwe, kungisizani okwedlula isono sami?
4 “Ine ndikufuna ndikuyankheni inu pamodzi ndi abwenzi anu omwe.
Mina ngizakuphendula, labangane bakho kanye lawe.
5 Yangʼanani kumwamba ndipo muone mitambo imene ili kutali ndi inuyo.
Khangela amazulu ubone; ukhangele amayezi, aphakeme kulawe.
6 Inuyo mukachimwa, Iye zimamukhudza motani? Ngati machimo anu ndi ochuluka, zimenezo zimachita chiyani kwa Iye?
Uba usona, wenzani kuye? Uba iziphambeko zakho zizinengi, wenzani kuye?
7 Ngati inu ndinu wolungama, mumamupatsa Iyeyo chiyani? Kapena Iye amalandira chiyani chochokera mʼdzanja lanu?
Uba ulungile, umnikani, kumbe wemukelani esandleni sakho?
8 Kuyipa kwanu kumangokhudza anthu ngati inuyo, ndipo chilungamo chanu chimakhudza anthu anzanu.
Ububi bakho buthinta umuntu onjengawe, lokulunga kwakho indodana yomuntu.
9 “Anthu akufuwula chifukwa cha kuzunzidwa; akufuna chithandizo kuti achoke pansi pa ulamuliro wa anthu amphamvu.
Ngenxa yobunengi bencindezelo babenza bakhale; bayakhala ngenxa yengalo yabalamandla.
10 Koma palibe amene akunena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga, amene amatisangalatsa nthawi ya usiku,
Kodwa kakho othi: Ungaphi uNkulunkulu umenzi wami, onika amahubo ebusuku,
11 amene amatiphunzitsa kupambana nyama za dziko lapansi ndipo amatipatsa nzeru kupambana mbalame zowuluka?’
osifundisa okwedlula inyamazana zomhlaba, asenze sihlakaniphe okwedlula inyoni zamazulu?
12 Iye sayankha pamene anthu akufuwulira kwa Iye chifukwa cha kudzikuza kwa anthu oyipa.
Lapho bayakhala, kodwa kaphenduli, ngenxa yokuzigqaja kwababi.
13 Ndithu, Mulungu samva kupempha kwawo kopanda pake; Wamphamvuzonse sasamalira zimenezi.
Isibili uNkulunkulu kayikuzwa ize, loSomandla kayikukunanza.
14 Ndipo ndi bodza lalikulu kunena kuti Iye saona zimene zikuchitika. Iye adzaweruza molungama ngati inu mutamudikira
Yebo, lanxa usithi: Kawumboni, kanti isahlulelo siphambi kwakhe; ngakho umlindele.
15 ndiye tsono popeza kuti ukali wake sukupereka chilango, zoyipa zambiri zimene anthu amachita,
Kodwa khathesi, ngoba intukuthelo yakhe ingajezisanga, laye kayikwejwayela kakhulu yini ukuziphakamisa?
16 abambo Yobu mumangoyankhula zopandapake, mukungochulukitsa mawu opanda nzeru.”
Ngakho uJobe uvule umlomo wakhe ngeze, wandisa amazwi engelalwazi.

< Yobu 35 >