< Yobu 35 >

1 Ndipo Elihu anawonjeza kunena kuti,
Eka Elihu nowacho kama:
2 “Kodi mukuganiza kuti mukukhoza? Mukunena kuti, ‘Ndine wolungama pamaso pa Mulungu.’
“Bende iparo ni itimo gima ber kiwacho ni, ‘In kare e nyim Nyasaye?’
3 Komanso inu mukufunsa kuti, ‘Kodi phindu langa nʼchiyani, ndipo ndimapeza chiyani ndikapanda kuchimwa?’
To e iyeno bende ipenjo ni, ‘Mano to konya gangʼo, koso ohala mane ma ayudo ka ok atimo richo?’
4 “Ine ndikufuna ndikuyankheni inu pamodzi ndi abwenzi anu omwe.
“Daher mondo adwoki in kaachiel gi osiepenigo.
5 Yangʼanani kumwamba ndipo muone mitambo imene ili kutali ndi inuyo.
Ngʼiuru polo malo mondo unee boche polo kaka ni kuma bor.
6 Inuyo mukachimwa, Iye zimamukhudza motani? Ngati machimo anu ndi ochuluka, zimenezo zimachita chiyani kwa Iye?
Ka umedo timo richo, to obadhe gangʼo? Kata ka richou ngʼeny to mano nyalo timone angʼo?
7 Ngati inu ndinu wolungama, mumamupatsa Iyeyo chiyani? Kapena Iye amalandira chiyani chochokera mʼdzanja lanu?
Ka un joma kare to bedou makare miye angʼo, koso en angʼo muchiwone?
8 Kuyipa kwanu kumangokhudza anthu ngati inuyo, ndipo chilungamo chanu chimakhudza anthu anzanu.
Timbeu maricho hinyo mana dhano machal kodu, kendo timbeu makare bedo konyruok mana ne yawuot ji.
9 “Anthu akufuwula chifukwa cha kuzunzidwa; akufuna chithandizo kuti achoke pansi pa ulamuliro wa anthu amphamvu.
“Ji ywak malit nikech tingʼ mapek moyie kuomgi; giywak mana ni mondo ogolgi e bwo loch joma thirogi.
10 Koma palibe amene akunena kuti, ‘Kodi ali kuti Mulungu, Mlengi wanga, amene amatisangalatsa nthawi ya usiku,
To onge ngʼato kuomgi mawachoe ni, ‘Nyasaye mane ochweya nikanye, Nyasaye mamiyo ji wende gotieno,
11 amene amatiphunzitsa kupambana nyama za dziko lapansi ndipo amatipatsa nzeru kupambana mbalame zowuluka?’
mapuonjowa gik mathoth moloyo kaka opuonjo le manie piny kendo mamiyo wabedo mariek moloyo winy mafuyo e kor polo?’
12 Iye sayankha pamene anthu akufuwulira kwa Iye chifukwa cha kudzikuza kwa anthu oyipa.
Ok odwok ji ka giywakne nikech wich teko mar joricho.
13 Ndithu, Mulungu samva kupempha kwawo kopanda pake; Wamphamvuzonse sasamalira zimenezi.
Adier, Nyasaye ok chik ite ne ywakgi maonge tiendgi Jehova Nyasaye Maratego ok dewgi.
14 Ndipo ndi bodza lalikulu kunena kuti Iye saona zimene zikuchitika. Iye adzaweruza molungama ngati inu mutamudikira
Iwacho ni Nyasaye ok winj wecheni ka iwacho ni ok inene, kata obedo ni isetero kwayoni e nyime, kendo pod irite mondo odwoki.
15 ndiye tsono popeza kuti ukali wake sukupereka chilango, zoyipa zambiri zimene anthu amachita,
Bende imedo wacho ni kata ji ok okum gi mirimbe mager kendo kata mana richo ma ji timo ok obadhe.
16 abambo Yobu mumangoyankhula zopandapake, mukungochulukitsa mawu opanda nzeru.”
Omiyo Ayub wuoyo ka ngʼama ofuwo; maonge rieko.”

< Yobu 35 >