< Yobu 3 >
1 Pambuyo pake Yobu anatsekula pakamwa pake nayamba kutemberera tsiku limene iyeyo anabadwa.
Tukun wik sac, na Job el fah kasla ac selngawi len se ma osweyukla el.
3 “Tsiku limene ine ndinabadwa litembereredwe ndi usiku umene ananena kuti, ‘Mwana wamwamuna wabadwa!’
“O God, selngawiya fong se ma srimetak nga ah; Ac len se ma osweyukla nga!
4 Tsiku limenelo lisanduke mdima; Mulungu wa kumwambako asalilabadirenso; kuwala kusaonekenso pa tsikulo.
O God, ekulla len sac nu ke lohsr lulap. Nimet kom sifil esam len sac; Ac tia pac lela tuh in oasr kalem tolak len sac.
5 Mdima ndi mthunzi wa imfa zikhale pa tsiku limeneli; mtambo uphimbe tsikuli; mdima wandiweyani udetse kuwala kwake.
Oru tuh in sie len ohkok ac lohsr matoltol; Afinya ke pukunyeng, ac kosrala kalmen faht uh liki.
6 Usiku umenewo ukutidwe ndi mdima wandiweyani; usawerengedwenso pamodzi ndi masiku a chaka, kapena kukhala pa mwezi wina uliwonse.
Eela fong sac liki yac uh, Ac tia lela in sifil oekyuk.
7 Usiku umenewo usabweretse chilichonse chabwino; kusamvekenso nthungululu za chikondwerero.
Oru tuh in wangin koanon fong sac, Sie fong wangin pusren engan lohngyuk.
8 Odziwa kutemberera masiku alitemberere tsikulo, iwo amene akonzekera kuwutsa Leviyatani.
Lela tuh mwet inutnut in selngawi len sac, Elos su etu in pirakak kosro sulallal Leviathan.
9 Nyenyezi zake za mʼbandakucha zikhale mdima; tsikulo liyembekezere kucha pachabe ndipo lisaonenso kuwala koyamba kwa mʼbandakucha.
Lela tuh itu Nasren in tia tolak, Ac oru tuh lohsr lun fong sac in lohsr na, ac tia sifil kalmelik.
10 Pakuti tsiku limenelo ndiye ndinatuluka mʼmimba ya amayi anga ndipo ndi limene linandionetsa zovuta.
Selngawiya fong sac lah pwanang nga isusla, Ac oru nga pula ma upa ac keok.
11 “Bwanji ine sindinawonongeke pamene ndinkabadwa ndi kufa pamene ndimatuluka mʼmimba?
“Nga ke ngan misa na insien nina kiuk ah, Ku ke pacl se na ma osweyukla nga ah.
12 Chifukwa chiyani panali mawondo wondilandirirapo ndi mawere woti andiyamwitsepo?
Mwe mea nina kiuk ah in sruokyuwi finyepal? Mwe mea elan katitiyu?
13 Pakuti tsopano bwenzi ndili gone mwamtendere; ndikanakhala nditagona tulo ndili pa mpumulo
Nga funu misa na in pacl sac, nga lukun mongla na in pacl inge,
14 pamodzi ndi mafumu ndi aphungu a dziko lapansi, amene anadzimangira nyumba zikuluzikulu zimene tsopano ndi mabwinja,
Oanna motul oana tokosra, ku mwet leum Su sifil musaela inkul matu sin mwet leum uh.
15 pamodzi ndi olamulira amene anali ndi golide, amene anadzaza nyumba zawo ndi siliva.
Nga lukun motul na oana fisrak Su nwakla lohm selos ke gold ac silver,
16 Kapena, bwanji sindinakwiriridwe pansi monga mwana wobadwa wakufa kale, ngati khanda limene silinaone kuwala kwa dzuwa?
Ku motul oana sie tulik fusr ma misa na meet liki el isusla uh.
17 Ku mandako anthu oyipa sakhalanso pa mavuto, ndipo kumeneko anthu otopa ali pa mpumulo.
In kulyuk uh, mwet koluk ac tila orekma koluk, Ac mwet orekma su totola elos eis pacl in mongla lalos ke elos oan in kulyuk uh.
18 A mʼndende kumeneko akusangalala ndi mtendere; sakumvanso mawu ofuwula a kapitawo wa akapolo.
Mwet sruoh ma misa tari elos muta in misla, Ac elos sukosok liki pusren sapsap ac kas kou.
19 Anthu wamba ndi anthu apamwamba ali kumeneko, ndipo kapolo ndi womasuka kwa mbuye wake.
Mwet nukewa ac sun misa — mwet pwengpeng oayapa mwet tia eteyu — Ac mwet foko elos sukosokla.
20 “Chifukwa chiyani dzuwa limawalira iwo amene ali pa mavuto, ndipo moyo umapatsidwa kwa owawidwa mtima,
“Efu ku kom oru tuh mwet uh in mutana in moul keok? Efu ku kom sang kalem in tolak mwet asor?
21 kwa iwo amene amalakalaka imfa imene sibwera, amene amayifunafuna imfayo kupambana chuma chobisika,
Elos tupanna elos in misa, a elos tiana misa. Elos lungse kulyuk uh liki kutena mwe kasrup.
22 amene amakondwa ndi kusangalala akamalowa mʼmanda?
Elos ac tiana engan nwe ke na elos misa ac pukpuki.
23 Chifuwa chiyani moyo umaperekedwa kwa munthu amene njira yake yabisika, amene Mulungu wamuzinga ponseponse?
God El okanlana ma ac sikyak nu selos tok uh, Ac El kosralosla tuh elos in tia ku in oru kutena ma.
24 Mʼmalo moti ndidye, ndimalira, ndi kubuwula kwanga nʼkosalekeza.
Nga tia mongo — nga tung na, Ac nga tia ku in kutongya sasao luk.
25 Chimene ndinkachiopa chandigwera; chimene ndinkachita nacho mantha chandichitikira.
Ma nukewa ma nga sangeng ac sensen kac uh sikyak.
26 Ndilibe mtendere kapena bata, ndilibe mpumulo, koma mavuto okhaokha.”
Wangin misla nu sik, wangin mongla luk, Ac wangin saflaiyen mwe lokoalok nu sik.”