< Yobu 3 >
1 Pambuyo pake Yobu anatsekula pakamwa pake nayamba kutemberera tsiku limene iyeyo anabadwa.
Eso fesuale da baligili, Yoube da ouiya: le esalu amo sia: baoui amola e lalelegei eso amo gagabuli amane sia: i,
3 “Tsiku limene ine ndinabadwa litembereredwe ndi usiku umene ananena kuti, ‘Mwana wamwamuna wabadwa!’
“A: i! Gode! Na lalelegei eso amoga gagabuli sia: ma! Na: mea hagomo ganodini hamobe galu amoga gagabuli sia: ma!
4 Tsiku limenelo lisanduke mdima; Mulungu wa kumwambako asalilabadirenso; kuwala kusaonekenso pa tsikulo.
Gode, amo eso bu gasilisima. Amo eso bu maedafa bu dawa: loma. Amo esoga hadigi bu mae diga: ma: ma.
5 Mdima ndi mthunzi wa imfa zikhale pa tsiku limeneli; mtambo uphimbe tsikuli; mdima wandiweyani udetse kuwala kwake.
Amo eso gasi dunasima: ne hamoma. Mu mobi da amo eso hadigi dedeboma: ne hamoma! Amola eso ea diga: be uligilisima.
6 Usiku umenewo ukutidwe ndi mdima wandiweyani; usawerengedwenso pamodzi ndi masiku a chaka, kapena kukhala pa mwezi wina uliwonse.
Amo gasi odega dialebe fadegama! Amo gasi odega dialebe bu mae idima: ma.
7 Usiku umenewo usabweretse chilichonse chabwino; kusamvekenso nthungululu za chikondwerero.
Na: mea hagomo ganodini hamobe gasi, amo da da: i dioi bagade amola hamedei agoane ba: mu da defea.
8 Odziwa kutemberera masiku alitemberere tsikulo, iwo amene akonzekera kuwutsa Leviyatani.
Gabi dawa: su dunu (amo da hanome agoai ohe bagade Lifaiada: ne ouligimusa: dawa: ) ilia da amo gasiga gagabusu aligima: ne sia: mu da defea.
9 Nyenyezi zake za mʼbandakucha zikhale mdima; tsikulo liyembekezere kucha pachabe ndipo lisaonenso kuwala koyamba kwa mʼbandakucha.
Dia gusubia gasumuni ea diga: be amo uligilisima. Amola amo gasi mae hadigima: ne hamoma!
10 Pakuti tsiku limenelo ndiye ndinatuluka mʼmimba ya amayi anga ndipo ndi limene linandionetsa zovuta.
Amo gasi da na lalelegemu logo doasiba: le, amo gasiga gagabusu aligima: ne sia: ma. Bai amo gasi da nama bidi hamosu amola se nabasu fawane iasi.
11 “Bwanji ine sindinawonongeke pamene ndinkabadwa ndi kufa pamene ndimatuluka mʼmimba?
Na da na: me hina: hagomoa ganodini bogomu da defea galu. O lalelegesula amogalawane bogomu da defea galu.
12 Chifukwa chiyani panali mawondo wondilandirirapo ndi mawere woti andiyamwitsepo?
Na: me da abuliba: le ea masele da: iya na febela: ? Abuliba: le nama dodo iasula: ?
13 Pakuti tsopano bwenzi ndili gone mwamtendere; ndikanakhala nditagona tulo ndili pa mpumulo
Na amogala bogosa ganiaba, na da wali hele esala: loba!
14 pamodzi ndi mafumu ndi aphungu a dziko lapansi, amene anadzimangira nyumba zikuluzikulu zimene tsopano ndi mabwinja,
Na da hina bagade amola ouligisu dunu amo da musa: hina bagade diasu buga: le gagui, amo defele golai diala: loba.
15 pamodzi ndi olamulira amene anali ndi golide, amene anadzaza nyumba zawo ndi siliva.
Na da hina bagade manolali amo da ilia diasu silifa amola gouli amoga nabalesi, amo defele golai diala: loba.
16 Kapena, bwanji sindinakwiriridwe pansi monga mwana wobadwa wakufa kale, ngati khanda limene silinaone kuwala kwa dzuwa?
O na da daba: me asi mano agoai golai diala: loba.
17 Ku mandako anthu oyipa sakhalanso pa mavuto, ndipo kumeneko anthu otopa ali pa mpumulo.
Bogoi uli dogoi ganodini, wadela: i hamosu dunu da wadela: le hame hamosa. Amola hawa: hamonana helei dunu ilia da hawa: hamosu fisili, helefisa.
18 A mʼndende kumeneko akusangalala ndi mtendere; sakumvanso mawu ofuwula a kapitawo wa akapolo.
Bogoi uli dogoi ganodini sali dunu ili amolawane da olofosu ba: sa. Amogawi ouligisu dunu da ilima hame halagala: sa.
19 Anthu wamba ndi anthu apamwamba ali kumeneko, ndipo kapolo ndi womasuka kwa mbuye wake.
Amogawi, dunu huluane bogogia: i dialebe ba: sa. Mimogo dunu amola asaboi dunu huluanedafa da bogoi uli dogoiga doaga: le, dialebe. Udigili hawa: hamosu dunu da ilia udigili hawa: hamosu amoga fisiagai agoane ba: sa.
20 “Chifukwa chiyani dzuwa limawalira iwo amene ali pa mavuto, ndipo moyo umapatsidwa kwa owawidwa mtima,
Dia da abuliba: le, dunu se bagade nabawane esaloma: ne, ilia logo doasisala: ? Abuliba: le, da: i dioi bagade dunuma hadigi iaha?
21 kwa iwo amene amalakalaka imfa imene sibwera, amene amayifunafuna imfayo kupambana chuma chobisika,
Ilia da bogoma: ne ouligisa, be bogosu da ilima hame doaga: sa. Ilia da osobo bagade noga: idafa liligi hame hanai, bogoi uli dogoi fawane hanai gala.
22 amene amakondwa ndi kusangalala akamalowa mʼmanda?
Ilia da bogole, uli dogoiba: le fawane hahawane ba: sa.
23 Chifuwa chiyani moyo umaperekedwa kwa munthu amene njira yake yabisika, amene Mulungu wamuzinga ponseponse?
Gode da ilima fa: no misunu hou wamolegesa. Amola ili mae hobeama: ne, E da ili sisiga: sa.
24 Mʼmalo moti ndidye, ndimalira, ndi kubuwula kwanga nʼkosalekeza.
Na da ha: i mae nawane, unuma: ne fawane dinana. Na da gogonomonanusu da yolemu hamedei gala.
25 Chimene ndinkachiopa chandigwera; chimene ndinkachita nacho mantha chandichitikira.
Liligi huluane amoga na beda: be da dafawane hamosa.
26 Ndilibe mtendere kapena bata, ndilibe mpumulo, koma mavuto okhaokha.”
Na olofosu amola helefisu hamedafa dawa: , amola nama bidi hamosu da yolemu hame ba: sa.”