< Yobu 25 >

1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
Şuahlı Bildat şöyle yanıtladı:
2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
“Egemenlik ve heybet Tanrı'ya özgüdür, Yüce göklerde düzen kuran O'dur.
3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
Orduları sayılabilir mi? Işığı kimin üzerine doğmaz?
4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
İnsan Tanrı'nın önünde nasıl doğru olabilir? Kadından doğan biri nasıl temiz olabilir?
5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
O'nun gözünde ay parlak, Yıldızlar temiz değilse,
6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”
Nerede kaldı bir kurtçuk olan insan, Bir böcek olan insanoğlu!”

< Yobu 25 >