< Yobu 25 >

1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
Nanoiñe amy zao t’i Bildade nte-Sohy:
2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
Aze ty fifeheañe naho ty fañeveñañe; ampanintsiña’e ty andindi’e ao.
3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
Tsi-vatse o lahin-defo’eo! ama’ia ty tsy anjiriha’ i hazavà’ey?
4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
Aia te ho to aolon’Añahare ondatio? Aia te halio ty nasaman-drakemba?
5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
Ndra i volañey tsy mazava vaho tsy ki’e am-pivazohoa’e o vasiañeo,
6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”
àntsake ondatio, fa oletse, naho o ana’ ondatio, fa aisañe.

< Yobu 25 >