< Yobu 25 >

1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
時にシユヒ人ビルダデこたへて曰く
2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
神は大權を握りたまふ者 畏るべき者にましまし 高き處に平和を施したまふ
3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
その軍旅數ふることを得んや 其光明なに物をか照さざらん
4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
然ば誰か神の前に正義かるべき 婦人の產し者いかでか清かるべき
5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
視よ月も輝かず 星も其目には清明ならず
6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”
いはんや蛆のごとき人 蟲のごとき人の子をや

< Yobu 25 >