< Yobu 25 >

1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
and to answer Bildad [the] Shuhite and to say
2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
to rule and dread with him to make peace in/on/with height his
3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
there number to/for band his and upon who? not to arise: rise light his
4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
and what? to justify human with God and what? to clean to beget woman
5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
look! till moon and not to shine and star not be clean in/on/with eye his
6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”
also for human worm and son: child man worm

< Yobu 25 >