< Yobu 25 >
1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
Nu nam Bildad van Sjóeach het woord, en sprak:
2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
Hem is de macht en de schrik, Hem, die vrede gebiedt in zijn hoge hemel!
3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
Zijn soms zijn legioenen te tellen, Tegen wien staan zijn troepen niet op!
4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
Hoe kan dan een mens tegen God in zijn recht zijn, Of rein, die uit een vrouw is geboren?
5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
Zie, zelfs de maan is niet helder, De sterren zijn niet rein in zijn ogen:
6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”
Hoeveel minder een mens, een aas, Een mensenkind, een worm!