< Yobu 25 >

1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
Tedy odpovídaje Bildad Suchský, řekl:
2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
Panování a hrůza Boží působí pokoj na výsostech jeho.
3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
Zdaliž jest počet vojskům jeho? A nad kým nevzchází světlo jeho?
4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
Jakž by tedy spravedliv býti mohl bídný člověk před Bohem silným, aneb jak čist býti narozený z ženy?
5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
Hle, ani měsíc nesvítil by, ani hvězdy nebyly by čisté před očima jeho,
6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”
Nadto pak smrtelný člověk, jsa jako červ, a syn člověka, jako hmyz.

< Yobu 25 >