Preface
Bibles
+
CHW
CSG
X
<
h5467
>
X
<
^
>
<
>
<
Yobu
25
>
1
Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
叔亞人彼耳達得發言說:
2
“Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
權能和威嚴為他所有,他在高天締造和平。
3
Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
他的隊伍,豈可勝數﹖他的光明升起,誰不蒙受照耀﹖
4
Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
人在天主面前,怎能自以為義﹖婦人所生的,怎能自稱潔淨﹖
5
Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
在他眼中,月亮都不明亮,星辰也不皎潔,
6
nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”
何況像蟲的人,像蛆的人子!
<
Yobu
25
>
Go to
>
Bookmark
/
Concordance
/
Maps
/
Report Issue
The world's first Holy Bible un-translation!