< Yobu 25 >

1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
叔亞人彼耳達得發言說:
2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
權能和威嚴為他所有,他在高天締造和平。
3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
他的隊伍,豈可勝數﹖他的光明升起,誰不蒙受照耀﹖
4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
人在天主面前,怎能自以為義﹖婦人所生的,怎能自稱潔淨﹖
5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
在他眼中,月亮都不明亮,星辰也不皎潔,
6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”
何況像蟲的人,像蛆的人子!

< Yobu 25 >