< Yobu 25 >

1 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
Te phoeiah Shuhi Bildad loh a doo tih,
2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu, Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
“A taemrhai ham neh birhihnah he amah hut ni. Amah kah hmuensang ah rhoepnah a saii.
3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka? Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
A caem taengah hlangmi om nim? U soah nim amah kah vangnah a hlah pawh.
4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu? Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
Te dongah hlanghing he Pathen taengah metlam a tang thai? Huta kah a sak te metlam a cim eh?
5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni, ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
A mikhmuh ah hla pataeng khaw aa pawt tih aisi khaw a cil moenih.
6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi, mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”
Hlanghing aisat a rhit banghui ni, hlang capa khaw talam banghui,” a ti nah.

< Yobu 25 >