< Yobu 22 >

1 Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha kuti,
A LAILA olelo aku o Elipaza, i aku la,
2 “Kodi munthu nʼkukhala waphindu kwa Mulungu? Kodi munthu wanzeru angamupindulire Iye?
E hiki anei i ke kanaka, ke hoopomaikai i ke Akua, E like me ka mea naauao, e hoopomaikai ia ia iho?
3 Kodi Wamphamvuzonse akanapeza chabwino chotani iweyo ukanakhala wolungama? Kodi iyeyo akanapeza phindu lanji makhalidwe ako akanakhala angwiro?
He mea oluolu anei ke pono oe i ka Mea mana? A e waiwai anei oia ke hoohemolele oe i kou mau aoao?
4 “Kodi nʼchifukwa choti umamuopa, kuti azikudzudzula, kuti azifuna kukukokera ku mlandu?
No ka makau ia oe, e hoopaapaa mai anei ia ia oe? E hele mai anei ia me oe ma ka hooponopono ana?
5 Kodi osati nʼchifukwa chakuti kuyipa kwako nʼkwakukulu? Kodi machimo ako si opanda malire?
Aole anei he nui kou hewa? A ua hope ole kou mau hala?
6 Iwe unkawumiriza abale ako kuti akupatse chikole popanda chifukwa; umalanda anthu zovala zawo ndi kuwasiya amaliseche.
No ka mea, ua hoopanai wale oe i kou hoahanau, A ua lawe oe i na aahu o ka poe kapa ole.
7 Sunawapatse madzi anthu otopa, ndipo unawamana chakudya anthu anjala,
Aole oe i haawi i ka wai i ka mea nawaliwali, A ua ana oe i ka berena i ka mea pololi.
8 ngakhale unali munthu wamphamvu, wokhala ndi malo akeake, munthu waulemu wake, wokhala mʼdzikomo.
Aka, o ke kanaka ikaika, nona ka honua; A noho iho la ka mea koikoi ilaila.
9 Ndipo akazi amasiye unawachotsa wopanda kanthu, ndipo unapondereza ana amasiye.
Ua hoihoi nele aku oe i na wahinekanemake, A ua paopaoia na lima o na mea makua ole.
10 Nʼchifukwa chake misampha yakuzungulira, nʼchifukwa chake tsoka ladzidzidzi lakuchititsa mantha,
Nolaila ua puni oe i na pahele, A o ka makau wale ke hooweliweli mai nei ia oe;
11 nʼchifukwa chake kuli mdima kuti sungathe kuona kanthu, nʼchifukwa chakenso madzi achigumula akumiza.
A o ka pouli paha au i ike ole ai; A he nui loa ka wai e halana ana maluna ou.
12 “Kodi Mulungu sali kutalitali kumwamba? Ndipo ona nyenyezi zili mmwamba kwambirizo, ona kutalika kwake pamene zililipo!
Aole anei ke Akua ma ka lani kiekie? Aia hoi, ke poo o na hoku, ua kiekie lakou.
13 Komabe iweyo ukunena kuti, ‘Kodi Mulungu amadziwa chiyani? Kodi Iye amaweruza mu mdima woterewu?
A i mai la oe, Pehea la ke Akua e ike ai? E hiki anei ia ke hooponopono mawaena mai o ke ao pouli?
14 Mitambo yakuda yamuphimba, kotero kuti Iye sakutiona pamene akuyendayenda pamwamba pa thambopo.’
O na ao naulu ka uhi nona, i ike ole ai ia, A hele no ia ma ka poai o ka lani.
15 Kodi iwe udzayendabe mʼnjira yakale imene anthu oyipa ankayendamo?
Ua noonoo pono anei oe i ka aoao kahiko, Kahi a ka poe hewa i hele ai?
16 Iwo anachotsedwa nthawi yawo isanakwane, maziko awo anakokoloka ndi madzi achigumula.
Ka poe i noopauia mamua o ka manawa, Ua nininiia ke kaiakahinalii maluna o ko lakou kahua;
17 Anthuwo anati kwa Mulungu, ‘Tichokereni! Kodi Wamphamvuzonse angatichitire chiyani?’
Ka poe i olelo aku i ke Akua, E hele mai o makou aku; A heaha ka ka Mea mana e hana mai ai no lakou?
18 Chonsecho ndi Iye amene anadzaza nyumba zawo ndi zinthu zabwino, choncho ine sindigwirizana ndi uphungu wa anthu oyipa.
Ua hoopiha no nae ia i ko lakou mau hale i ka waiwai; Aka. o ka manao o ka poe hewa ua mamao loa aku ia ia'u.
19 “Anthu olungama amaona kuwonongeka kwawo ndipo amakondwera; anthu osalakwa amangoseka, akamuona woyipa akulangidwa.
Ua ike no ka poe pono ia, a olioli, A akaaka ka poe hala ole ia lakou.
20 Amanena kuti, ‘Ndithudi adani athu awonongeka ndipo moto wawononga chuma chawo!’
Ina paha ua lukuia ko makou poe enemi, A ua hoopauia ka waiwai nui o lakou i ke ahi.
21 “Gonjera Mulungu kuti ukhale naye pamtendere; ukatero udzaona zabwino.
E hookuikahi ae me ia ano, a e pomaikai; Pela no e hiki mai ai ka pomaikai ia oe.
22 Landira malangizo a pakamwa pake ndipo usunge mawu ake mu mtima mwako.
Ke koi aku nei au ia oe, E lawe oe i ke kanawai mai kona waha mai, A e waiho oe i kana mau olelo iloko o kou naau.
23 Ukabwerera kwa Wamphamvuzonse udzabwezeretsedwa; ukachotsa zoyipa zonse zimene zimachitika mʼnyumba mwako,
Ina e hoi hou oe i ka Mea mana, e kukuluia oe, E hoomamao loa aku oe i ka hewa mai kou mau halelewa aku.
24 ndipo chuma chamtengowapatali nuchiona ngati fumbi, golide wa ku Ofiri numutaya ku miyala ya ku zigwa.
A e hoolei aku oe i kou houlunlu ana i ke gula i ka lepo, A i ke gula Opira hoi i na pohaku o na kahawai
25 Pamenepo Wamphamvuzonseyo adzakhala golide wako, siliva wako wamtengowapatali.
A o ka Mea mana kou gula, A me ke kala o na waiwai nou.
26 Pamenepo udzakondwera naye Wamphamvuzonse ndipo udzakweza nkhope yako kwa Mulungu.
No ka mea, alaila e hauoli oe i ka Mea mana, A e hoala ae i kou maka i ke Akua.
27 Udzamupempha ndipo adzakumvera, ndipo udzapereka zimene unalonjeza.
E pule aku no oe ia ia, a e hoolohe mai ia ia oe, A e hooko aku oe i na mea au i hoohiki ai.
28 Chimene watsimikiza kuti uchite, chidzachitikadi, kuwala kudzakuwunikira pa njira yako.
A e noonoo oe i kahi mea, a e hoopaaia oia nou; A e alohi mai ka malamalama maluna o kou mau ala.
29 Pamene anthu agwetsedwa pansi, iwe nʼkunena kuti, ‘Akwezeni!’ Pamenepo Iye adzapulumutsa anthu oponderezedwa.
A e hoohaahaaia lakou, alaila e olelo oe, He kiekie; A e hoola mai no ia i ka mea i kulou na maka.
30 Iye adzapulumutsa ngakhale munthu amene ndi wolakwa, ameneyo adzapulumutsidwa kudzera mʼkulungama kwako.”
E hoopakele no ia i ka mea lawe hala; A e hoopakeleia oia ma ka maemae o kou mau lima.

< Yobu 22 >