< Yobu 19 >

1 Pamenepo Yobu anayankha kuti,
Eka Ayub nodwoko niya,
2 “Kodi mudzakhala mukundizunza mpaka liti, ndi kundilasa ndi mawu anuwo?
“Ubiro chando chunya nyaka karangʼo ka uchuoya gi weche?
3 Inuyo mwandinyoza kwambiri; mwanditsutsa mopanda manyazi.
Koro useyanya nyadipar kendo uonge gi wichkuot ka umonja.
4 Ngati ndi zoona kuti ine ndasochera, cholakwachotu nʼchanga.
Kapo ni en adier ni asebaro mabor, to mano obadhou gangʼo.
5 Ngati ndithudi mukudziyika nokha pamwamba panga, ndi kugwiritsa ntchito kunyozedwa kwanga polimbana nane,
To kapo ni unyalo tingʼoru malo moloya kendo uchuoya gi wach nikech chandruok ma an-go,
6 pamenepa dziwani kuti Mulungu wandilakwira ndipo wandizinga ukonde wake.
to kara ngʼeuru ni Nyasaye osechwanya kendo gogo mare osemaka.
7 “Ngakhale ndifuwule kuti, ‘Akundizunza!’ Palibe wondiyankha; ngakhale ndipemphe thandizo, palibe wondichitira zolungama.
“Ka aywak ni, ‘Itimona marach!’ Onge ngʼama dewa; to kata ka adwaro kony, to ok anyal yudo.
8 Mulungu wanditsekera njira yanga kotero sindingathe kudutsa; waphimba njira zanga ndi mdima.
Osedino yorena ma ok anyal kalo; kendo osemiyo kuonde maluwo otimo mudho.
9 Iye wandilanda ulemu wanga ndipo wandivula chipewa chaufumu pamutu panga.
Osemaya duongʼna mi ogolo osimbo e wiya.
10 Wandiphwanyaphwanya mbali zonse ndipo ndatheratu; Iye wazula chiyembekezo changa ngati mtengo.
Oseturo denda duto motieka kendo opudho genona ka ngʼama pudho yien.
11 Wandikwiyira ndipo akundiyesa mmodzi mwa adani ake.
Mirimbe maliel ka mach ni kuoma; kendo okwana kaka achiel kuom wasike.
12 Ankhondo ake akubwera kwa ine mwamphamvu, akonzekera zodzalimbana nane ndipo azungulira nyumba yanga.
Jolweny mage pangore kochoma gi tekregi duto; gigona agengʼa ka gidwaro kedo koda, kendo giguro hembegi e alwora mar dalana.
13 “Mulungu wandisiyanitsa ndi abale anga; wasandutsa odziwana nane kukhala achilendo kwa ine.
“Osepoga gi owetena monywolago; kendo jogo mosiepena bende oseringo oweya.
14 Abale anga andithawa; abwenzi anga andiyiwala.
Anywolana oseringo oweya; kendo osiepena wigi osewil koda.
15 Anthu odzacheza ku nyumba kwanga ndiponso antchito anga aakazi andisandutsa mlendo; ndasanduka mlendo mʼmaso mwawo.
Wenda gi jotichna ma nyiri kwana kaka ngʼat ma gikia; kendo ginena kaka japiny moro.
16 Ndikayitana wa ntchito wanga, iye sandiyankha, ngakhale ndikapempha ndi pakamwa panga sandichitira kanthu.
Ka aluongo jatichna moro kata bed mana ni asaye gi dhoga awuon, to ok odewa.
17 Mpweya wanga umamunyansa mkazi wanga; ndine chinthu chonyansa kwa abale anga a mimba imodzi.
Chiega ok dwar winjo tikna; kendo kata mana owetena bende ok dwar sudo buta machiegni.
18 Inde, ngakhale ana amandinyoza; akandiona amandinyodola.
Nyaka yawuowi matindo bende jara; kendo ka ginena, to ginyiera.
19 Anzanga onse apamtima amanyansidwa nane; iwo amene ndinkawakonda andiwukira.
Osiepena mageno ok dwara; jogo mane chunya ohero bende ok dwara.
20 Ndangotsala khungu ndi mafupa okhaokha; ndapulumuka lokumbakumba.
Adhero mi adongʼ choke lilo; kendo gima adongʼ-go en mana ring laka.
21 “Mvereni chisoni, inu abwenzi anga, mvereni chisoni, pakuti dzanja la Mulungu landikantha.
“Kechauru, yaye osiepena, kechauru, nikech lwet Nyasaye osetieka.
22 Chifukwa chiyani mukundilondola ngati Mulungu? Kodi simunatope nalo thupi langa?
Angʼo momiyo ulaworu koda kaka Nyasaye lawa? Sando ringra pok oromou?
23 “Aa, achikhala mawu anga analembedwa, achikhala analembedwa mʼbuku,
“Yaye, mad ne ngʼato mak wechegagi, kendo ndikgi e kitabu,
24 akanalembedwa pa mwala ndi chitsulo, akanalembedwa pa thanthwe kuti sangathe kufufutidwa!
kata ndikgi gi kalamb chuma, kata ne gorgi e lwanda kama ok ginyal ruchoree!
25 Koma ndikudziwa kuti mpulumutsi wanga ali ndi moyo, ndipo pa nthawi yomaliza adzabwera kudzanditeteza.
Angʼeyo ni Jawarna nitie kendo ngima, kendo chiengʼ giko nochungʼ kongʼado bura ne piny.
26 Ndipo khungu langa litatha nʼkuwonongeka, mʼthupi langa lomweli ndidzamuona Mulungu.
Kata ka tuo oketho denda kamano, to e ringruogni anane Nyasaye.
27 Ine ndemwe ndidzamuona Iye ndi maso angawa, ineyo, osati wina ayi. Ndithu mtima wanga ukufunitsitsadi!
Adier, ananene gi wangʼa awuon mana an ma ok ngʼat moro. Mano kaka chunya ogeno odiechiengno!
28 “Koma inu mukuti, ‘Haa! Tingamuzunze bwanji, popeza kuti zonsezi zaoneka chifukwa cha iye yemweyo?’
“Ka uwacho ni, ‘Mano kaka udhi nyime kungʼadona bura, mana ka gima oseyala moseyudi ni an jaketho,’
29 Inu muyenera kuopa lupanga; pakuti mkwiyo wake umalangadi ndi lupanga; zikadzatero muzadziwa kuti chiweruzo chilipo ndithu.”
to un bende asiemou ni ibiro kumou; nikech paro marach ma un-gono, eka unungʼe ni nitiere chiengʼ ngʼado bura.”

< Yobu 19 >