< Yobu 17 >

1 “Mtima wanga wasweka, masiku anga atha, manda akundidikira.
Me sunsum atɔ piti, me nna so atwa, na damena retwɛn me.
2 Ndithudi, anthu ondiseka andizungulira; maso anga akupenyetsetsa mdani wanga.
Ampa ara fɛdifoɔ atwa me ho ahyia; ɛsɛ sɛ mehwɛ wɔn atutupɛ.
3 “Inu Mulungu, patseni chikole chimene mukufuna. Ndani wina amene adzandiperekera ine chikole?
“Ao Onyankopɔn, hyɛ me ɛbɔ a wopɛ. Hwan bio na ɔbɛma me banbɔ?
4 Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu; choncho simudzawalola kuti apambane.
Woato wɔn adwene mu a wɔnte asɛm ase; enti woremma wɔnni nkonim.
5 Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma, ana ake sadzaona mwayi.
Sɛ obi sopa ne nnamfonom de nya akatua a, ne mma ani bɛfira.
6 “Mulungu wandisandutsa chisudzo chochiseka aliyense, munthu amene anthu amalavulira malovu nkhope yake.
“Onyankopɔn de me ayɛ asɛm a ɛda obiara ano, obi a wɔte ntasuo gu nʼani so.
7 Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni; ndawonda ndi mutu womwe.
Awerɛhoɔ ama mʼani ayɛ samoo me bɔberɛ nyinaa yɛ sunsumma.
8 Anthu olungama akudabwa nazo zimenezi; anthu osachimwa akupsera mtima anthu osapembedza Mulungu.
Ateneneefoɔ hunu me a, ɛyɛ wɔn nwanwa. Wɔn a wɔdi bem no bɛsɔre atia wɔn a wɔnni nyamesu.
9 Komabe anthu olungama adzasunga njira zawo, ndipo anthu a makhalidwe abwino mphamvu zawo zidzanka zikuchuluka.
Ateneneefoɔ bɛkɔ wɔn anim, na wɔn a wɔn nsa ho teɛ bɛkɔ so anya ahoɔden.
10 “Tsono bwerani nonsenu, bwerezaninso mawu anuwo, sindidzapezapo munthu wanzeru pakati panupo.
“Mo nyinaa mo nsane mmra mmɛsɔ me nhwɛ! Na merennya onyansafoɔ wɔ mo mu.
11 Masiku anga atha, zimene ndinakonza zalephereka, pamodzinso ndi zokhumba za mtima wanga.
Me nna atwam, me nhyehyɛeɛ apansam, saa ara na mʼakoma apɛdeɛ nso ayɛ.
12 Anthu awa amasandutsa usiku kukhala usana, nthawi ya usiku iwo amati ‘kwatsala pangʼono kucha.’
Saa nnipa yi ma anadwo dane awia; esum mu koraa no, wɔka sɛ, ‘Hann abɛn,’
13 Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
Sɛ efie baako pɛ a mʼani da so ne damena, sɛ mesɛ me kɛtɛ wɔ esum mu, (Sheol h7585)
14 ngati ndinena kwa dzenje la manda ‘ndinu abambo anga,’ ndiponso kwa mphutsi kuti, ‘ndinu amayi anga’ kapena ‘mlongo wanga,’
sɛ meka kyerɛ porɔeɛ sɛ, ‘Woyɛ mʼagya,’ na me kyerɛ ɔsonsono sɛ, ‘Me maame’ anaa ‘Me nuabaa’ a,
15 tsono chiyembekezo changa chili kuti? Ndani angaone populumukira panga?
na afei mʼanidasoɔ wɔ he? Hwan na ɔbɛtumi anya anidasoɔ bi ama me?
16 Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)
Ɛbɛsiane akɔ owuo ɛpono ano anaa? Yɛn nyinaa bɛsiane akɔ mfuturo mu anaa?” (Sheol h7585)

< Yobu 17 >