< Yobu 17 >

1 “Mtima wanga wasweka, masiku anga atha, manda akundidikira.
Min Aand er brudt, mine Dage ere udslukkede, Gravene vente mig.
2 Ndithudi, anthu ondiseka andizungulira; maso anga akupenyetsetsa mdani wanga.
Er der ikke Spot omkring mig, og maa mit Øje ikke dvæle ved deres Genstridighed?
3 “Inu Mulungu, patseni chikole chimene mukufuna. Ndani wina amene adzandiperekera ine chikole?
Kære, stil mig Borgen hos dig, lov for mig; hvo er der ellers, der giver mig Haandslag?
4 Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu; choncho simudzawalola kuti apambane.
Thi du har lukket deres Hjerte for Indsigt, derfor skal du ikke ophøje dem.
5 Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma, ana ake sadzaona mwayi.
Man byder Venner ud til Bytte, og deres Børns Øjne hentæres.
6 “Mulungu wandisandutsa chisudzo chochiseka aliyense, munthu amene anthu amalavulira malovu nkhope yake.
Men han har stillet mig til at være et Ordsprog iblandt Folkene, og jeg er bleven som den, man spytter i Ansigtet.
7 Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni; ndawonda ndi mutu womwe.
Derfor er mit Øje mørkt af Harm, og alle mine Lemmer ere som en Skygge.
8 Anthu olungama akudabwa nazo zimenezi; anthu osachimwa akupsera mtima anthu osapembedza Mulungu.
For sligt maa de oprigtige forskrækkes, og den uskyldige harmes over den vanhellige.
9 Komabe anthu olungama adzasunga njira zawo, ndipo anthu a makhalidwe abwino mphamvu zawo zidzanka zikuchuluka.
Dog holder den retfærdige fast ved sin Vej, og den, som har rene Hænder, faar mere Styrke.
10 “Tsono bwerani nonsenu, bwerezaninso mawu anuwo, sindidzapezapo munthu wanzeru pakati panupo.
Men I, kommer kun alle frem igen, og jeg vil dog ikke finde en viis iblandt eder.
11 Masiku anga atha, zimene ndinakonza zalephereka, pamodzinso ndi zokhumba za mtima wanga.
Mine Dage ere gangne forbi; oprykkede ere mine Tanker, hvilke mit Hjerte besad.
12 Anthu awa amasandutsa usiku kukhala usana, nthawi ya usiku iwo amati ‘kwatsala pangʼono kucha.’
De gøre Nat til Dag; og Lyset skal være nær, naar Mørket kommer.
13 Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
Dersom jeg end forventer noget, da er det Graven som min Bolig; jeg har redet mit Leje i Mørket. (Sheol h7585)
14 ngati ndinena kwa dzenje la manda ‘ndinu abambo anga,’ ndiponso kwa mphutsi kuti, ‘ndinu amayi anga’ kapena ‘mlongo wanga,’
Jeg har raabt til Graven: Du er min Fader! til Ormen: Min Moder og min Søster!
15 tsono chiyembekezo changa chili kuti? Ndani angaone populumukira panga?
Hvor skulde da min Forventelse være? ja min Forventelse — hvo skuer den?
16 Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)
Den skal nedfare til Gravens Porte, naar der tilmed bliver Ro i Støvet. (Sheol h7585)

< Yobu 17 >