< Yobu 17 >

1 “Mtima wanga wasweka, masiku anga atha, manda akundidikira.
Dýchání mé ruší se, dnové moji hynou, hrobu blízký jsem.
2 Ndithudi, anthu ondiseka andizungulira; maso anga akupenyetsetsa mdani wanga.
Jistě posměvači jsou u mne, a pro jejich mne kormoucení nepřichází ani sen na oči mé.
3 “Inu Mulungu, patseni chikole chimene mukufuna. Ndani wina amene adzandiperekera ine chikole?
Postav mi, prosím, rukojmě za sebe; kdo jest ten, nechť mi na to ruky podá.
4 Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu; choncho simudzawalola kuti apambane.
Nebo srdce jejich přikryl jsi, aby nerozuměli, a protož jich nepovýšíš.
5 Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma, ana ake sadzaona mwayi.
Kdož pochlebuje bližním, oči synů jeho zhynou.
6 “Mulungu wandisandutsa chisudzo chochiseka aliyense, munthu amene anthu amalavulira malovu nkhope yake.
Jistě vystavil mne za přísloví lidem, a za divadlo všechněm,
7 Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni; ndawonda ndi mutu womwe.
Tak že pro žalost pošly oči mé, a oudové moji všickni stínu jsou podobni.
8 Anthu olungama akudabwa nazo zimenezi; anthu osachimwa akupsera mtima anthu osapembedza Mulungu.
Užasnouť se nad tím upřímí, a však nevinný proti pokrytci vždy se zsilovati bude.
9 Komabe anthu olungama adzasunga njira zawo, ndipo anthu a makhalidwe abwino mphamvu zawo zidzanka zikuchuluka.
Přídržeti se bude, pravím, spravedlivý cesty své, a ten, jenž jest čistých rukou, posilní se více.
10 “Tsono bwerani nonsenu, bwerezaninso mawu anuwo, sindidzapezapo munthu wanzeru pakati panupo.
Tolikéž i vy všickni obraťte se, a poďte, prosím; neboť nenacházím mezi vámi moudrého.
11 Masiku anga atha, zimene ndinakonza zalephereka, pamodzinso ndi zokhumba za mtima wanga.
Dnové moji pomíjejí, myšlení má mizejí, přemyšlování, pravím, srdce mého.
12 Anthu awa amasandutsa usiku kukhala usana, nthawi ya usiku iwo amati ‘kwatsala pangʼono kucha.’
Noc mi obracejí v den, a světla denního ukracují pro přítomnost temností.
13 Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
Abych pak čeho i očekával, hrob bude dům můj, ve tmě usteli ložce své. (Sheol h7585)
14 ngati ndinena kwa dzenje la manda ‘ndinu abambo anga,’ ndiponso kwa mphutsi kuti, ‘ndinu amayi anga’ kapena ‘mlongo wanga,’
Jámu nazovu otcem svým, matkou pak a sestrou svou červy.
15 tsono chiyembekezo changa chili kuti? Ndani angaone populumukira panga?
Kdež jest tedy očekávání mé? A kdo to, čím bych se troštoval, spatří?
16 Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)
Do skrýší hrobu sstoupí, poněvadž jest všechněm v prachu země odpočívati. (Sheol h7585)

< Yobu 17 >