< Yobu 17 >

1 “Mtima wanga wasweka, masiku anga atha, manda akundidikira.
我的心灵消耗,我的日子灭尽; 坟墓为我预备好了。
2 Ndithudi, anthu ondiseka andizungulira; maso anga akupenyetsetsa mdani wanga.
真有戏笑我的在我这里, 我眼常见他们惹动我。
3 “Inu Mulungu, patseni chikole chimene mukufuna. Ndani wina amene adzandiperekera ine chikole?
愿主拿凭据给我,自己为我作保。 在你以外谁肯与我击掌呢?
4 Inu mwatseka maganizo awo kuti asamvetse zinthu; choncho simudzawalola kuti apambane.
因你使他们心不明理, 所以你必不高举他们。
5 Ngati munthu apereka mnzake chifukwa cha chuma, ana ake sadzaona mwayi.
控告他的朋友、以朋友为可抢夺的, 连他儿女的眼睛也要失明。
6 “Mulungu wandisandutsa chisudzo chochiseka aliyense, munthu amene anthu amalavulira malovu nkhope yake.
神使我作了民中的笑谈; 他们也吐唾沫在我脸上。
7 Mʼmaso mwanga mwada ndi chisoni; ndawonda ndi mutu womwe.
我的眼睛因忧愁昏花; 我的百体好像影儿。
8 Anthu olungama akudabwa nazo zimenezi; anthu osachimwa akupsera mtima anthu osapembedza Mulungu.
正直人因此必惊奇; 无辜的人要兴起攻击不敬虔之辈。
9 Komabe anthu olungama adzasunga njira zawo, ndipo anthu a makhalidwe abwino mphamvu zawo zidzanka zikuchuluka.
然而,义人要持守所行的道; 手洁的人要力上加力。
10 “Tsono bwerani nonsenu, bwerezaninso mawu anuwo, sindidzapezapo munthu wanzeru pakati panupo.
至于你们众人,可以再来辩论吧! 你们中间,我找不着一个智慧人。
11 Masiku anga atha, zimene ndinakonza zalephereka, pamodzinso ndi zokhumba za mtima wanga.
我的日子已经过了; 我的谋算、我心所想望的已经断绝。
12 Anthu awa amasandutsa usiku kukhala usana, nthawi ya usiku iwo amati ‘kwatsala pangʼono kucha.’
他们以黑夜为白昼, 说:亮光近乎黑暗。
13 Ngati nyumba imene ndikuyiyembekezera ndi manda, ngati ndiyala bedi langa mu mdima, (Sheol h7585)
我若盼望阴间为我的房屋, 若下榻在黑暗中, (Sheol h7585)
14 ngati ndinena kwa dzenje la manda ‘ndinu abambo anga,’ ndiponso kwa mphutsi kuti, ‘ndinu amayi anga’ kapena ‘mlongo wanga,’
若对朽坏说:你是我的父; 对虫说:你是我的母亲姊妹;
15 tsono chiyembekezo changa chili kuti? Ndani angaone populumukira panga?
这样,我的指望在哪里呢? 我所指望的谁能看见呢?
16 Ndithu sindidzakhalanso ndi chiyembekezo chilichonse, polowa mʼmanda, pamene ndidzatsikira ku fumbi.” (Sheol h7585)
等到安息在尘土中, 这指望必下到阴间的门闩那里了。 (Sheol h7585)

< Yobu 17 >