< Yeremiya 51 >

1 Yehova akuti, “Taonani, ndidzadzutsa mphepo yowononga kuti iwononge Babuloni pamodzi ndi anthu a ku Lebi Kamai.
Hiche hi Pakaiyin aseiye: “Keiman Babylon mite douna mi sumangpa katil doh ding ahi.”
2 Ndidzatuma alendo ku Babuloni kudzamupeta ndi kuwononga dziko lake kotheratu. Iwo adzalimbana naye ku mbali zonse pa tsiku la masautso ake.
Gamchom mite hunguva huisin changpol alhoh manjel bang a, gimna nikhoa amanu doudia jet le veiya kona ahindel khum diu ahi.
3 Okoka uta musawalekerere kapena wonyadira chovala chawo chankhondo. Musawasiye anyamata ake kuti akhale ndi moyo; koma muwononge ankhondo ake kotheratu.
Galvon kivon manlouvin lhauvin, ahilou le thalpi kap thempa jong chun athalpi kamda henlang; galsat mi phalai ho hing hoi dauvin! Sepai jouse sugam hel’ un
4 Adzavulazidwa ndi kufera mʼdziko la Babuloni lomwelo ndi mʼmisewu yawo yomwe.
Babylon mite gamsung le lamlen ho-a akithat ho lhuchap ding ahiuve.
5 Pakuti Yuda ndi Israeli sanasiyidwe ngati amasiye ndi Mulungu wawo, Yehova Wamphamvuzonse, koma ngakhale dziko la Babuloni ndi lodzaza ndi machimo pamaso pa Woyerayo wa Israeli.
Van Sepai Pakai in Israel leh Judah adalha poi. Ama chu a Pathen-u ahijing in, agamsung-u chonsetna le Israel mithengpa douna adim jeng vang uvin.
6 “Thawaniko ku Babuloni! Aliyense apulumutse moyo wake! Musawonongeke naye pamodzi chifukwa cha machimo ake. Imeneyi ndi nthawi yoti Yehova amulange; Yehova adzamulipsira.
Babylon na konin jam un! Kihinsona din lhaiyun! Amanu talen kipehnaa chun kisat lhah thasah hih-uvin! Pakai phulah phat ahin lethuhna lhingset ding ahi.
7 Babuloni anali ngati chikho cha golide mʼdzanja la Yehova; kuti aledzeretse dziko lonse lapansi. Mitundu yambiri ya anthu inamwa vinyo wake; nʼchifukwa chake tsopano inachita misala.
Babylon hi Pakai khut’a sana khon tobang chu ahin, vannoi pumpi kidon khamsah ahi, namtin vaipin Babylon lengpitwiya kham ahin, chule hichea chu ngolgam a ahitauve.
8 Babuloni wagwa mwadzidzidzi ndi kusweka. Mulireni! Mfunireni mankhwala opha ululu wake; mwina iye nʼkuchira.”
Hetman louvin Babylon alhun Amanu din kap’uvin. Amanu ding damdoi peuvin. Ijemtia adam kitthei a ahi le.
9 Ena anati, “‘Ife tinayesa kumupatsa mankhwala Babuloni, koma sanachire; tiyeni timusiye ndipo aliyense apite ku dziko la kwawo, pakuti mlandu wake wafika mpaka mlengalenga, wafika mpaka kumwamba.’
Kithopi ding kanom in, ahinlah tun huhdoh thei ahitapoi. Amanu dalhauvin, chetau hite igamcheh uva. Ajeh chu athu kitan lhah na-in van asun, anasa behseh in akitepi abeihel e.
10 “‘Yehova waonetsa poyera kuti ndife osalakwa; tiyeni tilengeze mu Ziyoni zimene Yehova Mulungu wathu wachita.’
Pakaiyin idihna aphongdoh tai. Hungun, Pakai i-Pathen’u thilbol Zion a seichoi juhite.
11 “Yehova wadzutsa mitima ya mafumu a Amedi, popeza cholinga chake ndi kuwononga Babuloni. Motero adzalipsira Ababuloni chifukwa chowononga Nyumba yake. Ndiye Yehova akuti, ‘Nolani mivi, tengani zishango.’
Thalchang ho notval un! lumho domsang un, Pakaiyin Medes lengte lung asuthoutai. Ajeh chu atup chu Babylon a suhmang ding chu ahi, ajeh chu hiche Pakai phulah, a-hou in phulahna ahi.
12 Kwezani mbendera yankhondo kuti muwononge malinga a Babuloni! Limbitsani oteteza, ikani alonda pa malo awo, konzekerani kulalira. Pakuti Yehova watsimikiza ndipo adzachitadi zomwe ananena za anthu a ku Babuloni.
Babylon kulbang vum'a gal ponlap tungdoh-un, khongah hatsah-un, khongah ho tungdoh-un, ajeh chu Babylon mite douna’a Pakaiyin asei chu agongtoh in, atong tai.
13 Inu muli ndi mitsinje yambiri ndi chuma chambiri. Koma chimaliziro chanu chafika, moyo wanu watha.
Hiche gamsung’a hin vadung tampi along in. Kiveina manlu tahtah aum e, ahivangin aphat akichaina ahunglhun tai.
14 Yehova Wamphamvuzonse analumbira pali Iye mwini kuti: Ndidzakutumizira adani ochuluka ngati dzombe, kuti adzakuthire nkhondo ndipo adzafuwula kuonetsa kuti apambana.
Pakai Sepai chu amatah akihahsel e, ama min in, “Nakhopi sung’u nagal mite hungdim din, khaokho ho tobang hela mihem kahindip teitei ding nahi, amahon nangma douna’a hung ao-doh diu ahi.”
15 “Yehova analenga dziko lapansi ndi mphamvu zake; Iye anapanga dziko lonse ndi nzeru zake ndipo anayala thambo mwaluso lake.
Pakai in leiset hi Amathahatna asem ahin, asetlouna dinga achihnaa akoi, ahetchetnaa kona jong Aman van aphajal ahitai.
16 Iye akayankhula, kumamveka mkokomo wamadzi akumwamba. Iyeyo amabweretsa mitambo kuchokera ku malekezero a dziko lapansi. Amabweretsa mphenzi pamodzi ndi mvula ndi kutulutsa mphepo yamkuntho kumalo kumene amasungira.
Ama a-aw asodoh teng, van hoa twipi tamtah ahung umjin van monga konin meilhang asemkhom e. Gojuh teng kol aphetsah-in, akholmuna kon khohui anunsah e.
17 “Anthu onse ndi opusa ndiponso opanda nzeru; mmisiri aliyense wosula golide akuchita manyazi ndi mafano ake. Mafano akewo ndi abodza; alibe moyo mʼkati mwawo.
Hiche amuteng ule mitin a ngolden jiuve chule hetthemna anei pove! Mikhut thiem takip semthu milim a kijumso ahiuve. Ajeh chu amilim semthu uchu joubulom ahin, amaho – a haitheina hu le thilboltheina aumpoi.
18 Mafanowo ndi achabechabe, zinthu zosekedwa nazo. Pamene anthuwo azidzaweruzidwa mafanowo adzawonongedwa.
Hiche milim semthu hochu mohseh, athu aki kholtoh phatteng ule mangthah cheh diu ahi.
19 Koma Yehova amene ndi Cholowa cha Yakobo sali ngati mafanowo. Iyeyu ndi Mlengi wa zinthu zonse, kuphatikizapo mtundu umene anawusankha kuti ukhale anthu ake. Dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse.
Ahinlah Israel Pathen vang chu milim semthu ahipoi! Thil ijakai Sempa le ahung konna ahin, ama amite ama goulo ahi. Van Pakai sepai janel chu Ama min ahi.
20 “Iwe Babuloni ndi ndodo yanga, chida changa chankhondo. Ndi iwe ndimaphwanya mitundu ya anthu, ndi iwe ndimawononga maufumu,
Pakaiyin aseiyin, nangma kagal heicha le chemjam nahin, “Namtin vaipi le lenggam jouse suhmangna kaman nahi.”
21 ndi iwe ndimaphwanya kavalo ndi wokwerapo, ndi iwe ndimaphwanya galeta ndi woyendetsa wake.
Chule nangma’a sakolte le achunga toupa kasuh chip ding, kangtalaiho le atolte jong mangthah ding ahi.
22 Ndi iwe ndimaphwanya mwamuna ndi mkazi, ndi iwe ndimaphwanya nkhalamba ndi wachinyamata, ndi iwe ndimaphwanya mnyamata ndi namwali.
Nangma’a pasal le numei jong kasuchip ding, tehse le chate jong kasuchip ding ahi; Chule nangma’a nungah le gollhang jong kasuchip ding ahi.
23 Ndi iwe ndimaphwanya mʼbusa ndi ziweto, ndi iwe ndimaphwanya mlimi ndi ngʼombe, ndi iwe ndimaphwanya abwanamkubwa ndi atsogoleri a ankhondo.
Nangma’a kelngoichingpa le akelngoihon jong kasuchip ding, nangma’a loubolpa le abongchal ho, chule agal lamkaiho le vaihom ho jong kasuchip ding ahi.
24 “Inu mukuona ndidzalanga Babuloni ndi onse amene amakhala mʼdziko la Babuloni chifukwa cha zolakwa zonse anachita ku Ziyoni,” akutero Yehova.
Pakaiyin aseiyin, “Keima in Jerusalem a kamite chun thilse abol chengseu Babylon mite kale thuhding ahi,” ati.
25 “Taonani, ndikukuzenga mlandu, iwe phiri lowononga, amene umawononga dziko lonse lapansi,” akutero Yehova. “Ndidzatambalitsa dzanja langa pofuna kukulanga, kukugubuduzira pansi kuchokera pa matanthwe ako, ndi kukusandutsa kukhala phiri lopserera.
Pakayin aseiyin “Ven, thahat mollentah leiset pumpi sumang! Keima nakidoupi kahi.” Nachung a kakhut kalhan doh a, munsang’a kona kasuh lhah’a, nangma ima hilou akavamsa mol kaso ding nahi.
26 Palibe ngakhale ndi mwala wako umodzi umene anthu adzawutenga kuti awugwiritse ntchito kumangira nyumba, chifukwa iwe udzakhala chipululu mpaka muyaya,” akutero Yehova.
Nangma tonsot’a dalpeia umdin nanga kona in – ning song ding le inbul song dia alah lou diu ahitan, nangma hi pampei hel’a um ding nahitai, tin Pakaiyin aseije.
27 “Kwezani mbendera ya nkhondo mʼdziko! Lizani lipenga pakati pa mitundu ya anthu! Konzekeretsani mitundu ya anthu kuti ikamuthire nkhondo; itanani maufumu awa: Ararati, Mini ndi Asikenazi kuti adzamuthire nkhondo. Ikani mtsogoleri wankhondo kuti amenyane naye; tumizani akavalo ochuluka ngati magulu a dzombe.
Namtin din ponlap khat tahdoh unlang, namtin vaipi lah’a sumkon gintoh kigotsah un kisat ding! Ararat sepaite hinpuidoh un, Minni, chule Ashkenaz gal lamkai semun lang, khao khoho bang in sakol ho hungtousah – un.
28 Konzekeretsani mitundu ya anthu. Amenewa ndiwo mafumu a Amedi, abwanamkubwa awo, atsogoleri a ankhondo, ndiponso ankhondo a mayiko amene amawalamulira, kuti idzathire nkhondo Babuloni.
Amanu douding namtin vaipi hinpui un, lamkai ding Medes lengte chule a vaihom ho jouse toh,
29 Dziko likunjenjemera ndi kunthunthumira, chifukwa zidzachitikadi zimene Yehova wakonzera Babuloni; kusakaza dziko la Babuloni kuti musapezeke wokhalamo.
agam chu akithing thing jeng in anasalheh jeng e. Pakaiyin Babylon dounaa thil agon jouse kikhel lou ding ahi. Babylon gamsung ahomkeova umsah ding aching beihel’a koi ding ahi.
30 Ankhondo a ku Babuloni aleka kuchita nkhondo; iwo angokhala mʼmalinga awo. Mphamvu zawo zatheratu; ndipo akhala ngati akazi. Malo ake wokhala atenthedwa; mipiringidzo ya zipata zake yathyoka.
Amanu galhat ho, galsat ahaiyun. Akul sunga aumden tauve ahatnau adailhan numei toh abang tauve. Achen nau ahallha uvin chule khopi kelkot jouse atumkeh – un ahi.
31 Othamanga akungopezanapezana, amithenga akungotsatanatsatana kudzawuza mfumu ya ku Babuloni kuti alande mzinda wake wonse.
Thusep khat chu achomto kisuto ding, thangkou khat chu achom khattoh kisuto – a, akhopi chu among khatna konin akilatai ti hil dingin.
32 Madooko onse alandidwa, malo onse obisalamo alonda atenthedwa ndi moto, ndipo ankhondo onse asokonezeka.”
Jam na diu lampi ho akikhah in pumpeng aneihou meiya akihal lhan, sepaite akicha gam tauve.
33 Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti, “Babuloni wokongola uja wakhala ngati malo opunthirapo tirigu pa nthawi yake yopuntha tirigu; A ku Yerusalemu akuti, Posachedwapa nthawi yake yomukolola ifika.”
Ijeh-inem itileh thaneipen Pakai, Israel Pathen in hitin aseiye, “Babylon chanu chu kengto chotpha akinei tengleh changpol tobang ahin, Ahivang in phat chomkhat nung leh achang –at phat hung lhung ding ahitai,’’ ati.
34 A ku Yerusalemu akuti, “Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni watiwononga, watiphwanya, ndi kutitaya ngati mbiya yopanda kanthu. Watimeza ngati ngʼona, wakhuta ndi zakudya zathu zokoma, kenaka nʼkutilavula.”
“Babylon lengpa Nebuchadnezzar in keima eival lhum in, aman eisuchip in; kathahat jouse asugoitan ahi. Hing ne bangin keima eivel lhum tai, ka haosatna oiva set in eine peh tan. Aman kagam sunga kon in eipei doh tai.
35 Anthu a ku Ziyoni anene kuti, “Zankhanza zimene anatichitira ife ziwabwerere Ababuloni.” Anthu okhala mu Yerusalemu anene kuti, “Magazi athu amene anakhetsedwa akhale pa amene akukhala ku Babuloni.”
Keima chungle kaphunggol mite chunga pum hat jinga thil kibol chu Babylon khopi chunga chujeng hen,’’ ati. Zion cheng mite chun seiju hen, “Keima thisan man chu Babylon mite gam'a chengte chung a chu jeng hen,’’ tin Jerusalem in jong seihen.
36 Nʼchifukwa chake Yehova akuti, “Taona, ndidzakumenyera nkhondo ndi kukulipsirira; ndidzawumitsa nyanja yake ndipo akasupe ake adzaphwa.
Jerusalem mite koma Pakaiyin aseiyin, “Nakhan khou gel’ing ting, namelma teuvin nabolnau chu kale ditsah ding ahi. Babylon twikul kansah ingting chule avadung jouse kangsoh ding ahi.”
37 Motero Babuloni adzasanduka mulu wa nyumba zogumuka, malo okhala nkhandwe, malo ochititsa mantha ndi onyozedwa, malo wopanda aliyense wokhalamo.
Chuteng Babylon chu ingem jeng kisechop ding, gamsa chenna soh ding; chule koima chenna hitalouva, gamsa jengseh chenna hiding ahi.
38 Anthu ake onse adzabangula ngati mkango, adzadzuma ngati ana amkango.
Amaho abonchauvin keipi bahkai hon banga kitum tum diu, sakei noute banga ngih ngih jeng diu ahi.
39 Ngati achita dyera ndiye ndidzawakonzera madyerero ndi kuwaledzeretsa, kotero kuti adzasangalala, kenaka nʼkugona tulo mpaka muyaya ndipo sadzadzukanso,” akutero Yehova.
Amaho nei-yin ahul sat pet tah’a keiman golvah kagonpeh ding, ju kadon sah a; aitih chan geiya ihmu mu jeng diu, kithoukit louva thidiu ahi, tin Pakainyin aseiye.
40 “Ine ndidzawatenga kuti akaphedwe ngati ana ankhosa onenepa, ngati nkhosa zazimuna ndi mbuzi.
Keiman amaho thuhi kelngoi nou akitha na ding le kel ngoichal ho kelcha ho banga kilhainaa ki that bang hi ding ahiuve.
41 “Ndithu Babuloni walandidwa, mzinda umene dziko lonse lapansi limanyadira wagwidwa! Taonani, mmene Babuloni wasandukira chinthu chochititsa mantha pakati pa mitundu ya anthu!
Itidan a Babylon chu lhujeng hi tam vannoi pumpi in apachat khopi chu tua hi, amanu namtin a dingin kichat umta thil ahidohtai.
42 Nyanja yakwera ndi kumiza Babuloni; mafunde ake okokoma aphimba Babuloni.
Babylon chu twikhanglen in achup tan, amanu achunga twipi aki deldel e.
43 Mizinda yake yasanduka bwinja, dziko lowuma ndi lachipululu, dziko losakhalamo wina aliyense, dziko losayendamo munthu aliyense.
Akhopi hochu akam hel in, gamgo, gamthip, mikhat cha chennalou gam, mihem chapa khatchan ajotpa louhel asoh tai.
44 Ndidzalanga Beli mulungu wa Ababuloni, ndidzamusanzitsa zimene anameza. Mitundu ya anthu sidzapitanso kwa iye. Malinga a Babuloni agwa.
Keiman Babylon Pathen bel chu talent kapeh ding, aval lhumsa chu akam sunga kona kalah doh peh ding ahi. Namtin vaipi ho Amahou dinga aheng a hung kitol tol lou hel ding ahi. Ajeh chu Babylon khopi pal chu chim ahitai.
45 “Tulukani mʼBabuloni anthu anga! Pulumutsani miyoyo yanu! Thawani mkwiyo woopsa wa Yehova.
Hung potdoh'un, kamite, Babylon khopi akon in jam doh loiyun nangma kihuhhing cheh un! Pakai lunghan na kon in jam un.
46 Musataye mtima kapena kuchita mantha pamene mphekesera zikumveka mʼdziko mwanu. Chaka ndi chaka pamabuka mphekesera za ziwawa mʼdziko lapansi, ndiponso yakuti mfumu yakuti ikuthira nkhondo mfumu ina.
Nalungthim lhahsam sah hih-uvin, Gamsunga thu kithang jeh hin kicha hih uvin; kum khat sunga thu thang khat hung lhung ji ahin, khonung teng akum kit’a chu thu thang khatma hung lhung jia ahiye; Gamsunga pumhat jeng aumtan, Vaihom khat chu vaihom khat dou umcheh ahitai.
47 Pakuti taonani, nthawi ikubwera ndithu pamene ndidzalanga mafano a ku Babuloni; dziko lake lonse lidzachita manyazi ndi ophedwa ake onse adzakhala ngundangunda pakati pake.
Hijeh chun vetan, keiman Babylon khopia pathen lim sem thuho talent kapeh na ding nikho ho chu ahung lhunge. Agam sung pumpi hi kijum so ding, alam len dunga amite ki that jouse ki jam dan ding ahiuve.
48 Pamenepo kumwamba ndi dziko lapansi ndi zonse zili mʼmenemo zidzayimba mokondwa chifukwa cha kugwa kwa Babuloni. Anthu owononga ochokera kumpoto adzamuthira nkhondo,” akutero Yehova.
Chujou teng le van le leiset chule asung a umjousen, Babylon khopi chunga kipa la asah diu ahi. Ijeh-inam itileh amaho dou dinga Misumang ho chu Sah lam gamkaiya kona hung kondoh ding ahitauve, tin Pakaiyin seiye.
49 “Babuloni anapha anthu ambiri pa dziko lapansi. Tsono, nawo anthu a ku Babuloni ayenera kuphedwa chifukwa anapha anthu a ku Yerusalemu.
Babylon in Israel mite athagam banga, chuleh leiset pumpi kitha gam jeh a amanu lhu a ahitai.
50 Inu amene munapulumuka ku nkhondo ya Babuloni, chokani pano ndipo musazengereze! Kumbukirani Yehova ngakhale muli ku mayiko akutali, ganizirani za Yerusalemu.”
Pohdoh un, nangho chemjam’a kona houidoh ho! ding den hih un chule ve hih un – jam thei ahi pat in! Pakai chu geldoh jing un kholgam lhatah a naum vang un, chule na gam lang u Jerusalem gel doh jing un.
51 Inu mukuti, “Tikuchita manyazi, chifukwa tanyozedwa ndipo nkhope zathu zili ndi manyazi, chifukwa anthu achilendo alowa malo opatulika a Nyumba ya Yehova.”
Jumsona kachang un ahi, ijeh-inem itileh houset kachan u-ahitai. Kamai jengu jong jabolna akilah tapoi, ajeh chu Pakai munthenga gamdang miho ahunglut tauve, tia nasei diu ahi.
52 Nʼchifukwa chake Yehova akuti, “Masiku akubwera pamene ndidzalanga mafano ake, ndipo mʼdziko lake lonse anthu ovulala adzabuwula.
Hijeh chun ven, hiche nikho ho chu ahung lhung tai, tin Pakaiyin aseije; milim semthu ho chunga thu katan ding, agam pumpi lung leng ding chule maha pua peng ding ahi.
53 Ngakhale Babuloni atadzikweza mpaka mlengalenga ndi kulimbitsa nsanja zake, ndidzatuma anthu owononga kudzamenyana naye,” akutero Yehova.
Babylon chu vanlam sanga kaltou ding hihen, akulpi jeng jong sangtah'a aget ding hijongleh, kamite ama sumang dinga achunga hung lhung ding ahi.
54 “Imvani mfuwu wolira kuchokera ku Babuloni. Imvani phokoso lachiwonongeko chachikulu kuchokera mʼdziko la Babuloni.
Babylon awgin kithong leh Chaldea mite gam'a manthahna awgin akithong e.
55 Pakuti Yehova akuwononga Babuloni, ndipo akuthetsa phokoso lake lalikulu. Mfuwu wa adani ukumveka ngati mkokomo wa madzi ambiri. Phokoso lawo likunka likwererakwerera.
Ijeh-inem itileh Pakaiyin Babylon hi akeosah a aumsah ahitan, husa gin beihel a alhaa; acheh chaunau gin jong twi kinong tobang'in aging in, a awgin husan ujong agimnei cheh cheh in ahi.
56 Pakuti wowononga wafika kudzamenyana ndi Babuloni, ankhondo ake agwidwa, ndipo mauta awo athyoka. Paja Yehova ndi Mulungu wobwezera chilango; adzabwezera kwathunthu.
Misumangpa Babylon chunga achutan, agal hang sepai ho jong akhomtup soh tai. Athalpi jouse jong abang abaijin aum gam in, ajeh chu Pakai chu milethuh Pakai ahin, thon louhel’a lethuhna apehji ahi.
57 Ndidzaledzeretsa akuluakulu ake pamodzi ndi anzeru ake, abwanamkubwa ake, atsogoleri a ankhondo pamodzinso ndi ankhondo; adzagona kwamuyaya osadzukanso,” akutero Mfumu, amene dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse.
Aleng chapate ahin, ami ching ho jouse jaona ju ka-khamsah soh hel ding, chule agam vaipo ahin asepai lah’a thunei vaihom ho, agal hang ho jouse jong khamsoh hel diu ahi. Thabeiya imu lhu diu, kithou talou diu ahitai, tin thaneipen Pakaiyin aseiye.
58 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Malinga aakulu a Babuloni adzasalazidwa ndipo zipata zake zazitali zidzatenthedwa; mitundu ya anthu inangogwira ntchito pachabe. Anthu anatopa ndi kumanga zimene tsopano zikupsa ndi moto.”
Hatchungnung Pakaiyin hiti hin aseiye, Babylon in pal nasatah akai chu tollham a
59 Zedekiya mfumu ya Yuda inali ndi phungu wake wamkulu amene dzina lake linali Seraya mwana wa Neriya chidzukulu cha Maseya. Mʼchaka chachinayi cha ulamuliro wake, Zedekiya anapita ndi Seraya ku Babuloni. Tsono mneneri Yeremiya anamupatsirako uthenga Serayayo.
Judah lengpa Zedekiah leng ahikal kumli alhing in, Jeremiah themgaovin Babylon mun’a ana kilhonp’n Mahseiah chapa, Neriah chapa Seraiah thu anapen hiti hin anaseiyin ahi. Saraiah kitipa hi thil ijakai chingtup dinga ngensena ana chang ahi.
60 Yeremiya anali atalemba mʼbuku za masautso onse amene adzafike pa Babuloni ndi zina zonse zokhudza Babuloni.
Hiti chun Jeremiah chun Babylon mun’a lhung ding thil abonchan anajih lut’in, Babylon thudol in thu hijatpi chu ana kijihlut tan ahi.
61 Yeremiya anawuza Seraya kuti, “Ukakafika ku Babuloni, ukaonetsetse kuti wawawerengera anthu onse mawu onsewa.
Chuin Jeremiah in Saraiah henga hiti hin aseiyin, “Babylon mun nalhung teng thu hichengse hi nasim doh tei ding ahi, phatah in vephan,” atin,
62 Ndipo ukanene kuti, ‘Inu Yehova, mwanena kuti mudzawononga malo ano, kotero kuti simudzatsala munthu kapena nyama mʼdziko muno; lidzakhala chipululu mpaka muyaya.’
hiti hin aseiyin, ‘Pakai nangman hiche mun chungchang thudol’a hin seiyin, hiche mun hi kisu mang ding, asung hi chenna hita lou ding; mihem ahin chule gamsa jeng jong aitih channa chenna hilouding ahom keu jeng hiding ahi.’
63 Ukakatha kuwerenga bukuli, ukalimangirire ku mwala ndipo ukaliponye pakati pa mtsinje wa Yufurate.
Hiche lekha hi nasim chai teng songkhat toh nakan beh ding, hichu vadung lailunga nase lut ding ahi.
64 Ndipo ukanene kuti, ‘Umu ndi mmene adzamirire Babuloni ndipo sadzadzukanso chifukwa cha masautso amene adzamugwere.’” Mawu a Yeremiya athera pamenepa.
Chuteng keiman hiche mun’a kahin lhut ding thilse jal’a hi Babylon jong kidodoh kit talou ding, hitia chu mangthah hel ding ahitai, tin seiyin,” ati. Hichengse hi Jeremiah thusei dohho ahi.

< Yeremiya 51 >