< Yeremiya 46 >

1 Yehova anamupatsa Yeremiya uthenga wonena za anthu a mitundu ina.
KA olelo a Iehova i hiki mai io Ieremia la i ke kaula, e ku e i ko na aina;
2 Kunena za Igupto: Yehova ananena za gulu lankhondo la Farao Neko mfumu ya ku Igupto limene Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni analigonjetsa ku Karikemesi ku mtsinje wa Yufurate mʼchaka cha chinayi cha Yehoyakimu mwana wa Yosiya mfumu ya Yuda,
E ku e ia Aigupita, i ka poe kaua hoi o Parao-neko, ke alii o Aigupita, aia ma ka muliwai o Euperate, ma Karekemisa, ka poe a Nebukaneza i luku ai i ka makahiki aha o Iehoiakima, ke keiki a Iosia, ke alii o ka Iuda.
3 anati, “Konzani zishango zanu ndi malihawo, ndipo yambanipo kupita ku nkhondo!
E hoomakaukau oukou i ka paku a me ka palekaua, a e hookokoke i ke kaua.
4 Mangani akavalo, ndipo kwerani inu okwerapo! Khalani pa mzere mutavala zipewa! Nolani mikondo yanu, valani malaya anu ankhondo!
E kahiko i na lio, a e ee ae, e na hololio, a e ku mai me na mahiole; e hookala i na ihe, e komo na paleumaumaunahi.
5 Yeremiya anati: Kodi ndikuona chiyani? Achita mantha akubwerera, ankhondo awo agonjetsedwa. Akuthawa mofulumirapo osayangʼananso mʼmbuyo, ndipo agwidwa ndi mantha ponseponse,” akutero Yehova.
No ko aha la wau i ike aku ai ia lakou ua makau a hoi hope? ua hahauia na mea ikaika o lakou, a ua hee loa, aole i nana ihope; puni lakou i ka makau, wahi a Iehova.
6 Waliwiro sangathe kuthawa ngakhale wankhondo wamphamvu sangathe kupulumuka. Akunka napunthwa ndi kugwa kumpoto kwa mtsinje wa Yufurate.
Aole e hiki i ka mea mama e holo, aole hoi e pakele ka poe ikaika; e okupe no lakou a hina ma ke kukulu akau, ma ka muliwai o Euperate.
7 “Kodi ndani amene akukwera ngati Nailo, ngati mtsinje wa madzi amkokomo?
Owai keia mea e hele mai nei, me he wai pii la, a kupikipikio na wai, e like me ka wai kahe la?
8 Igupto akusefukira ngati Nailo, ngati mitsinje ya madzi amkokomo. Iye akunena kuti, ‘Ndidzadzuka ndi kuphimba dziko lapansi; ndidzawononga mizinda ndi anthu ake.’
Ke pii nei o Aigupita, me he wai pii la, a ua kupikipikio kona mau wai me he wai kahe la; a olelo no hoi oia, E pii aku no wau, e uhi no wau i ka honua; e luku no wau i ke kulanakauhale, a me ka poe e noho ana ilaila.
9 Tiyeni, inu akavalo! Thamangani inu magaleta! Tulukani, inu ankhondo, ankhondo a ku Kusi ndi Puti amene mumanyamula zishango, ankhondo a ku Ludi amene mumaponya uta.
E pii mai, e na lio, e holo ikaika hoi, e na kaakaua; e hele mai na kanaka ikaika, o ko Aitiopa, a me ko Libua, ka poe lawelawe i ka palekaua, a me ka Ludia, o ka poe i lawelawe, a lena ke kakaka.
10 Koma tsikulo ndi la Ambuye Yehova Wamphamvuzonse; tsiku lolipsira, lolipsira adani ake. Lupanga lake lidzawononga ndi kukhuta magazi, lidzaledzera ndi magazi. Pakuti Yehova, Yehova Wamphamvuzonse, adzapereka adani ake ngati nsembe mʼdziko la kumpoto mʼmbali mwa mtsinje wa Yufurate.
Oia no ka la o ka Haku, o Iehova o na kaua, ka la o ka hoopai ana, e hoopai ai i kona poe enemi nona; e ai no ka pahikaua, a e maona no, a e ona no hoi i ko lakou koko; no ka mea, he mohai ko ka Haku, ko Iehova o na kaua ma ka aina o ke kukuluakau, ma ka muliwai o Euperate.
11 “Pita ku Giliyadi ukatenge mankhwala iwe namwali Igupto. Wayesayesa mankhwala ambiri koma osachira; palibe mankhwala okuchiritsa.
E pii aku oe i Gileada, a e lawe mai oe i nini, e ka wahine puupaa, ke kaikamahine o Aigupita; he make hewa nae kou lawe ana i ka laaulapaau a nui, no ka mea, aole loaa ia oe ke ola.
12 Anthu a mitundu ina amva za manyazi ako; kulira kwako kwadzaza dziko lapansi. Ankhondo akunka nagwetsanagwetsana, onse awiri agwa pansi limodzi.”
Ua lohe ko na aina i kou hilahila, a ua hoopiha kou uwe ana i ka aina; no ka mea, ua okupe kekahi kanaka ikaika i kekahi kanaka ikaika, a ua hina pu laua.
13 Uthenga umene Yehova anapatsa mneneri Yeremiya wonena za kubwera kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni kudzathira nkhondo Igupto ndi uwu:
Ka olelo a Iehova i olelo mai ai ia Ieremia, i ke kaula, no ka hele ana mai o Nebukaneza, ke alii o Babulona, e anai i ka aina o Aigupita.
14 “Mulengeze ku Igupto. Mulengeze ku Migidoli. Mulengezenso ku Mefisi ndi ku Tapanesi. Muwawuze anthu akumeneko kuti, ‘Imani pamalo panu ndi kukhala okonzeka kudziteteza, chifukwa lupanga lidzawononga zonse zimene muli nazo.’
E hai aku oukou ma Aigupita, e kala aku hoi ma Migedola, e kala aku ma Nopa, a ma Tapehanesa; e i aku, E kupaa, a e hoomakaukau ia oe; no ka mea, e ai no ka pahikaua a puni oe.
15 Chifukwa chiyani mulungu wanu wamphamvu uja Apisi wathawa? Iye sakanatha kulimba chifukwa Yehova anamugwetsa.
No ke aha la i hoohinaia'i kou poe koa, aole lakou i kupaa, no ka mea, hooauhee o Iehova ia lakou.
16 Ankhondo anu apunthwa ndi kugwa. Aliyense akuwuza mnzake kuti, ‘Tiyeni tibwerere kwathu, ku dziko kumene tinabadwira, tithawe lupanga la adani athu.’
Nana no i hoohina i na mea he nui loa; oia, hina no kekahi maluna o kekahi; olelo no nae lakou, E ku kakou iluna, e hoi hou kakou i ko kakou kanaka iho, a i ko kakou aina i hanau ai, mai ke alo aku o ka pahikaua luku.
17 Kumeneku iwo adzafuwula kuti, ‘Farao, mfumu ya ku Igupto mupatseni dzina lakuti, Waphokoso, Wotaya mwayi wake.’
Uwe no lakou malaila, he walaau wale o Parao, ke alii o Aigupita, ua hala kona manawa pono.
18 “Pali Ine wamoyo,” ikutero Mfumu, imene dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse, “wina adzabwera amene ali ngati Tabori phiri lopambana mapiri ena, ngati phiri la Karimeli loti njoo mʼmbali mwa nyanja.
Me au e ola nei, wahi a ke Alii, nona ka inoa, o Iehova o na kaua, Oiaio, me Tabora iwaena o na mauna, a me Karemela ma kahakai, e hele mai no ia.
19 Konzani katundu wanu wopita naye ku ukapolo inu anthu a ku Igupto, pakuti Mefisi adzasanduka chipululu ndipo adzakhala bwinja mopanda wokhalamo.
E ke kaikamahine e noho la ma Aigupita, e hoomakaukau oe i kahiko no kou hele pio ana; no ka mea, e olohelohe auanei, a e mehameha hoi o Nopa, aohe mea noho malaila.
20 “Igupto ali ngati mwana wangʼombe wokongola, koma chimphanga chikubwera kuchokera kumpoto kudzalimbana naye.
He keiki bipi wahine maikai o Aigupita, ke hele mai nei kona make, mai ka akau mai ka hele ana.
21 Ngakhale ankhondo aganyu amene ali naye ali ngati ana angʼombe onenepa. Nawonso abwerera mʼmbuyo, nathawa pamodzi. Palibe amene wachirimika. Ndithu, tsiku la tsoka lawafikira; ndiyo nthawi yowalanga.
O kona poe paaua iwaenakonu ona, ua like me na keikibipi kupaluia; no ka mea, ua hee lakou, ua auhee pu aku no; aole lakou i ku paa, no ka mea, ua hiki mai ka la o ko lakou poino maluna o lakou, o ka manawa hoi o ko lakou hoopaiia.
22 Aigupto akuthawa ndi liwu lawo lili ngati la njoka yothawa pamene adani abwera ndi zida zawo, abwera ndi nkhwangwa ngati anthu odula mitengo.
E loheia ka leo ona me ko ka nahesa la; no ka mea, e hele mai no lakou me ka poe kaua, a e hele ku e ia ia me na lipi, e like me ka poe kualaau.
23 Iwo adzadula nkhalango ya Igupto,” akutero Yehova, “ngakhale kuti ndi yowirira. Anthuwo ndi ochuluka kupambana dzombe, moti sangatheke kuwerengeka.
E kua lakou i kona ululaau ilalo, wahi a Iehova, ina no e hiki ole ke nana ia ia a pau; no ka mea, ua oi aku ko lakou lehulehu i ko na uhini, hiki ole ke heluia aku.
24 Anthu a ku Igupto achita manyazi atengedwa ukapolo ndi anthu a kumpoto.”
E hoohilahilaia ke kaikamahine o Aigupita; e haawiia oia iloko o ka lima o na kanaka o ke kukuluakau.
25 Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, akunena kuti, “Ndili pafupi kulanga Amoni mulungu wa Tebesi. Ndidzalanganso Farao ndi Igupto pamodzi ndi milungu yake yonse, mafumu ake ndi onse amene amamukhulupirira.
Ke i mai nei o Iehova o na kaua, ke Akua o ka Iseraela, penei; Aia hoi, e hoopai no wau ia Amona o No, a me Parao, a me Aigupita, a me ko lakou poe Akua, a me ko lakou poe alii, ia Parao no, a me ka poe a pau e hilinai ia ia.
26 Ndidzawapereka kwa amene akufuna kuwapha, ndiye kuti kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni ndi atsogoleri ake ankhondo. Komabe, mʼtsogolomo Igupto adzakhalanso ndi anthu monga kale,” akutero Yehova.
A e haawi no wau ia lakou iloko o ka lima o ka poe imi i ko lakou ola, a iloko o ka lima o Nebukaneza, ke alii o Babulona, a iloko o ka lima o kana poe kauwa. A mahope iho e nohoia no ia e like me ka wa kahiko, wahi a Iehova.
27 “Iwe mtumiki wanga Yakobo, usachite mantha; usataye mtima, iwe Israeli. Ndithu Ine ndidzakupulumutsa kuchokera ku mayiko akutali, ndidzapulumutsanso zidzukulu zako kuchokera ku mayiko kumene anapita nazo ku ukapolo. Yakobo adzabwerera ndipo adzakhala motakasuka ndi pa mtendere, ndipo palibenso wina amene adzamuopsa.
Mai makau oe. e ka'u kauwa, e Iakoba, mai weliweli hoi, e ka Iseraela; no ka mea, aia hoi, e hoola no wau ia oe, mai kahi loihi mai, a me kau poe mamo hoi, mai ka aina mai o ko lakou noho pio ana; a e hoi no ka Iakoba, a e noho hoomaha, a e oluolu no, aohe mea nana e hoomakau ia ia.
28 Iwe mtumiki wanga Yakobo, usachite mantha, pakuti Ine ndili nawe,” akutero Yehova. “Ndidzawonongeratu mitundu yonse ya anthu a ku mayiko kumene ndakupirikitsira, Koma iwe sindidzakuwononga kotheratu. Ndidzakulanga iwe ndithu koma moyenerera; sindidzakulekerera osakulanga.”
Mai makau oe, e Iakoba, e ka'u kauwa, wahi a Iehova; no ka mea, owau pu me oe; no ka mea, e hoopau ana au i ko na aina a pau, kahi a'u i kipaku ai ia oe: aka, aole au e hoopau ia oe, e hoouku pono aku no nae wau ia oe, aole au e hooki loa aku ia oe.

< Yeremiya 46 >