< Yeremiya 45 >
1 Uwu ndi uthenga umene mneneri Yeremiya anawuza Baruki mwana wa Neriya mʼchaka cha chinayi cha Yehoyakimu mwana wa mwana ya Yosiya kuti alembe mʼbuku.
Rijeè koju reèe Jeremija prorok Varuhu sinu Nirijinu, kad pisaše ove rijeèi u knjigu iz usta Jeremijinijeh, èetvrte godine Joakima sina Josijina, govoreæi:
2 “Yehova Mulungu wa Israeli, akunena kwa iwe Baruki kuti:
Ovako veli Gospod Bog Izrailjev za tebe, Varuše:
3 Iwe unati, ‘Kalanga ine! Yehova wawonjezera chisoni pa mavuto anga. Ine ndatopa ndi kubuwula ndipo sindikupeza mpumulo.’”
Rekao si: teško meni! jer Gospod dodade mi žalost na tugu; iznemogoh uzdišuæi, i mira ne nalazim.
4 Koma Yehova akukuwuza kuti, “Ndidzagwetsa chimene ndinamanga ndipo ndidzazula chimene ndinadzala. Ndidzachita zimenezi mʼdziko lonse.
Reci mu ovo: ovako veli Gospod: evo, što sam sagradio ja razgraðujem, i što sam posadio iskorenjavam po svoj toj zemlji.
5 Kodi tsono ukudzifunira wekha zinthu zazikulu? Usadzifunire. Pakuti ndidzagwetsa mavuto pa anthu onse, koma ndidzasunga moyo wako kulikonse kumene ungadzapite.”
A ti li æeš tražiti sebi velike stvari? Ne traži; jer evo, ja æu pustiti zlo na svako tijelo, govori Gospod; ali æu tebi dati dušu tvoju mjesto plijena u svijem mjestima, kuda otideš.