< Yeremiya 42 >

1 Atsogoleri onse a ankhondo pamodzi ndi Yohanani mwana wa Kareya ndi Azariya mwana wa Hosayia, ndiponso anthu onse, ana ndi akuluakulu omwe, anapita
Amalalu, Youha: ina: ne (Galia egefe), A:salia (Housia: ia egefe), dadi gagui ouligisu dunu amola eno dunu bagade amola fonobahadi, da nama misini,
2 kwa mneneri Yeremiya ndipo anamuwuza kuti, “Chonde imvani dandawulo lathu ndipo mutipempherere anthu otsalafe kwa Yehova Mulungu wanu. Pakuti monga tsopano mukuona, ngakhale kuti kale tinalipo ambiri, koma tsopano ochepa okha ndiye amene atsala.
amane sia: i, “Ninia adole ba: su nabima! Nini fidima: ne, Hina Godema sia: ne gadoma! Nini huluane da mae bogole esaloma: ne, amo fidima: ne Ema sia: ne gadoma! Musa: ninia da bagohame esalu. Be wali di da ba: loba, ninia da bagahame esala.
3 Mupemphere kuti Yehova Mulungu wanu atiwuze kumene tiyenera kupita ndi chimene tiyenera kuchita.”
Hina Gode da ninima logo olelema: ne amola ninia hamomu olelema: ne, Ema sia: ne gadoma.”
4 Mneneri Yeremiya anawayankha kuti, “Ndamva zimene mwanenazi. Ndithu ndidzapemphera kwa Yehova Mulungu wanu monga momwe mwandipemphera. Ndidzakuwuzani chilichonse chimene Yehova anene ndipo sindidzakubisirani kanthu kalikonse.”
Na da ilima bu adole i, “Defea! Dilia adole ba: i defele, na da ninia Hina Godema sia: ne gadomu. Ea sia: i liligi huluane, na da mae wamolegele, huluane dilima olelemu.”
5 Ndipo iwo anawuza Yeremiya kuti, “Yehova akhale mboni yoona ndi yokhulupirika yodzatitsutsa ife ngati sitichita mogwirizana ndi chilichonse chimene Yehova Mulungu adzakutumani kuti mutiwuze.
Amalalu, ilia da nama amane sia: i, “Ninia da Hina Gode ba: ma: ne, dafawanedafa ilegesa. Ninia da hamoma: ne sia: i huluane amo Hina Gode da dima sia: mu liligi, amo huluanedafa ilima fa: no bobogemu.
6 Kaya ndi zotikomera kapena zosatikomera, ife tidzamvera Yehova Mulungu wathu, amene takutumaniko. Tidzamvera Yehova Mulungu wathu kuti zinthu zidzatiyendere bwino.”
Ninia da dia nini fidima: ne Hina Godema sia: ne gadoma: ne adole ba: sa. Amo sia: ninia hahawane ba: sea o da: i dioiwane ba: sea, ninia da mae dawa: le, Hina Gode Ea sia: nabawane hamomu. Amasea, ninia da hahawane ba: mu.”
7 Patapita masiku khumi, Yehova anayankhula ndi Yeremiya.
Eso nabuane aligili, Hina Gode da nama sia: i.
8 Choncho Yeremiya anayitana Yohanani mwana wa Kareya pamodzi ndi atsogoleri onse a ankhondo amene anali naye ndiponso anthu onse, ana ndi akulu omwe.
Amaiba: le, na da Youha: ina: ne amola dadi gagui ouligisu dunu e sigi esalu, amola dunu eno huluane ilima gilisima: ne sia: i.
9 Yehova, Mulungu wa Israeli amene munanditumako kuti ndikapereke madandawulo mʼdzina lanu akuti,
Na da ilima amane sia: i, “Hina Gode, Isala: ili fi ilia Gode, Ema dilia da na Ema adole ba: musa: asunasi, E da amane sia: i,
10 “Ngati mukhala mʼdziko muno, ndiye kuti ndidzakukhazikitsani, osakuchotsani. Inde ndidzakudzalani osakuchotsani pakuti ndi kumva chisoni kwambiri chifukwa cha mavuto amene ndabweretsa pa inu.
‘Dilia da amo soge ganodini esaloma: ne hanai galea, Na da dilia fi gaguia gadomu - hame mugulumu. Na da dili bugimu amola hame fadegale fasimu. Na da dilima wadela: su iabeba: le, da: i diosa.
11 Musayiope mfumu ya ku Babuloni, imene mukuyiopa tsopano. Musachite nayo mantha, akutero Yehova, pakuti Ine ndili nanu ndipo ndidzakupulumutsani ndi kukulanditsani mʼmanja mwake.
Dilia Ba: bilone hina bagade ema beda: su hou yolesima. Na da dili amola nini esala. Amola ea gasa amoga dili se mae nabima: ne, Na da dili gaga: mu
12 Ndidzakuchitirani chifundo, ndipo mfumuyonso idzakuchitirani chifundo ndi kukulolani kuti mukhale mʼdziko mwanumwanu.
Bai Na da asigi amola gogolema: ne olofosu dawa: Na da hamobeba: le, Ba: bilone hina bagade da dilima asigimu, amola dilia sogedafa amoga buhagima: ne, logo doasimu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.’
13 “Koma mwina simudzamvera Yehova Mulungu wanu nʼkumanena kuti, ‘Ayi ife sitidzakhala mʼdziko muno,
Be dilia dunu amo da Yuda soge ganodini esalebe, Hina Gode Ea sia: amola amo soge ganodini bu esalumu amo mae higama. Agoane mae sia: ma, ‘Hame mabu! Ninia da asili, Idibidi sogega masunu. Bai amogawi ninia da gegesu hame ba: mu, amola gegemusa: ha lasu hame nabimu, amola hame ha: mu.’ Dilia da amane sia: sea, amasea Hina Gode Bagadedafa, Isala: ili fi ilia Gode, da amane sia: sa, ‘Dilia da Idibidi sogega esaloma: ne masunu hanai galea,
14 ndipo ngati mukunena kuti, ‘Ayi, koma tidzapita ku Igupto kumene sitidzaonako nkhondo kapena kumva kulira kwa lipenga kapenanso kusowa chakudya.’
15 Tsono, inu otsala a ku Yuda, imvani mawu a Yehova. Iye akuti, ngati mutsimikiza zopita ku Igupto, nʼkupitadi kukakhala kumeneko,
16 ndiye nkhondo imene mukuyiopayo idzakugonjetsani ku Igupto komweko. Njala imene mukuyiopayo idzakupezani ku Igupto komweko ndipo mudzafera kumeneko.
gegesu (amoga dilia da beda: i) amo da dilima doaga: mu amola ha: i bagade (amoga dilia da beda: i) amo dilia ba: mu. Amasea, dilia Idibidi soge ganodini bogogia: mu.
17 Kunena zoona, onse amene atsimikiza zopita ku Igupto kuti akakhale kumeneko adzafa ndi nkhondo njala ndi mliri. Palibe ndi mmodzi yemwe amene adzapulumuke kapena kuthawa mavuto amene ndidzawagwetsera.’
Dunu huluane amo da Idibidi sogega masunu hanai gala, amo huluane da gegesu o ha: i bagade o olosu amoga bogogia: i dagoi ba: mu. Dunu afae esalebe da hame ba: mu. Bai Na da ilima wadela: su bagade iasimu.’
18 Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti, ‘Momwe ndinawakwiyira mwaukali anthu okhala mu Yerusalemu, koteronso ndidzakukwiyirani mukapita ku Igupto. Mudzasanduka chinthu chotembereredwa ndi chochititsa mantha, choseketsa ndi chonyozeka. Malo ano simudzawaonanso.’
Hina Gode, Isala: ili fi ilia Gode, da amane sia: sa, ‘Na da Na ougi bagade amo Yelusaleme fi dunu ilima sogadigi. Amo defele, dilia da Na sia: mae nabawane Idibidi sogega ahoasea, Na da Na ougi bagade dilima sogadigimu. Dilia da wadela: lesi dagoi ba: mu. Dunu eno da dili higamu amola dilia dio amoga gagabusu aligima: ne ilegemu. Dilia da amo soge bu hamedafa ba: mu.’”
19 “Inu otsala a ku Yuda, Yehova wakuwuzani kuti, ‘Musapite ku Igupto.’ Dziwani chinthu ichi: Ine lero ndikukuchenjezani
Amalalu, na da eno amane sia: i, “Hina Gode da dili Yuda soge ganodini hame mugululi asi esalebe dunu dilima dilia Idibidi sogega mae masa: ne sia: i dagoi. Amaiba: le, na da dilima sisasu iaha.
20 kuti munalakwitsa kwambiri. Inu munandituma kwa Yehova Mulungu wanu nʼkumati ‘Mukatipempherere kwa Yehova Mulungu wathu, nʼkudzatiwuza chimene afuna kuti tichite, ndipo ife tidzachita.’
Dilia da bogoma: ne giadofasu hamonana. Dilia da nama na da Hina Godema dili fidima: ne sia: ne gadoma: ne sia: i. Amola dilia da Ea sia: i liligi huluane amoma fa: no bobogema: ne dafawane ilegele sia: i.
21 Ine lero ndakuwuzani, koma inu simukumverabe zonse zimene Yehova Mulungu anandituma kuti ndikuwuzeni.
Amola wali, na da dilima sia: huluane adoi dagoi. Be dilia sia: huluane amo Hina Gode da na dilima alofele iasima: ne asunasi, amo nabimu higasa.
22 Tsono dziwani ichi: mudzafadi ndi nkhondo, njala ndi mliri kumalo kumene mukufuna mukakhaleko.”
Amaiba: le, amo bu dawa: ma! Dilia da Idibidi sogega esaloma: ne masunu hanai gala. Be amo ganodini dilia da gegesu o ha: i bagade o olo bagade amoga bogogia: i dagoi ba: mu.”

< Yeremiya 42 >