< Yeremiya 4 >
1 “Ngati mukufuna kubwerera, inu Aisraeli, bwererani kwa Ine,” akutero Yehova. “Chotsani mafano anu onyansa pamaso panga ndipo musasocherenso.
Hina Gode da amane sia: sa, “Isala: ili fi dunu! Dilia da sinidigimusa: dawa: sea, Nama sinidigima. Dilia da moloiwane Nama fa: no bobogesea amola loboga hamoi ogogosu ‘gode’ fadegasea,
2 Muzilumbira mokhulupirika ndiponso mwa chilungamo kuti, ‘Pali Yehova wamoyo.’ Mukatero anthu a mitundu ina yonse adzandipempha kuti ndiwadalitse ndipo adzanditamanda.”
dilia da Na Dioba: le dafawane ilegemu da defea ba: mu. Amasea, fifi asi gala huluane da Nama Na da ili hahawane dogolegele sia: ma: ne adole ba: mu. Amola ilia da Nama nodone sia: ne gadomu.”
3 Zimene Yehova akunena kwa anthu a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu ndi izi: “Limani masala anu musadzale pakati pa minga.
Hina Gode da Yuda soge amola Yelusaleme moilai bai bagade dunu ilima amane sia: sa, “Dilia soge hame gidinai amo gidinama. Dilia hawa: amo aya: gaga: nomei gisi ganodini mae bugima.
4 Dziperekeni nokha kwa Ine kuti munditumikire ndi mtima wanu wonse, inu anthu a ku Yuda ndi ku Yerusalemu. Muzichita zimenezi kuopa kuti mkwiyo wanga ungabuke ngati moto ndi kukutenthani, chifukwa cha ntchito zanu zoyipazo popanda wina wowuzimitsa.
Dilia Gousa: su amo dilia da Na, Hina Gode, Nama hamoi, amo bu dawa: le, mae fima. Dilia Yuda amola Yelusaleme fi dunu! Nama sia: sima! Amane hame hamosea, Na ougi da lalu agoane nemu. Bai dilia wadela: le hamoi dagoi. Na ougi da dunu enoga ha: ba: domu hamedene nenanumu.”
5 “Lengeza ku Yuda ndi kulalikira mu Yerusalemu kuti, ‘Lizani lipenga mʼdziko lonse!’ Ndipo fuwulani kuti, ‘Sonkhanani! Tiyeni tithawire ku mizinda yotetezedwa!’
Soge huluane amo ganodini, dalabede fulaboma! Ha: giwane wele sia: ma! Yuda soge amola Yelusaleme fi dunu ilima ilia da gasa bagade gagole moilai bai bagadega hehenama: ne sia: ma!
6 Kwezani mbendera kuyangʼana ku Ziyoni! Musachedwe, thawani kuti mupulumuke! Pakuti Ine ndikubweretsa chilango kuchokera kumpoto, kudzakhala chiwonongeko choopsa.”
Saione amoma doaga: ma: ne, logo olelema! Dilia esalusu gaga: ma: ne hobeama! Mae aligima! Hina Gode da se nabasu amola soge wadela: su hou gagoe (north) amoga gaguli maha.
7 Monga mkango umatulukira mʼngaka yake momwemonso wowononga mayiko wanyamuka ndi kutuluka ku mbuto yake. Watero kuti awononge dziko lanu. Mizinda yanu idzakhala mabwinja popanda wokhalamo.
Laione wa: me da ea wamoaligisu amoga manebe, amo defele fifi asi gala wadela: su dunu da manebe goea. E da Yuda wadela: lesimusa: manebe. Yuda soge moilai huluane da mugului dagoi ba: mu. Amo ganodini, dunu afae esalebe da hame ba: mu.
8 Choncho valani ziguduli, lirani ndi kubuwula, pakuti mkwiyo waukulu wa Yehova sunatichokere.
Amaiba: le, wadela: i eboboi abula salawane, dima amola didigia: ma. Bai Hina Gode da Yuda fi ilima ougi bagade amola Ea ougi da hame gumi.
9 “Pa tsiku limenelo, mfumu ndi nduna zake adzataya mtima, ansembe adzachita mantha kwambiri, ndipo aneneri adzathedwa nzeru,” akutero Yehova.
Hina Gode da amane sia: i, “Amo esoha, hina bagade amola eagene ouligisu dunu da bagade beda: mu. Gobele salasu dunu amola balofede dunu da beda: ne, fofogadigimu.”
10 Ndipo ine ndinati, “Haa, Ambuye Yehova, ndithu munawanyenga anthu awa pamodzi ndi Yerusalemu pamene munanena kuti, ‘Mudzakhala pa mtendere,’ chonsecho lupanga lili pakhosi pathu.”
Amalalu, na da amane sia: i, “Ouligisudafa Hina Gode! Di da Yelusaleme fi dunu ilima dafawane ogogoi dagoi. Di da olofosu manebe sia: i dagoi, be ilia asogoa hedofama: ne, gegesu gobihei bagade galebe ba: sa.”
11 Nthawi imeneyo anthu awa ndi Yerusalemu adzawawuza kuti, “Mphepo yotentha yochokera ku magomo a mʼchipululu ikuwomba pa anthu anga, osati mphepo yopeta kapena yoyeretsa;
Eso da manebe, amoga Yelusaleme da sia: nabimu. Amo sia: da hafoga: i sogega gia: i bagade fo agoane ilima doaga: ma: ne manebe. Asaboi fo da gisi fawane gaguli ahoa. Be amo fo da agoaiwane hame.
12 koma mphepo yamphamvu kwambiri yochokera kwa Ine. Tsono ndi Ineyo amene ndikuwaweruza.”
Amo fo da Hina Gode da sia: beba: le misunu, amola fo eno ea gasa bagade baligimu. Bai amo fo da Hina Gode Hisu da Ea dunu fi ilima se ima: ne fofada: musa: manebe ba: mu.
13 Taonani, adani akubwera ngati mitambo, magaleta awo akubwera ngati kamvuluvulu, akavalo awo ndi aliwiro kupambana chiwombankhanga. Tsoka ilo! Tawonongeka!
Ba: ma: i! Ha lai dunu da mu mobi agoane manebe. Ea gegesu ‘sa: liode’ da fo ononoi defele ba: sa. Amola ea hosi ea hehenasu da buhiba ea hagili ahoasu baligisa. Ninia da fisi dagoi! Nini da wadela: lesi dagoi!
14 Iwe Yerusalemu, tsuka mtima wako kuchotsa zoyipa kuti upulumuke. Kodi maganizo ako oyipawo udzakhala nawo mpaka liti?
Yelusaleme! Dia gaga: su ba: ma: ne, dia dogo nigima: amo dodofema! Di da habogala wadela: i asigi dawa: su yolesima: bela: ?
15 Pakuti amithenga akulalika mawu mʼdziko la Dani; akulengeza za masautso kuchokera ku mapiri a Efereimu.
Sia: adola ahoasu dunu da Da: ne moilai amola Ifala: ime agolo amoga misini, wadela: su sia: olelesa.
16 Iwo akuti, “Fotokozani zimenezi kwa anthu a mitundu ina, lengezani zimenezi mu Yerusalemu kuti, ‘Ankhondo akubwera kuchokera ku dziko lakutali, akufuwula ndi kudzazinga mizinda ya Yuda.
Ilia da fifi asi gala ilima sisa: ma: ne misi. Amola Yelusaleme fi ilima ha lai da soge sedaganini manebe amo ilima sisasu olelemusa: misi. Amo ha lai dunu da Yuda soge moilai amoma ha lamu.
17 Azinga Yerusalemu ngati anthu olondera munda, chifukwa Yerusalemu wandiwukira,’” akutero Yehova.
Ilia da dunu da soge sosodo aligisu defele, Yelusaleme sisiga: mu. Bai Yelusaleme fi da Hina Gode Ema odoga: su. Hina Gode da sia: i dagoi.
18 “Makhalidwe anu ndi zochita zanu zakubweretserani zimenezi. Chimenechi ndiye chilango chanu. Nʼchowawa kwambiri! Nʼcholasa mpaka mu mtima!”
Yuda! Disu dia hamobeba: le amola dia esalusu hou amoba: le, amo se iasu da dima doaga: i. Dia wadela: i hou hamobeba: le, amo se nabasu da dima misi. Dia wadela: i hou da gobihei agoane dia dogo soi dagoi.
19 Mayo, mayo, ndikumva kupweteka! Aa, mtima wanga ukupweteka, ukugunda kuti thi, thi, thi. Sindingathe kukhala chete. Pakuti ndamva kulira kwa lipenga; ndamva mfuwu wankhondo.
Na da se nabi dagoi. Amo se nabasu nabimu da nama hamedei! Na dogo! Na dogo da ilibu agoane hedolole dusa! Na da ouiya: mu gogolesa. Na da dalabede fulabosu naba, amola gegesu halasu naba.
20 Tsoka limatsata tsoka linzake; dziko lonse lasanduka bwinja. Mwadzidzidzi matenti athu awonongedwa, mwa kanthawi kochepa nsalu zake zotchinga zagwetsedwa.
Wadela: su afae ba: lalu, wadela: su eno da hedolowane doaga: sa. Soge huluane da wadela: lesi dagoi. Hedolowane, ninia abula diasu da wadela: lesi dagoi ba: sa. Ilia abula da gadelale, fofonoboi dagoi ba: sa.
21 Kodi ndikhale ndikuona mbendera ya nkhondo, ndi kumva kulira kwa lipenga mpaka liti?
Gegesu da bagadewane heda: sa. Na da habowali seda amo gegesu ba: ma: bela: ? Dalabede ea fulabosu, na da naba. Amo na da habowali seda nabima: bela: ?
22 Yehova akuti, “Anthu anga ndi zitsiru; iwo sandidziwa. Iwo ndi ana opanda nzeru; samvetsa chilichonse. Ali ndi luso lochita zoyipa, koma sadziwa kuchita zabwino.”
Hina Gode da amane sia: sa, “Na fi dunu da gagaoui dagoi. Ilia da Na hame dawa: Ilia da gagaoui mano defele, asigi dawa: su hame gala. Ilia da wadela: i hou hamomusa: bagade dawa: su dunu agoai ba: sa. Be hou ida: iwane didili hamomusa: hamedafa dawa:”
23 Ndinayangʼana dziko lapansi, ndipo linali lopanda anthu ndi lopanda kanthu; ndinayangʼana thambo, koma linalibe kuwala kulikonse.
Na da osobo bagade ba: i. E da wadela: lesi dagoi ba: i. Na da mu ba: i. Be amoga da hadigi hame galu.
24 Ndinayangʼana mapiri, ndipo ankagwedezeka; magomo onse ankangosunthira uku ndi uku.
Na da goumi ba: i. Ilia da fogoi amola agolo da la: ididili, la: ididili fogolalebe ba: i.
25 Ndinayangʼana, ndipo sindinaone anthu; mbalame iliyonse ya mlengalenga inali itathawa.
Na ba: loba, dunu fi huluane da hamedafa gala. Sio fi huluane amola da hagili asi dagoi ba: i.
26 Ndinayangʼana, dziko lachonde linali litasanduka chipululu; mizinda yake yonse inali itasanduka bwinja pamaso pa Yehova, chifukwa cha mkwiyo wake.
Nasegagi soge huluane da hafoga: i soge agoane hamoi dagoi ba: i. Soge ea moilai bai bagade huluane da mugululi, wadela: lesi dagoi ba: i. Bai Hina Gode Ea ougi bagade da amo sogega dialebe ba: i.
27 Yehova akuti, “Dziko lonse lidzasanduka chipululu komabe sindidzaliwononga kotheratu.
(Hina Gode da amane sia: i dagoi, “Osobo bagade huluane da wadela: lesi dagoi ba: mu. Be Na da dafawanedafa hame wadela: lesimu.”)
28 Chifukwa chake dziko lapansi lidzalira ndipo thambo lidzachita mdima, pakuti ndayankhula ndipo sindidzafewa mtima, ndatsimikiza ndipo sindidzabwerera mʼmbuyo.”
Osobo bagade da da: i diomu. Mu da gasimu. Hina Gode da sia: i dagoi, amola E da Ea asigi dawa: su amo hame afadenemu. E da amo hou hamomusa: dawa: i dagoi, amola E da Ea asigi dawa: su hame bu sinidigimu.
29 Pakumva phokoso la okwera pa akavalo ndi la anthu oponya mivi, anthu a mʼmizinda adzathawa. Ena adzabisala ku nkhalango; ena adzakwera mʼmatanthwe mizinda yonse nʼkuyisiya; popanda munthu wokhalamo.
Dunu huluane da hosi amoga fila heda: i dunu amola dadi gagui dunu ilia halasu nabasea, hobeamu. Mogili da iwilaga hobeamu amola mogili da igi sogega hobeamu. Moilai huluane da dunu hamedafa esalebe ba: mu. Amola amo moilai ganodini, dunu da bu hamedafa fi dialumu.
30 Iwe Yerusalemu, ndiwe bwinja! Ukutanthauza chiyani kuvala zovala zofiira ndi kuvalanso zokometsera zagolide? Ngakhale udzikonze maso ako powapaka zokometsera, ukungodzivuta chabe. Zibwenzi zako zikukunyoza; zikufuna kuchotsa moyo wako.
Yelusaleme! Di da wadela: lesi dagoi ba: mu! Di da abuliba: le yoi abula gasisalabala? Dia da abuliba: le nina: hamoma: ne, igi noga: iwane legesa amola dia si amoga soa: legesala: ? Di da udigili nina: hamosa. Bai dima gamu dunu ilia da wali di higasa amola di medole legemusa: dawa: lala.
31 Ndikumva kulira ngati kwa mayi pa nthawi yake yobereka, kubuwula ngati kwa mayi amene akubereka mwana wake woyamba. Kuliraku ndi kwa anthu a mu Ziyoni, wefuwefu. Atambalitsa manja awo nʼkumati, “Kalanga ife! Tikukomoka. Moyo wathu waperekedwa kwa anthu otipha.”
Na da se nabasu wele sia: su, amo uda da ea magobo mano lamu gadenesa wele sia: be agoane wesa, amo nabi dagoi. Amo da fedege agoane, Yelusaleme ea mifo lamu hamedeiba: le, habe ha: ha: iya wele sia: nebe agoai nabi. E da ea lobo ilua: le amane sia: su, “Na da wadela: lesi dagoi. Ilia da na medole legemusa: manebe!”