< Yeremiya 38 >
1 Sefatiya mwana wa Matani, Gedaliya mwana wa Pasi-Huri, Yukali mwana wa Selemiya, ndi Pasi-Huri mwana wa Malikiya anamva zimene Yeremiya ankawuza anthu onse kuti,
At that time, says the Lord, I will be a God to the family of Israel, and they shall be to me a people.
2 “Yehova akuti, ‘Aliyense amene akhale mu mzinda muno adzafa ndi nkhondo njala kapena mliri. Koma aliyense amene atatuluke kukadzipereka kwa Ababuloni adzapulumutsa moyo wake; iyeyo adzakhala ndi moyo.
Thus says the Lord, I found him warm in the wilderness with them that were slain with the sword: go you and destroy not Israel.
3 Mzinda uno udzaperekedwa ndithu kwa gulu lankhondo la mfumu ya ku Babuloni, amene adzawulande.’”
The Lord appeared to him from afar, [saying], I have loved you with an everlasting love: therefore have I drawn you in compassion.
4 Tsono akuluakuluwo anawuza mfumu kuti, “Munthu uyu ayenera kuphedwa. Iye akutayitsa mtima asilikali pamodzi ndi anthu onse amene atsala mu mzinda muno, chifukwa cha zimene akuwawuza. Munthu ameneyu sakufunira zabwino anthuwa koma chiwonongeko chawo.”
For I will build you, and you shall be built, O virgin of Israel: you shall yet take your timbrel, and go forth with the party of them that make merry.
5 Mfumu Zedekiya anayankha kuti, “Munthuyu ali mʼmanja mwanu. Ine sindingakuletseni chimene mukufuna kumuchitira.”
For you have planted vineyards on the mountains of Samaria: plant you, and praise.
6 Choncho iwo anatenga Yeremiya nakamuponya mʼchitsime cha Malikiya, mwana wa mfumu, chimene chinali mʼbwalo la alonda. Iwo anamutsitsira mʼdzenjemo ndi chingwe. Munalibe madzi koma matope okhaokha, ndipo Yeremiya anamira mʼmatopewo.
For it is a day when those that plead on the mountains of Ephraim shall call, [saying], Arise you, and go up to Sion to the Lord your God.
7 Koma Ebedi-Meleki, Mkusi, mmodzi mwa anthu ofulidwa ogwira ntchito mʼnyumba ya mfumu, anamva kuti Yeremiya anamuponya mʼchitsime. Nthawi imeneyo nʼkuti mfumu ili ku chipata cha Benjamini.
For thus says the Lord to Jacob; Rejoice you, and exult over the head of the nations: make proclamation, and praise you: say, The Lord has delivered his people, the remnant of Israel.
8 Ebedi-Meleki anatuluka ku nyumba ya mfumu kukayiwuza kuti,
Behold, I bring them from the north, and will gather them from the end of the earth to the feast of the passover: and [the people] shall beget a great multitude, and they shall return hither.
9 “Mbuye wanga mfumu, zimene anthu awa amuchitira mneneri Yeremiya ndi zoyipa kwambiri. Iwo amuponya mʼchitsime, ndipo adzafa ndi njala chifukwa buledi watha mu mzinda muno.”
They went forth with weeping, and I will bring them back with consolation, causing them to lodge by the channels of waters in a straight way, and they shall not err in it: for I am become a father to Israel, and Ephraim is my firstborn.
10 Tsono mfumu inalamula Ebedi-Meleki, Mkusi, kuti, “Tenga anthu makumi atatu, ndipo mukamutulutse mʼchitsimemo mneneri Yeremiya asanafe.”
Hear the words of the Lord, you nations, and proclaim [them] to the islands afar off; say, He that scattered Israel will also gather him, and keep him as one that feeds his flock.
11 Pamenepo Ebedi-Meleki anatenga anthuwo, napita nawo ku nyumba ya mfumu ya pansi pa chipinda chosungiramo chuma. Kumeneko anakatengako sanza ndipo anatsitsira sanzazo ndi chingwe mʼchitsime mʼmene munali Yeremiya.
For the Lord has ransomed Jacob, he has rescued him out of the hand of them [that were] stronger than he.
12 Ebedi-Meleki, Mkusi, anawuza Yeremiya kuti, “Ika sanzazo mkwapa mwako kuti zingwe zingakupweteke.” Yeremiya anachitadi zimenezi,
And they shall come, and shall rejoice in the mount of Sion, and shall come to the good things of the Lord, [even] to a land of corn, and wine, and fruits, and cattle, and sheep: and their soul shall be as a fruitful tree; and they shall hunger no more.
13 ndipo anamukoka ndi zingwe ndi kumutulutsa mʼchitsimecho. Ndipo Yeremiya anakhalabe ku bwalo la alonda.
Then shall the virgins rejoice in the assembly of youth, and the old men shall rejoice; and I will turn their mourning into joy, and will make them merry.
14 Tsiku lina Mfumu Zedekiya anayitana mneneri Yeremiya ndipo anabwera naye ku chipata chachitatu cha Nyumba ya Yehova. Mfumu inawuza Yeremiya kuti, “Ndikufuna kukufunsa kanthu kena, ndipo usandibisire chilichonse.”
I will expand and cheer with wine the soul of the priests the sons of Levi, and my people shall be satisfied with my good things: thus says the Lord.
15 Yeremiya anati kwa Zedekiya, “Ndikakuyankhani, kodi simundipha? Ngakhaletu ine nditakulangizani, inu simudzandimvera.”
A voice was heard in Rama, of lamentation, and of weeping, and wailing; Rachel would not cease weeping for her children, because they are not.
16 Koma Mfumu Zedekiya mwachinsinsi inalumbira kwa Yeremiya kuti, “Pali Yehova wamoyo, amene amatipatsa moyo, sindidzakupha ngakhalenso kukupereka kwa amene akufuna kukuphawa.”
Thus says the Lord; Let your voice cease from weeping, and your eyes from your tears: for their is a reward for your works; and they shall return from the land of [your] enemies.
17 Pamenepo Yeremiya anati kwa Zedekiya, “Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti, ‘Ngati mutuluka kukadzipereka kwa ankhondo a mfumu ya ku Babuloni, mudzakhala ndi moyo ndipo mzinda uno sadzawutentha, inu pamodzi ndi banja lanu mudzakhala ndi moyo.
[There shall be] an dwelling [home] for your children.
18 Koma ngati simutuluka kukadzipereka kwa ankhondo a mfumu ya ku Babuloni, mzinda uno udzaperekedwa kwa Ababuloni ndipo adzawutentha; inuyo simudzapulumuka mʼdzanja mwawo.’”
I have heard the sound of Ephraim lamenting, [and saying], You have chastened me, and I was chastened; I as a calf was not [willingly] taught: turn you me, and I shall turn; for you [are] the Lord my God.
19 Mfumu Zedekiya inati kwa Yeremiya, “Ine ndikuopa Ayuda amene anathawira kale kwa Ababuloni, pakuti mwina Ababuloniwo adzandipereka kwa Ayudawo ndipo iwowo adzandizunza.”
For after my captivity I repented; and after I knew, I groaned for the day of shame, and showed you that I bore reproach from my youth.
20 Yeremiya anayankha kuti, “Ngati mumvera Yehova ndi kuchita zimene ndakuwuzani, ndiye kuti zinthu zidzakuyenderani bwino. Inu simudzaphedwa.
Ephraim is a beloved son, a pleasing child to me: for because my words are in him, I will surely remember him: therefore I made haste [to help] him; I will surely have mercy upon him, says the Lord.
21 Koma mukakana kudzipereka, chimene Yehova wandiwululira ndi ichi:
Prepare yourself, O Sion; execute vengeance; look to your ways: return, O virgin of Israel, by the way by which you went, return mourning to your cities.
22 Akazi onse amene atsala mʼnyumba ya mfumu ya Yuda adzaperekedwa kwa akuluakulu a mfumu ya ku Babuloni. Akazi amenewo adzakuwuzani kuti, “‘Abwenzi ako okhulupirika aja anakusokeretsa, ndipo anakugonjetsa. Poti tsopano miyendo yako yazama mʼmatope; abwenzi ako aja akusiya.’
How long, O disgraced daughter, will you turn away? for the Lord has created safety for a new plantation: men shall go about in safety.
23 “Akazi pamodzi ndi ana anu adzaperekedwa kwa Ababuloni. Inuyo simudzapulumuka mʼmanja mwawo koma mfumu ya ku Babuloni idzakugwirani; mzinda uno adzawutentha.”
For thus says the Lord; They shall yet speak this word in the land of Juda, and in the cities thereof, when I shall turn his captivity; blessed be the Lord on his righteous holy mountain!
24 Pamenepo Zedekiya anati kwa Yeremiya, “Usawuze munthu wina aliyense zimene takambiranazi, ukatero udzaphedwa.
And there shall be dwellers in the cities of Juda, and in all his land, together with the husbandman, and [the shepherd] shall go forth with the flock.
25 Akuluakulu akamva kuti ndinayankhula nawe ndipo akabwera kwa iwe nʼkudzakufunsa kuti, ‘Tiwuze zimene unanena kwa mfumu ndi zimene mfumu inanena kwa iwe; usatibisire, ukatero tidzakupha,’
For I have saturated every thirsting soul, and filled every hungry soul.
26 udzawawuze kuti, ‘Ine ndimapempha mfumu kuti isandibwezerenso ku nyumba ya Yonatani kuti ndikafere kumeneko.’”
Therefore I awake, and saw; and my sleep was sweet to me.
27 Akuluakulu onse anabweradi kwa Yeremiya kudzamufunsa. Iye anawayankha monga momwe mfumu inamulamula. Choncho palibe amene ananenanso kanthu, pakuti palibe amene anamva zomwe anakambirana ndi mfumu.
Therefore, behold, the days come, says the Lord, when I will sow the house of Israel and the house of Juda with the seed of man, and the seed of beast.
28 Ndipo Yeremiya anakhalabe mʼbwalo la alonda mpaka tsiku limene mzinda wa Yerusalemu unalandidwa.
And it shall come to pass, that as I watched over them, to pull down, and to afflict, so will I watch over them, to build, and to plant, says the Lord.
In those days they shall certainly not say, The fathers ate a sour grape, and the children's teeth were set on edge.
But every one shall die in his own sin; and the teeth of him that eats the sour grape shall be set on edge.
Behold, the days come, says the Lord, when I will make a new covenant with the house of Israel, and with the house of Juda:
not according to the covenant which I made with their fathers in the day when I took hold of their hand to bring them out of the land of Egypt; for they abode not in my covenant, and I disregarded them, says the Lord.
For this is my covenant which I will make with the house of Israel; after those days, says the Lord, I will surely put my laws into their mind, and write them on their hearts; and I will be to them a God, and they shall be to me a people.
And they shall not at all teach every one his [fellow] citizen, and every one his brother, saying, Know the Lord: for all shall know me, from the least of them to the greatest of them: for I will be merciful to their iniquities, and their sins I will remember no more.
Thus says the Lord, who gives the sun for a light by day, the moon and the stars for a light by night, and [makes] a roaring in the sea, so that the waves thereof roar; the Lord Almighty is his name:
if these ordinances cease from before me, says the Lord, then shall the family of Israel cease to be a nation before me forever.
Though the sky should be raised to a [greater] height, says the Lord, and though the ground of the earth should be sunk [lower] beneath, yet I will not cast off the family of Israel, says the Lord, for all that they have done.
Behold, the days come, says the Lord, when the city shall be built to the Lord from the tower of Anameel to the gate of the corner.
And the measurement of it shall proceed in front of them as far as the hills of Gareb, and it shall be compassed with a circular wall of choice stones.
And all the Asaremoth even to Nachal Kedron, as far as the corner of the horse-gate eastward, shall be holiness to the Lord; and it shall not fail any more, and shall not be destroyed for ever.