< Yeremiya 34 >
1 Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni ndi gulu lake lonse lankhondo, pamodzi ndi maufumu onse a pa dziko lapansi amene ankawalamulira ndiponso anthu a mitundu yonse ankathira nkhondo Yerusalemu ndi mizinda yonse yozungulira Yehova anayankhula ndi Yeremiya kuti,
Ka Nebukadneza ruodh Babulon kod jolweny mage duto gi pinjeruodhi duto gi ji duto mane ni e gwengʼ mane orito ne kedo gi Jerusalem kod dala mane olwore duto, wachni nobiro ne Jeremia koa ir Jehova Nyasaye:
2 “Yehova, Mulungu wa Israeli akuti: Pita kwa Zedekiya mfumu ya Yuda ndipo ukamuwuze kuti Yehova akuti mzinda uno ndidzawupereka mʼmanja mwa mfumu ya ku Babuloni ndipo adzawutentha ndi moto.
“Ma e gima Jehova Nyasaye, Nyasach Israel, wacho: Dhi ir Zedekia ruodh Juda kendo inyise kama, ‘Ma e gima Jehova Nyasaye wacho: Achiegni chiwo dala maduongʼni ne ruodh Babulon, kendo enowangʼe pep.
3 Iweyo sudzapulumuka mʼmanja mwake koma udzagwidwa ndithu ndipo adzakupereka mʼmanja mwake. Udzayiona mfumu ya ku Babuloni maso ndi maso ako ndipo udzayankhula nayo pakamwa ndi pakamwa. Ndipo udzapita ku Babuloni.
Ok initony ngangʼ e wachni to adiera enomaki kendo nochiwi ne en. Inine ruodh Babulon gi wengeni iwuon, kendo enowuo kodi wangʼ gi wangʼ kendo inidhi Babulon.
4 “Koma iwe Zedekiya mfumu ya Yuda, imva lonjezo ili la Yehova. Izi ndi zimene Yehova akunena za iwe: Sudzaphedwa pa nkhondo;
“‘Kata kamano winj singruok mar Jehova Nyasaye, yaye Zedekia ruodh Juda. Ma e gima Jehova Nyasaye wacho kuomi: Ok enonegi gi ligangla;
5 udzafera pa mtendere. Monga anthu ankafukiza lubani poyika maliro a makolo ako akale, amene anali mafumu iwe usanalowe ufumu, choncho nawenso podzayika maliro ako adzafukiza lubani ndipo polira azidzati, ‘Kalanga, mbuye wanga!’ Ine mwini ndalonjeza zimenezi, akutero Yehova.”
initho gi kwe. Kaka ji noloso mach mar liel mar miyo wuonu luor; ruodhi machon mane otelo nyimi, mondo omi gilos mach mar miyi luor kendo mar ywak, “Aa, yaye jatelo!” An awuon aketo singoni, Jehova Nyasaye owacho.’”
6 Ndipo mneneri Yeremiya anawuza zonsezi Zedekiya mfumu ya Yuda, mu Yerusalemu.
Eka Jeremia janabi nonyiso Zedekia ruodh Juda gigo duto e Jerusalem,
7 Nthawi imeneyi nʼkuti gulu lankhondo la mfumu ya ku Babuloni likuthira nkhondo Yerusalemu ndi mizinda ina yotsala ya Yuda, Lakisi ndi Azeka. Imeneyi yokha ndiye inali mizinda yotetezedwa yotsala ya ku Yuda.
sa mane jolweny mar ruodh Babulon ne kedo gi Jerusalem kod mier madongo mamoko mag Juda mane pod odongʼ, ma gin Lakish kod Azeka. Magi kende e mier madongo mochiel motegno gohinga mane odongʼ e Juda.
8 Yehova anayankhulanso ndi Yeremiya. Nthawi imeneyi nʼkuti mfumu Zedekiya atachita pangano ndi anthu onse a mu Yerusalemu kuti alengeze zakuti akapolo awo adzawamasule.
Wach Jehova Nyasaye nobiro ne Jeremia bangʼ ka Zedekia noloso winjruok gi ji duto man Jerusalem mondo oland ni wasumbini owe thuolo.
9 Aliyense amene anali ndi akapolo a Chihebri, aamuna kapena aakazi awamasule; palibe amene ayenera kusunga mu ukapolo Myuda mnzake.
Ngʼato ka ngʼato ne onego we misumbane ma ja-Hibrania, madichwo kod ma dhako; onge ngʼama ne dongʼ gi ja-Yahudi wadgi e twech.
10 Choncho akuluakulu pamodzi ndi anthu onse amene anachita pangano ili anagwirizana kuti amasule akapolo awo aamuna ndi aakazi ndi kuti asawasungenso mu ukapolo. Iwo anachitadi zimenezi ndipo anawamasuladi.
Omiyo jotelo duto kod ji mane odonjo e winjruokni noyie ni giniwe thuolo wasumbini mag-gi machwo kod mamon kendo ok ginibed e twech kendo. Ne giyie, kendo ne giwegi thuolo.
11 Koma pambuyo pake anasintha maganizo awo ndi kuwatenganso amuna ndi akazi amene anawamasula aja ndipo anawasandutsanso akapolo.
To bangʼe negiloko pachgi mi gikawo kendo wasumbinigi mane giseweyo thuolo mi giketogi gibedo wasumbini kendo.
12 Tsono Yehova anawuza Yeremiya kuti:
Eka wach Jehova Nyasaye nobiro ne Jeremia kama:
13 “Yehova Mulungu wa Israeli akuti: Ine ndinachita pangano ndi makolo anu pamene ndinawatulutsa ku Igupto, mʼdziko la ukapolo. Ine ndinati,
“Ma e gima Jehova Nyasaye, Nyasach Israel, wacho: Ne aketo winjruok gi kwereu mane agologi gia Misri, e piny mar bedo misumba. Ne awacho ni,
14 ‘Chaka chachisanu ndi chiwiri chilichonse aliyense wa inu ayenera kumasula mʼbale wake wa Chihebri amene anadzigulitsa yekha kwa inuyo. Iyeyo amasulidwe akagwira ntchito zaka zisanu ndi chimodzi, mumulole apite mwaufulu.’ Komatu makolo anu sanandimvere kapena kusamala konse.
‘E higa mar abiriyo ka higa mar abiriyo ngʼato ka ngʼato kuomu nyaka we ja-Hibrania wadgi thuolo ma osebedo katiyone. Bangʼ ka osetiyone kuom higni auchiel, nyaka iweye thuolo.’ Wuoneu, kata kamano, ne ok owinja kata luoro chikna.
15 Posachedwa pomwepa inu munalapa ndi kuchita zinthu zabwino pamaso panga: Aliyense wa inu anamasula mʼbale wake. Ndipo munachita pangano pamaso panga mʼNyumba imene imadziwika ndi dzina langa kuti mudzachitadi zimenezi.
Kinde mosekadho machiegni, ne ikwayo weruok kendo ne itimo gima nikare e nyim wangʼa: Un duto ne uyie weyo oweteu thuolo. Bende ne utimo singruok e nyima e ot motingʼo Nyinga.
16 Koma tsopano mwasintha maganizo anu ndipo mwayipitsa dzina langa. Mwatenganso ukapolo aamuna ndi aakazi amene munawamasula aja kuti apite kumene akufuna. Mwawakakamiza kuti akhalebe akapolo anu.
To koro uselokoru kendo usedwanyo nyinga; uduto usekawo wasumbini machwo kod mamon mane useweyo thuolo mondo gidhi kama gidwaro. Usechunogi mondo gibed wasumbini magu kendo.
17 “Nʼchifukwa chake Yehova akuti: Inu simunandimvere Ine; simunalengeze kuti abale anu amasulidwe. Chabwino! Ine ndidzakupatsani ufulu; ufulu wake ukhala wophedwa ndi nkhondo, mliri ndi njala. Ndidzakusandutsani chinthu chochititsa mantha pakati pa maufumu onse a dziko lapansi.
“Emomiyo, ma e gima Jehova Nyasaye wacho: Pod ok uluora; pod ok uyie weyo oweteu thuolo. Omiyo koro awacho mondo owenu thuolo mondo onegu gi ligangla, masiche kod kech. Anami ogendini manie piny duto bedo gibuok ka ginenou.
18 Inu simunasunge pangano limene munachita ndi Ine. Simunasamale lonjezo limene munachita pamaso panga. Choncho ndidzakusandutsani ngati mwana wangʼombe uja amene ankamudula pawiri napita pakati pa zigawozo.
Chwo duto ma oseketho winjruokna kendo pod ok ochopo winjruok mane giloso e nyima, nakawgi ka nyaroya mane gingʼado nyadiriyo kendo giwuotho e kind lemogo.
19 Amene ankadutsa pakati pa zigawozo anali atsogoleri a Yuda ndi Yerusalemu, akuluakulu a bwalo, ansembe ndi anthu onse a mʼdzikomo.
Jotend Juda gi Jerusalem, jotelo mag agola, jodolo kod ji duto mag pinyni mane owuotho e kind lemo ariyogo,
20 Onsewa ndidzawapereka kwa adani awo amene akufuna kuwapha. Mitembo yawo idzakhala chakudya cha mbalame zamlengalenga ndi zirombo za dziko lapansi.
anachiwgi ne wasikgi madwaro ngimagi. Ringregi motho nobed chiemb winy mafuyo e kor polo kod le manie piny.
21 “Ndidzapereka Zedekiya mfumu ya Yuda ndi nduna zake kwa adani awo amene akufuna kuwapha, kwa gulu lankhondo la mfumu ya ku Babuloni limene nthawi ino layamba kubwerera mʼmbuyo.
“Anachiw Zedekia ruodh Juda kod jotende ne wasike madwaro ngimagi, ne jolwenj ruodh Babulon, mosengʼanyo oa kuomu.
22 Taonani, Ine ndidzawalamula, akutero Yehova, ndipo ndidzawabweretsanso ku mzinda uno. Adzathira nkhondo mzindawu, kuwulanda ndi kuwutentha. Ndipo Ine ndidzasandutsa chipululu mizinda ya Yuda kotero kuti palibe amene adzakhalemo.”
Anachiw chik, Jehova Nyasaye wacho, kendo anadwog-gi e dala maduongʼni. Giniked kode, ginikawe kendo giwangʼe pep. Kendo anaketh dala mag Juda mondo kik ngʼato angʼata dag kanyo.”