< Yeremiya 30 >

1 Yehova anawuza Yeremiya kuti,
Rijeè koja doðe Jeremiji od Gospoda govoreæi:
2 “Ine Yehova, Mulungu wa Israeli ndikuti, ‘Lemba mʼbuku mawu onse amene ndakuwuza.
Ovako veli Gospod Bog Izrailjev govoreæi: napiši u knjigu sve rijeèi koje ti govorih.
3 Nthawi ikubwera pamene ndidzachotse anthu anga, Israeli ndi Yuda kuchokera ku ukapolo ndi kuwabwezera dziko limene ndinapatsa makolo awo,’ akutero Yehova.”
Jer evo idu dani, govori Gospod, kad æu povratiti roblje naroda svojega Izrailja i Jude, govori Gospod, i dovešæu ih natrag u zemlju koju sam dao ocima njihovijem, i držaæe je.
4 Nawa mawu amene Yehova anayankhula ndi anthu a ku Israeli ndi Yuda:
I ovo su rijeèi koje reèe Gospod za Izrailja i Judu.
5 “Yehova akuti: “Ndamva kulira chifukwa cha nkhawa, ndamva kulira kwa mantha popeza palibe mtendere.
Jer ovako veli Gospod: èusmo viku od prepadanja, straha, a mira nema.
6 Tsono khalani pansi ndi kudzifunsa kuti: Kodi munthu wamwamuna angathe kubereka mwana? Nanga nʼchifukwa chiyani ndikuona munthu aliyense wamwamuna atagwira manja ake pa mimba pake ngati mayi pa nthawi yake yochira? Chifukwa chiyani nkhope iliyonse ili yakugwa?
Pitajte, i vidite, eda li muško raða? zašto dakle vidim gdje se svaki èovjek drži rukama svojima za bedra svoja kao porodilja i u svijeh se promijenila lica i poblijedjela?
7 Mayo ine! Tsiku limeneli ndi lalikulu kwambiri! Sipadzakhala lina lofanana nalo. Idzakhala nthawi ya masautso kwa Yakobo, koma adzapulumuka ku masautsowo.”
Jaoh! jer je velik ovaj dan, nije bilo takoga, i vrijeme je muke Jakovljeve, ipak æe se izbaviti iz nje.
8 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Pa tsiku limenelo, ndidzathyola goli la ukapolo mʼkhosi mwawo ndipo ndidzadula zingwe zowamanga; Aisraeli sadzakhalanso akapolo a alendo.
Jer u taj dan, govori Gospod nad vojskama, slomiæu jaram njegov s vrata tvojega, i sveze tvoje pokidaæu; i neæe ga više tuðini nagoniti da im služi.
9 Mʼmalo mwake, adzatumikira Yehova Mulungu wawo ndiponso Davide mfumu yawo, amene ndidzawasankhira.
Nego æe služiti Gospodu Bogu svojemu i Davidu caru svojemu, kojega æu im podignuti.
10 “‘Tsono usachite mantha, iwe mtumiki wanga Yakobo; usade nkhawa, iwe Israeli,’ akutero Yehova. ‘Ndithu ndidzakupulumutsa kuchokera ku dziko lakutali, zidzukulu zako kuchokera ku dziko la ukapolo wawo. Yakobo adzabwerera ndipo adzakhala modekha pa mtendere, ndipo palibe amene adzamuchititsa mantha.
Ti se dakle ne boj, Jakove slugo moj, govori Gospod, i ne plaši se, Izrailju; jer, evo, ja æu te izbaviti iz daljne zemlje, i sjeme tvoje iz zemlje ropstva tvojega, i Jakov æe se vratiti i poèivati, i biæe miran, i niko ga neæe plašiti.
11 Ine ndili nanu ndipo ndidzakupulumutsani,’ akutero Yehova. ‘Ngakhale ndidzawononga kotheratu mitundu yonse ya anthu kumene ndinakubalalitsirani, koma inu sindidzakuwonongani kotheratu. Sindidzakulekani kuti mukhale osalangidwa. Koma ndidzakulangani mwachilungamo.’”
Jer sam ja s tobom, govori Gospod, da te izbavim; i uèiniæu kraj svijem narodima, meðu koje sam te rasijao, ali tebi neæu uèiniti kraja, nego æu te pokarati s mjerom, a neæu te ostaviti sasvijem bez kara.
12 Yehova akuti, “Chilonda chanu nʼchosachizika, bala lanu ndi lonyeka.
Jer ovako veli Gospod: smrtan je polom tvoj i rana tvoja ljuta.
13 Palibe amene angathe kukutetezani pa mlandu wanu, palibe chiyembekezo choti inu nʼkuchira, palibe mankhwala ochiritsa inu.
Nema nikoga koji bi se primio tvoje stvari da te lijeèi, nema lijeka koji bi ti pomogao.
14 Abwenzi anu onse akuyiwalani; sasamalanso za inu. Ndakukanthani ngati mmene mdani akanachitira. Ndipo ndakulangani mwa nkhanza, chifukwa machimo anu ndi ambiri, ndipo kulakwa kwanu ndi kwakukulu.
Svi koji te ljube zaboraviše te, ne traže te, jer te udarih udarcem neprijateljskim, karom žestokim, za mnoštvo bezakonja tvojega, za silne grijehe tvoje.
15 Chifukwa chiyani mukulira nacho chilonda chanu? Bala lanu silingapole ayi. Ine ndakuchitani zimenezi chifukwa machimo anu ndi ambiri ndipo kulakwa kwanu nʼkwakukulu.
Zašto vièeš radi rane svoje, smrtnoga bola svojega? za mnoštvo bezakonja tvojega, za silne grijehe tvoje èinim ti to.
16 “Tsono onse amene anakuwonongani, nawonso adzawonongedwa; adani anu onse adzapita ku ukapolo. Iwo amene anafunkha zinthu zanu, zinthu zawo zidzafunkhidwanso; onse amene anakusakazani nawonso adzasakazidwa.
Ali svi koji te proždiru, proždrijeæe se, i neprijatelji tvoji svikoliki otiæi æe u ropstvo, i koji te gaze, biæe pogaženi, i sve koji te plijene, daæu ih da se oplijene.
17 Ndidzachiza matenda anu ndi kupoletsa zilonda zanu, akutero Yehova, ‘chifukwa mukutchedwa anthu otayika. Amati, ndi anthu a ku Ziyoni awa amene alibe wowasamala.’”
Jer æu te iscijeliti, i rane æu ti izlijeèiti, govori Gospod, jer te zvaše otjeranom: Sionom, kojega niko ne traži.
18 Yehova akuti, “Ndidzabwera nalo banja la Yakobo ku dziko lawo ndipo ndidzachitira chifundo malo ake okhalamo; mzinda wa Yerusalemu udzamangidwanso pa bwinja pake, nyumba yaufumu idzamangidwanso pa malo pake penipeni.
Ovako veli Gospod: evo, ja æu povratiti iz ropstva šatore Jakovljeve i smilovaæu se na stanove njegove; i grad æe se sazidati na mjestu svom, i dvor æe stajati na svoj naèin.
19 Anthuwo adzayimba nyimbo zoyamika Yehova ndipo kudzamveka phokoso lachisangalalo. Ndidzawachulukitsa, ndipo chiwerengero chawo sichidzatsika; ndidzawapatsa ulemerero, ndipo sadzanyozedwanso.
I iz njih æe izlaziti hvale i glas ljudi veselijeh, jer æu ih umnožiti, i neæe se umaljivati, i uzvisiæu ih, i neæe se poniziti.
20 Ana awo adzakhalanso monga mmene analili kale, ndipo gulu lawo ndidzalikhazikitsa pamaso panga; ndidzalanga onse owazunza.
I sinovi æe njegovi biti kao prije, i zbor æe njegov biti utvrðen preda mnom, i pohodiæu sve koji mu èine silu.
21 Mtsogoleri wawo adzakhala mmodzi mwa iwo. Wodzawalamulira adzachokera pakati pawo. Choncho ndidzawakokera kufupi ndi Ine ndipo iye adzandiyandikira. Ndani angalimbe mtima payekha kuyandikana nane popanda kuyitanidwa?” akutero Yehova.
I knez æe njihov biti od njih, i vladalac æe njihov izlaziti isred njih; i daæu mu da pristupa, i pristupaæe k meni; jer ko je taj koji se usuðuje pristupiti k meni? govori Gospod.
22 “Choncho inu mudzakhala anthu anga, ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wanu.”
I biæete mi narod, i ja æu vam biti Bog.
23 Taonani ukali wa Yehova wowomba ngati mphepo ya mkuntho. Mphepo ya namondwe ikuwomba pa mitu ya anthu oyipa.
Gle, vihor Gospodnji, gnjev, iziæi æe, vihor, koji ne prestaje, pašæe na glavu bezbožnicima.
24 Mkwiyo woopsa wa Yehova sudzachoka mpaka atakwaniritsa zolinga za mu mtima mwake. Mudzamvetsa zimenezi masiku akubwerawo.
Neæe se povratiti žestoki gnjev Gospodnji dokle ne uèini i izvrši što je naumio u srcu svom; napošljetku æete razumjeti to.

< Yeremiya 30 >