< Yeremiya 30 >
1 Yehova anawuza Yeremiya kuti,
Hina Gode, Isala: ili fi ilia Gode, da nama amane sia: i,
2 “Ine Yehova, Mulungu wa Israeli ndikuti, ‘Lemba mʼbuku mawu onse amene ndakuwuza.
“Na dima sia: i liligi huluane buga ganodini dedema.
3 Nthawi ikubwera pamene ndidzachotse anthu anga, Israeli ndi Yuda kuchokera ku ukapolo ndi kuwabwezera dziko limene ndinapatsa makolo awo,’ akutero Yehova.”
Bai eso da doaga: mu amoga Na da Na fi Isala: ili amola Yuda fi ilima gaheabolo hou hamomu. Na da soge amo Na da ilia aowalalia ilima i, amoga Na fi bu oule misunu. Amasea, ilia da amo soge bu lale gagumu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
4 Nawa mawu amene Yehova anayankhula ndi anthu a ku Israeli ndi Yuda:
Hina Gode da Isala: ili amola Yuda fi dunu ilima amane sia: sa,
5 “Yehova akuti: “Ndamva kulira chifukwa cha nkhawa, ndamva kulira kwa mantha popeza palibe mtendere.
“Na da beda: iwane dibi nabi. Amo da olofosu hame be beda: iba: le agoane dibi.
6 Tsono khalani pansi ndi kudzifunsa kuti: Kodi munthu wamwamuna angathe kubereka mwana? Nanga nʼchifukwa chiyani ndikuona munthu aliyense wamwamuna atagwira manja ake pa mimba pake ngati mayi pa nthawi yake yochira? Chifukwa chiyani nkhope iliyonse ili yakugwa?
Dilia! Aligima! Amola dawa: ma! Dunu da mano lalelegema: bela: ? Hame mabu! Amaiba: le, abuliba: le dunu huluane da uda mano lamu gadenebe defele, ea hagomo hi loboga digili ba: sala: ? Dunu huluane ilia odagi da abuliba: le haliga: sala: ?
7 Mayo ine! Tsiku limeneli ndi lalikulu kwambiri! Sipadzakhala lina lofanana nalo. Idzakhala nthawi ya masautso kwa Yakobo, koma adzapulumuka ku masautsowo.”
Se nabasu bagadedafa eso da doaga: mu. Agoaiwane eso da musa: hame ba: i amola fa: no hamedafa ba: mu. Na fi da bogomuwane se bagade nabimu. Be ilia da mae bogole, esalumu.”
8 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Pa tsiku limenelo, ndidzathyola goli la ukapolo mʼkhosi mwawo ndipo ndidzadula zingwe zowamanga; Aisraeli sadzakhalanso akapolo a alendo.
Hina Gode Bagadedafa da amane sia: sa, “Amo eso doaga: sea, Na da ‘youge’ ilia galogoa gasisali amo fifimu amola ilia sia: ine la: gi amo fadegamu. Ilia da hahawane asili, udigili hawa: hamosu dunu, amola ga fi dunu agoane bu hame ba: mu.
9 Mʼmalo mwake, adzatumikira Yehova Mulungu wawo ndiponso Davide mfumu yawo, amene ndidzawasankhira.
Be ilia Na, ilia Hina Gode, amo Na hawa: hamosu hamomu. Amola Na da Da: ibidi egaga fi Dunu afae, Isala: ili Hina Bagade hamoma: ne, ilegemu. Ilia da Ema hawa: hamomu.
10 “‘Tsono usachite mantha, iwe mtumiki wanga Yakobo; usade nkhawa, iwe Israeli,’ akutero Yehova. ‘Ndithu ndidzakupulumutsa kuchokera ku dziko lakutali, zidzukulu zako kuchokera ku dziko la ukapolo wawo. Yakobo adzabwerera ndipo adzakhala modekha pa mtendere, ndipo palibe amene adzamuchititsa mantha.
Na fi dunu! Mae beda: ma! Isala: ili fi dunu! Mae baligili beda: ma! Dilia da soge sedagaga udigili hawa: hamonana. Be Na da amogawi dili gaga: mu. Dilia da buhagili, olofoiwane esalumu. Dilia da gaga: i dagoi ba: mu, amola eno dunu dili beda: ma: ne hamomu da hamedei ba: mu.
11 Ine ndili nanu ndipo ndidzakupulumutsani,’ akutero Yehova. ‘Ngakhale ndidzawononga kotheratu mitundu yonse ya anthu kumene ndinakubalalitsirani, koma inu sindidzakuwonongani kotheratu. Sindidzakulekani kuti mukhale osalangidwa. Koma ndidzakulangani mwachilungamo.’”
Na da dilima misini, dili gaga: mu. Na da fifi asi gala huluane amoga Na da dili afagogoi, amo wadela: lesimu. Be Na da dili hame wadela: mu. Na da dilima se imunu, be moloidafa imunu amola baligili hame imunu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
12 Yehova akuti, “Chilonda chanu nʼchosachizika, bala lanu ndi lonyeka.
Hina Gode da Ea fi dunu ilima amane sia: sa, “Dilia fa: ginisi da bahomu hamedei. Dilia da uhimu hame dawa:
13 Palibe amene angathe kukutetezani pa mlandu wanu, palibe chiyembekezo choti inu nʼkuchira, palibe mankhwala ochiritsa inu.
Dilia da ouligisu dunu hame. Dilia da aiya legesu dunu hame gala. Uhimu da hamedei.
14 Abwenzi anu onse akuyiwalani; sasamalanso za inu. Ndakukanthani ngati mmene mdani akanachitira. Ndipo ndakulangani mwa nkhanza, chifukwa machimo anu ndi ambiri, ndipo kulakwa kwanu ndi kwakukulu.
Dilima magesa: i dunu da dili gogolei dagoi. Ilia da musa: dilima asigisu be wali hame. Na da dilia ha lai defele, dilima doagala: i. Dilima se iasu da gasa bagade ba: i. Bai dilia wadela: i hou da bagadedafa.
15 Chifukwa chiyani mukulira nacho chilonda chanu? Bala lanu silingapole ayi. Ine ndakuchitani zimenezi chifukwa machimo anu ndi ambiri ndipo kulakwa kwanu nʼkwakukulu.
Dilia se nababeba: le, bu mae egama. Dilia uhimu da hamedei. Dilia wadela: i hou da bagadedafa. Amaiba: le, Na da amaiwane dilima se iasu.
16 “Tsono onse amene anakuwonongani, nawonso adzawonongedwa; adani anu onse adzapita ku ukapolo. Iwo amene anafunkha zinthu zanu, zinthu zawo zidzafunkhidwanso; onse amene anakusakazani nawonso adzasakazidwa.
Be wali, dilia ha lai huluane amo da dili uasuli na dagoi, amo Na da uasuli na dagomu. Dili ha lai da afugili udigili hawa: hamoma: ne asi dagoi ba: mu. Nowa da dili banenesi, Na da amo banenesimu. Nowa da dilia liligi gegenana lai, amo ilia liligi gegenana lai dagoi ba: mu.
17 Ndidzachiza matenda anu ndi kupoletsa zilonda zanu, akutero Yehova, ‘chifukwa mukutchedwa anthu otayika. Amati, ndi anthu a ku Ziyoni awa amene alibe wowasamala.’”
Na da dili uhinisimu. Dilia ha lai da, ‘Saione fi da fisi dagoi. Huluane da ilima hame asigisa,’ amane sia: sa. Be Na da dilia fa: ginisi bahoma: ne, uhinisimu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
18 Yehova akuti, “Ndidzabwera nalo banja la Yakobo ku dziko lawo ndipo ndidzachitira chifundo malo ake okhalamo; mzinda wa Yerusalemu udzamangidwanso pa bwinja pake, nyumba yaufumu idzamangidwanso pa malo pake penipeni.
Hina Gode da amane sia: sa, “Na da Na fi ilia sogedafa amoga buhagima: ne, logo fodomu. Na da sosogo fi huluane ilima asigimu. Yelusaleme da bu gagui dagoi ba: mu. Amola ea hina bagade diasu bu gagui dagoi ba: mu.
19 Anthuwo adzayimba nyimbo zoyamika Yehova ndipo kudzamveka phokoso lachisangalalo. Ndidzawachulukitsa, ndipo chiwerengero chawo sichidzatsika; ndidzawapatsa ulemerero, ndipo sadzanyozedwanso.
Dunu amogawi esalebe da nodone gesami hea: mu. Ilia da hahawaneba: le, wele sia: mu. Na da ilima hahawane hamobeba: le, ilia fi idi da heda: mu. Amola Na da ilima hahawane hamobeba: le, eno fi dunu da ilima nodomu.
20 Ana awo adzakhalanso monga mmene analili kale, ndipo gulu lawo ndidzalikhazikitsa pamaso panga; ndidzalanga onse owazunza.
Musa: hemonega, Isala: ili fi da gasa bagade galu. Amo gasa bagade hou Na da ilima bu imunu, amola ilia da bu noga: le bugi dagoi ba: mu. Nowa da ili banenesisia, amo Na da banenesimu.
21 Mtsogoleri wawo adzakhala mmodzi mwa iwo. Wodzawalamulira adzachokera pakati pawo. Choncho ndidzawakokera kufupi ndi Ine ndipo iye adzandiyandikira. Ndani angalimbe mtima payekha kuyandikana nane popanda kuyitanidwa?” akutero Yehova.
22 “Choncho inu mudzakhala anthu anga, ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wanu.”
Ilia ouligisu hina bagade amola ea mano da ilia fidafa amoga misunu. Na da ema misa: ne sia: sea, e da Nama misunu. (Na da dunu amo Nama misa: ne hame hiougisia, e Nama misunu da hamedei). Ilia da Na fi dunu esalumu amola Na da ilia Gode esalebe ba: mu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
23 Taonani ukali wa Yehova wowomba ngati mphepo ya mkuntho. Mphepo ya namondwe ikuwomba pa mitu ya anthu oyipa.
24 Mkwiyo woopsa wa Yehova sudzachoka mpaka atakwaniritsa zolinga za mu mtima mwake. Mudzamvetsa zimenezi masiku akubwerawo.
Hina Gode Ea ougi hou da isula bobodobe bagadewane agoai gala. Ea ougi da isu bagade amo da wadela: i hamosu dunu ilia dialuma gadodili gegena ahoa. Amo da mae dagole, Hina Gode Ea hanai huluane hamoi dagosea fawane yolesimu. Hobea, eso enoga, Ea fi dunu da amo hou noga: le dawa: digimu.