< Yeremiya 3 >

1 “Ngati munthu asudzula mkazi wake ndipo mkaziyo nʼkuchoka nakakwatiwa ndi mwamuna wina, kodi mwamuna woyambayo angathe kumutenganso mkaziyo? Kodi atatero sindiye kuti dzikolo layipitsidwa kwambiri? Koma iwe Israeli wachita zadama ndi zibwenzi zambiri. Komabe bwerera kwa ine,” akutero Yehova.
Hina Gode da amane sia: sa, “Dunu afae da ea uda fisiagasea, amola amo uda da e fisili eno dunuma fisia, amo dunu da ea musa: lai uda bu lamu da hamedei. Amai galea, Isala: ili soge da wadela: lesi dagoi ba: mu. Be di, Isala: ili, da dunu bagohame ilima wadela: le fi dagoi. Amola, di da wali Nama sinidigimusa: dawa: lala.
2 “Tayangʼana ku zitunda zowuma. Kodi aliponso malo ena amene iwe sunachitepo zadama? Iwe unkakhala mʼmbali mwa njira kumadikira zibwenzi zako, ngati Mluya wobisalira anthu mʼchipululu. Inu mwayipitsa dziko ndi zadama zanu ndi ntchito zanu zoyipa.
Agolo da: iya gadodafa ba: ma! Soge huluane amoga di da hina: da: i bidi lasu uda ea hou defele hamosu. A: la: be dunu da hafoga: i sogega eno dunu famusa: ouligisa. Amo defele, di da logo bega: , dunu eno dima udigili golamusa: hogoi helelalebe ba: i. Dina: da: i bidi lasu hou da soge huluane wadela: lesi dagoi.
3 Nʼchifukwa chake Yehova wayimitsa mvula, ndipo mvula ya nthawi ya masika sinagwe. Komabe uli ndi maonekedwe a mkazi wachiwerewere; ndipo sukuchita manyazi ndi pangʼono pomwe.
Amaiba: le, Na da gibu logo ga: si dagoi. Amola woufo esoga Na da wou dabe logo ga: si dagoi. Di da dafawane hina: da: i bidi lasu uda defele ba: sa. Di da gogosiamu hame dawa:
4 Kodi iwe siposachedwa pomwepa pamene wanena kuti, ‘Abambo anga, Inu bwenzi langa la unyamata wanga,
Amola, wali di da Nama amane sia: sa, ‘Di da na ada. Di da na musa: manohadi eso amogainini wali nama asigi galu.
5 kodi mudzandikwiyira nthawi zonse? Kodi ukali wanu udzakhalabe mpaka muyaya?’ Umu ndimo mmene umayankhulira, koma umapitirizabe kuchita zoyipa monga momwe umathera.”
Di da nama ougi be eso huluane hame ougimu.’ Di amane sia: i, Isala: ili! Be dia hanaiga baligili wadela: i hou hamonanu.”
6 Pa nthawi ya Mfumu Yosiya Yehova anandiwuza kuti, “Kodi waona zomwe Israeli wosakhulupirika uja wachita? Anakwera pa phiri lililonse lalitali ndi kupita pa tsinde pa mtengo uliwonse wogudira kukapembedza. Choncho anachita za chiwerewere kumeneko.
Yousaia da Yuda soge amoma hina bagade esaloba, Hina Gode da nama amane sia: i, “Isala: ili da hohonosu uda defele esala. Dia da ea hamoi ba: bela: ? E da Na fisili, agolo bagade huluane amo da: iya amola golofoyei ifa huluane amo hagudu, e da hina: da: i bidi lasu uda ea hou defele hamonanu.
7 Ndinaganiza kuti atachita zonsezi, adzabwerera kwa Ine, koma sanabwerere, ndipo mlongo wake wosakhulupirika uja, Yuda, anaziona zimenezi.
Amo hamonanu, e da Nama bu sinidigimu, Na da dawa: iou. Be e da Nama hame sinidigi amola ea hohonosu dalusi Yuda amo hou huluane ba: i dagoi.
8 Anaona kuti ndinasudzula Israeli wosakhulupirikayo ndi kumupirikitsa chifukwa cha zigololo zake. Komabe Yuda mʼbale wake wosakhulupirika uja sanaope, nayenso anapita kukachita chigololo.
Isala: ili da Nama baligi fa: le, hina: da: i bidi lasu uda ea hou defele hamobeba: le, Na da uda fisiagasu hou defele e fisiagale, ga masa: ne asunasi. Yuda da amo hou amola ba: i dagoi. Be Yuda, Isala: ili ea hohonosu dalusi, e amola da mae beda: ne, hina: da: i bidi lasu uda ea hou defele hamoi.
9 Chiwerewere cha Israeli chinali chochititsa manyazi kotero kuti chinayipitsa dziko lonse. Anachita chigololo popembedza mafano a miyala ndi mitengo.
E da mae gogosiane, wadela: i uda lasu hou defele, igi amola ifa amoma nodone sia: ne gadosu.
10 Israeli atachita zonsezi, Yuda mʼbale wake wosakhulupirika uja sanabwerere kwa Ine ndi mtima wake wonse, koma mwachiphamaso chabe,” akutero Yehova.
Amolalu, Yuda (Isala: ili ea hohonosu dalusi) da Nama sinidigimusa: sia: i. Be e da ogogoi. E da moloidafa hou hamedafa dawa: i galu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
11 Yehova anandiwuza kuti, “Kusakhulupirika kwa Israeli nʼkochepa kuyerekeza ndi kusakhulupirika kwa Yuda.
Amalalu, Hina Gode da nama amane sia: i, “Dafawane! Isala: ili da Na yolesi dagoi. Be Yuda ea wadela: i hohonosu hou da Isala: ili ea hou baligi dagoi.”
12 Pita ukalalikire kumpoto uthenga wakuti, “‘Israeli wosakhulupirikawe, bwerera,’ akutero Yehova. ‘Sindidzakukalipira mpaka kalekale, pakuti ndine wachifundo,’ akutero Yehova. ‘Sindidzakukwiyira mpaka kalekale.
Hina Gode da nama amane sia: i, “Isala: ili fi ilima asili, amane sia: ma, ‘Hohonosu Isala: ili fi! Nama bu sinidigima. Na da asigi amola gogolema: ne olofosu hou dawa: Na da hame ougimu. Na da eso huluane ougili esalusu hame dawa:
13 Ungovomera kulakwa kwako kuti unawukira Yehova Mulungu wako. Vomera kuti unayendayenda kukapembedza milungu yachilendo pansi pa mtengo uliwonse wogudira, ndiponso kuti sunandimvere,’” akutero Yehova.
Be dia wadela: i hou amola Nama odoga: su hou amo fawane fofada: ma. Di da golofoyei ifa huluane amo hagudu, ga fi ogogosu ‘gode’ liligi ilima asigi hou olelei, amola Na sema hame nabasu. Amo fofada: nanu, Nama sinidigima. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.
14 “Bwererani, ana osakhulupirika, pakuti ndine mbuye wanu,” akutero Yehova. “Ndinakusankhani, mmodzimmodzi kuchokera ku mudzi uliwonse ndiponso awiriawiri kuchokera ku banja lililonse.
Hohonosu dunu fi! Sinidigima! Dilia da Na fi. Na da moilai huluane afae afae amoga dunu afae lale, amola fi huluane amoga dunu aduna lale, amola Saione Goumiga dili bu oule misunu.
15 Ndipo ndidzakupatsani abusa a pamtima panga amene adzakutsogolerani mwanzeru ndi mwaluntha.
Ouligisu dunu amo da Na sia: naba dunu, amo Na da dilima imunu. Amola ilia da dawa: iwane amola asigiwane dili ouligimu.
16 Masiku amenewo mukadzachulukana kwambiri mʼdzikomo, anthu sadzanenanso za ‘Bokosi la Chipangano la Yehova’ kapena kuliganizira. Sadzalikumbukiranso kapena kulifuna, ndipo sadzapanganso lina,” akutero Yehova.
Amasea, dilia idi da amo soge ganodini bagade heda: sea, dunu da Na Sema Gousa: su Gagili ea hou bu hame sia: mu. Ilia da amo bu hame dawa: mu, ilia da gogolemu. Bai ilia da hahawane esalebeba: le, Gousa: su Gagili ea fidisu hame hogomu. Amola ilia da eno Gousa: su Gagili hame hahamomu.
17 Nthawi imeneyo adzatcha Yerusalemu Mpando Waufumu wa Yehova, ndipo mitundu yonse ya anthu idzasonkhana mu Yerusalemu pamaso pa Yehova. Sadzawumiriranso kutsata mitima yawo yoyipa.
Bai amo eso da doaga: sea, ilia da Yelusaleme moilai bai bagade amoma dio ‘Hina Gode Ea Fisu’ asulimu. Amola fifi asi gala huluane da Nama nodone sia: ne gadomusa: gilisimu. Ilia da ilia wadela: i dogo asigi dawa: su ea hanaiga bu hame hamomu.
18 Masiku amenewo fuko la Yuda lidzaphatikizana ndi fuko la Israeli, onse pamodzi adzachokera ku dziko la kumpoto kupita ku dziko limene ndinapatsa makolo awo, kuti likhale cholowa.
Isala: ili fi da Yuda fi ilima gilisimu. Amola, elea fi dunu fifi asi gala gagoe (north) gala amoga mugululi asi da soge amo Na da dilia aowalalia ilima eso huluane gaguma: ne i, amoga bu sinidigimu.”
19 “Ine mwini ndinati, “‘Ndikanakonda bwanji kukukhazikani pakati pa ana anga ndikukupatsani dziko labwino kwambiri, cholowa chokongola kwambiri kuposa cha mitundu ina ya anthu.’ Ndinaganiza kuti mudzanditcha Ine ‘Atate’ ndi kuti simudzaleka kunditsata.
Hina Gode da amane sia: sa, “Isala: ili! Na da di Nagofe esaloma: ne hanai galu. Na da dima soge ida: iwane gala, eno osobo bagade soge baligi soge, amo dima imunusa: dawa: i galu. Di da Nama Ada dio asulimu, amola eso huluane bu Na hame fisimu, Na da dawa: i galu.
20 Koma monga mkazi wosakhulupirika amasiya mwamuna wake, momwemonso inu mwakhala osakhulupirika kwa Ine, inu fuko la Israeli,” akutero Yehova.
Be di da hohonosu uda defele, Nama hohonoi dagoi. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
21 Mawu akumveka pa magomo, Aisraeli akulira ndi kupempha chifundo chifukwa anatsata njira zoyipa ndi kuyiwala Yehova Mulungu wawo.
Agolo da: iya sia: bagade da naba. Amo da Isala: ili dunu, ilia da disa edegelala. Bai ilia da wadela: le hamosa esalu, amola ilia Hina Gode gogolei galu.
22 Inu mukuti, “Bwererani, anthu osakhulupirika; ndidzachiritsa kubwerera mʼmbuyo kwanu.” “Inde, tidzabwerera kwa Inu pakuti ndinu Yehova Mulungu wathu.
Dilia huluane da Hina Gode yolesi. Be bu sinidigima! E da dili uhinisimu amola dili bu didili hamoma: ne hamomu. Dilia da amane sia: sa, “Dafawane! Ninia da Hina Godema manebe goea. Bai E da ninia Gode.
23 Ndithu kupembedza pa magomo komanso kuchita maphwando pa mapiri zilibe phindu. Zoonadi chipulumutso cha Israeli chili mwa Yehova Mulungu wathu basi.
Ninia da agolo da: iya ogogosu ‘gode’ liligi ilima nodone sia: ne gadosu, be fidisu hame ba: i. Hina Gode, ninia Gode, Hifawane da fidisu dawa:
24 Kuyambira pa ubwana wathu milungu yochititsa manyazi ija yakhala ikutiwonongetsa phindu la ntchito za makolo athu, nkhosa ndi ngʼombe zawo, ana awo aamuna ndi aakazi.
Be ninia da Ba: iele (gogosiasu ‘gode’) ema sia: ne gadobeba: le, ninia sibi, bulamagau gilisisu, ninia dunu mano amola uda mano da fisi dagoi. Liligi huluane amo ninia aowalalia da lama: ne bagadewane hawa: hamosu, amo huluane da fisi dagoi ba: sa.
25 Tilekeni tigone pansi mwa manyazi, ndipo kunyozeka kwathu kutiphimbe. Paja tachimwira Yehova Mulungu wathu, ife pamodzi ndi makolo athu kuyambira nthawi ya ubwana wathu mpaka lero lino sitinamvere Yehova Mulungu wathu.”
Ninia da diasa: ili, ninia gogosiasu amoga dedeboi dagoi ba: mu da defea. Ninia amola ninia aowalalia da mae fisili, ninia Hina Godema wadela: lewane hamonanu. Ninia da Ea sia: hamedafa nabasu.”

< Yeremiya 3 >