< Yeremiya 27 >
1 Zedekiya mwana wa Yosiya, mfumu ya ku Yuda, atangoyamba kulamulira, Yehova anawuza Yeremiya kuti,
Sedegaia (Yousaia egefe) da Yuda fi hina bagade ouligibi hou lai. Amalalu, Hina Gode da nama,
2 “Tenga zingwe zomangira ndi mitengo ya goli ndipo uzimangirire mʼkhosi mwako.
na da bulamagau gadofo amola ifa bulufalegele, liligi lale, “youge” hamone, na galogoa amoga gasisalima: ne sia: i.
3 Tsono utumize uthenga kwa mafumu a Edomu, Mowabu, Amoni, Turo ndi Sidoni kudzera mwa amithenga amene abwera ku Yerusalemu kwa Zedekiya, mfumu ya Yuda.
Amalalu, Hina Gode da nama na da sia: amo Idome, Moua: be, A:mone, Daia amola Saidone amo ilia hina bagade ilima sia: adosima: ne sia: i. Amo fi dunu ilia sia: alofele iasu dunu ilia da hina bagade Sedegaia amo gousa: musa: , Yelusalemega misi esalu.
4 Uwapatse uthenga wokapereka kwa ambuye awo ndipo uwawuze kuti: Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti, ‘Mukawuze ambuye anu kuti:
Hina Gode Bagadedafa, Isala: ili fi ilia Gode, da nama na da ilia hina bagade sia: agoane olelema: ne sia: i,
5 Ndi mphamvu zanga ndi dzanja langa lamphamvu ndinalenga dziko lapansi ndi anthu ake onse pamodzi ndi nyama zili mʼmenemo, ndipo ndimalipereka kwa aliyense amene ndikufuna.
“Dilia hina bagade huluane ilima amane olelema! Na gasa bagade amoga Na da osobo bagade amola dunu fi amola ohe fi huluane osobo bagadega esala, amo huluane hamoi. Amola Na da Na gasa amo Na hanaiga fawane, eno dunuma iaha.
6 Tsopano ndidzapereka mayiko anu onse kwa mtumiki wanga Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni. Ndamupatsanso nyama zakuthengo zonse kuti zimutumikire.
Na da dilia soge huluane amo Na ilegei hawa: hamosu dunu Nebiuga: denesema imunu. Amola dunu huluane amola sigua ohe fi da ea hawa: hamosu hamomu.
7 Anthu a mitundu yonse adzamutumikira iyeyo, mwana wake ndi chidzukulu chake mpaka nthawi itakwana yoti dziko lake liwonongedwe. Pamenepo mitundu yambiri ndi mafumu amphamvu adzamugonjetsa.
Fifi asi gala huluane da ea udigili hawa: hamosu hamomu. Egefe amola e amola da amo fifi asi gala ouligilalu, amasea eso Na ilegei da doaga: sea, ea fi amola da dafamu. Amasea, eno gasa bagade fi amola gasa bagade hina bagade, ilia da ea fi ouligimu.
8 “‘Koma ngati anthu a mtundu wina uliwonse kapena ufumu wina uliwonse adzakana kutumikira Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni kapena kusenza goli lake, Ine ndidzalanga mtundu umenewo ndi lupanga, ndi njala ndi mliri, akutero Yehova, mpaka nditawapereka mʼmanja mwake kotheratu.
Be nowa fifi asi gala o hina bagade ea fi da ea ouligibi higale, hame nabasea, Na da amo fi gegesu amola ha: amola olo amoga se imunu. Amasea, Na da logo doasimuba: le, Nebiuga: denese da amo fi wadela: lesimu fawane.
9 Choncho musamvere aneneri anu, owombeza anu, otanthauza maloto anu, amawula anu kapena amatsenga anu akamakuwuzani kuti, ‘Simudzatumikira mfumu ya ku Babuloni.’
Dilia balofede dunu o nowa da fa: no misunu hou dawa: , hi fawane sia: sa, (e da simasia ba: sa o bogoi a: silibu amoma sia: sa o wamuni dawa: su hou amo ganodini ba: sa amola ogogole sia: sa) amo huluane mae nabima. Ilia huluane da dilia Ba: bilone hina bagade ea sia: mae nabima: ne sia: sa.
10 Iwo akukuloserani zabodza kotero kuti adani adzakuchotsani mʼdziko lanu nʼkupita nanu ku dziko lakutali. Ndidzakupirikitsani ndi kukuwonongani kotheratu.
Ilia da dilima ogogosa. Ilia hamobeba: le, dilia da dilia soge yolesili, soge sedagaga mugululi asi dagoi ba: mu. Na da dili ga sefasimu, amola dilia da wadela: lesi dagoi ba: mu.
11 Koma ngati mtundu wina uliwonse udzagonjera mfumu ya ku Babuloni ndi kuyitumukira, ndidzawusiya kuti ukhale mʼdziko lake kuti uzilima ndi kukhalamo, akutero Yehova.’”
Be nowa fi da Ba: bilone hina bagade ea sia: nabasea amola ea hawa: hamosea, Na da amo fi ilia sogedafaga esaloma: ne amola ha: i manu bugima: ne, logo doasimu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”
12 Uthenga womwewu ndinawuzanso Hezekiya mfumu ya Yuda. Ndinati, “Gonjerani mfumu ya ku Babuloni. Itumikireni iyoyo pamodzi ndi anthu ake ndipo mudzakhala ndi moyo.
Na da Yuda hina bagade Sedegaia ema defele sia: i, amane, “Ba: bilone hina bagade ea sia: nabawane hamoma! Dilia da ea amola ea fi dunu ilia hawa: hamosu hamosea, dilia da esalumu.
13 Nanga inu ndi anthu anu, muferenji ndi lupanga, ndi njala, ndi mliri, zimene Yehova waopsezera mtundu wina uliwonse umene sudzatumikira mfumu ya ku Babuloni?
Abuliba: le di amola dia fi dunu da gegesuga o ha: ga o oloiga bogoma: bela: ? Hina Gode da sia: i dagoi. Nowa fi da Ba: bilone hina bagade ea sia: hame nabasea da agoaiwane bogogia: mu.
14 Musamvere mawu a aneneri akamakuwuzani kuti, ‘Simudzatumikira mfumu ya ku Babuloni,’ chifukwa zimene akukuloseranizo nʼzabodza.
Balofede dunu da dima Ba: bilone hina bagade da mae hasalasima: ne gegema: ne sia: sa, amo mae nabima! Ilia da dilima ogogosa.
15 Sindinawatume ngakhale iwo akulosera mʼdzina langa. Nʼchifukwa chake, ndidzakupirikitsani ndipo mudzawonongeka kotheratu, inu pamodzi ndi aneneri amene akunenera zabodza kwa inu.”
Hina Gode Hisu da amo dunu ilia da Ea Dioba: le ogogosa, amo hamedafa asunasi sia: i. Amaiba: le, E da dili gadili sefasili, dili amola ogogosu balofede dunu da gilisili, medole legei dagoi ba: mu.”
16 Kenaka ndinawuza ansembe pamodzi ndi anthu ena onse kuti, “Yehova akuti: Musamvere aneneri amene akumanena kuti, ‘Posachedwapa ziwiya za mʼNyumba ya Yehova zibwera kuchokera ku Babuloni.’ Iwowo akunenera zabodza kwa inu.
Amalalu, na da gobele salasu amola balofede dunu ilima Hina Gode Ea sia: i liligi olelei, amane, “Ogogosu balofede dunu da Debolo liligi ida: iwane da hedolo Ba: bilone sogeganini bu Yelusaleme amoga gaguli misi dagoi ba: mu. Be ilia sia: mae nabima!
17 Musawamvere. Tumikirani mfumu ya ku Babuloni, ndipo mudzakhala ndi moyo. Mzindawu usandukirenji bwinja?
Ba: bilone hina bagade ea sia: nabawane hamoma. Amasea, dilia da esalumu. Yelusaleme da abuliba: le wadela: lesi isu gegedole liligisu agoane ba: ma: bela: ?
18 Ngati iwo ndi aneneri ndipo ali ndi mawu a Yehova, apempheretu kwa Yehova Wamphamvuzonse kuti ziwiya zimene zatsala mʼNyumba ya Yehova ndi mʼnyumba ya mfumu ya Yuda ndiponso mu Yerusalemu zisatengedwe kupita ku Babuloni.
Ilia da dafawane Na balofede dunu esala ganiaba, amola ilia da Na sia: lai dagoi ganiaba, ilia da Na, Hina Gode Bagadedafa, amoma Na da liligi ida: iwane gala Debolo diasu amola hina bagade diasu ganodini hame wamolai gala: loba, amo Ba: bilone dunu Ba: bilone sogega mae gaguli misa: ne logo hedofama: ne, Nama agoane adole ba: mu da defea.”
19 Pakuti Yehova akunena za zipilala, za mbiya ya madzi, maphaka ndi ziwiya zina zimene zatsala mu Yerusalemu.
20 Izi ndi zimene Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni sanatenge pamene anatenga ukapolo Yekoniya mwana wa Yehoyakimu mfumu ya Yuda kupita ku Babuloni kuchokera ku Yerusalemu, pamodzi ndi anthu olemekezeka a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu.
(Ba: bilone hina bagade Nebiuga: denese da Yuda hina bagade Yehoiagini (Yihoiagimi egefe) amola Yuda amola Yelusaleme ouligisu dunu amo Ba: bilone sogega afugili oule asiba: le, e da liligi bagohame gaguli asi. Be e da balase duni bugi amola balase ofodo bagade amola balase hosiga hiougi ‘gaguli fula ahoasu’ amola eno Debolo liligi ida: iwane gala, hame gaguli asi).
21 Inde, Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, akunena za zinthu zimene zinatsala mʼNyumba ya Yehova ndi mʼnyumba ya mfumu ya Yuda ndi mu Yerusalemu kuti,
“Na da Hina Gode Bagadedafa, Isala: ili fi ilia Gode! Na sia: nabima! Liligi ida: iwane gala Debolo diasu amola Yelusaleme hina bagade ea diasu ganodini diala,
22 ‘Zidzatengedwa kupita ku Babuloni ndipo zidzakhala kumeneko mpaka tsiku limene ndidzawakumbukirenso,’ akutero Yehova. ‘Pamenepo ndidzazitenganso ndi kuzibwezanso ku malo ano.’”
amo huluane Ba: bilone hina bagade da Ba: bilone sogega gaguli masunu. Amogawi, ilia da dialumu. Amalalu, Na da amo bu dawa: sea, Na da amo liligi bu Yelusalemega dialoma: ne bu gaguli misunu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.”