< Yeremiya 25 >
1 Yehova anayankhula ndi Yeremiya za anthu onse a ku Yuda mʼchaka chachinayi cha ufumu wa Yehoyakimu mwana wa Yosiya mfumu ya ku Yuda, chimene chinali chaka choyamba cha ufumu wa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni.
Yuda hina bagade Yihoiagimi (Yousaia egefe) amo ea ouligibi ode biyadu amoga, Hina Gode da Yuda dunu ilia hou olelema: ne, nama sia: i. (Amo odega, hina bagade Nebiuga: denese da degabo Ba: bilone soge ouligisu lai).
2 Choncho mneneri Yeremiya anawuza anthu onse a ku Yuda pamodzi ndi onse amene amakhala mu Yerusalemu kuti:
Na da Yuda fi dunu amola Yelusaleme fi dunu ilima amane sia: i,
3 Kwa zaka 23, kuyambira chaka cha 13 cha ufumu wa Yosiya mwana wa Amoni mfumu ya ku Yuda mpaka lero lino, Yehova wakhala akundipatsa mauthenga ake ndipo ine ndakhala ndikuyankhula ndi inu kawirikawiri, koma inu simunamvere.
“Hina Gode da ode 23amoga (amo da A: mone egefe Yousaia ea ode 13Yuda soge ouligibiga, amogainini, wali eso amoga doaga: i), nama sia: su. Amola na da moloidafa, amo sia: huluanedafa dilima alofele iasu. Be dilia da amo sia: hame nabi.
4 Ndipo ngakhale Yehova kawirikawiri wakhala akukutumizirani atumiki ake onse, aneneri, inuyo simunamvere kapena kutchera khutu.
Hina Gode da Ea hawa: hamosu dunu, amo balofede dunu dilima asula ahoasu. Be dilia da ili amola hame nabi.
5 Aneneriwo ankanena kuti, “Ngati aliyense wa inu abwerere, kusiya njira zake zoyipa ndi machitidwe ake oyipa, ndiye kuti mudzakhala mʼdziko limene Yehova anapereka kwa makolo anu kwamuyaya.
Amo balofede dunu da dilia soge amo Hina Gode da dilia aowalalia eso huluane gaguma: ne ilima i, amo ganodini hahawane esalalaloma: ne, dilia wadela: i esalusu amola wadela: i hawa: hamonanebe fisima: ne sia: i.
6 Musatsatire milungu ina nʼkuyitumikira ndi kuyipembedza. Musapute mkwiyo wanga ndi mafano amene mwapanga ndi manja anu. Mukatero Ine sindidzakuwonongani.
Ilia da dilia Hina Gode ougima: ne, eno ogogosu ‘gode’ ilima mae nodone sia: ne gadoma: ne, amola mae hawa: hamoma: ne sia: i. Dilia da Hina Gode Ea sia: nabawane hamoi ganiaba, E da dilima se hame ia: noba.
7 “Koma inu simunandimvere,” akutero Yehova, “ndipo munaputa mkwiyo wanga ndi mafano amene munapanga ndi manja anu. Choncho munadziwononga nokha.”
Be Hina Gode Hisu da dilia Ea sia: hame nabi sia: i. Be dilia da E ougima: ne, loboga hamoi ogogosu ‘gode’ ilima nodone sia: ne gadosu. Amaiba: le, dilila: da amo se iasu dilima doaga: ma: ne, logo fodoi dagoi.
8 Nʼchifukwa chake Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Chifukwa simunamvere mawu anga,
Amaiba: le, dilia da Hina Gode Ea sia: hame nababeba: le, E da amane sia: sa,
9 ndidzayitana mafuko onse akumpoto, pamodzi ndi mtumiki wanga Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni,” akutero Yehova, “ndipo adzathira nkhondo dziko lino ndi anthu ake pamodzi ndi mitundu yonse ya anthu ozungulira dzikoli. Ndidzawawononga kwathunthu ndi kuwasandutsa chinthu chochititsa mantha ndi chonyozeka, mpaka muyaya.
‘Na da fifi asi gala gagoe (north) amogawi esala, amola Na hawa: hamosu dunu amo Ba: bilone hina bagade Nebiuga: denese, ilima misa: ne sia: mu. Na da Yuda fi amola ea na: iyado fi huluane eso huluane mugului dagoi dialoma: ne, wadela: lesimu. Eno dunu da amo ba: sea, beda: iwane fofogadigimu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi.
10 Ndidzathetsa mfuwu wachimwemwe ndi wachisangalalo, mawu a mkwati ndi mkwatibwi, phokoso la mphero ndi kuwala kwa nyale.
Ilia da wali hahawane wele sia: sa, amola uda lasu lolo nabe amo ganodini hahawane sia: sa. Be amo ouiya: ma: ne, Na da dagolesimu. Ilia gamali ulagima: ne, ilia da susuligi hame ba: mu amola ilia gagoma ebelei dagoi ba: mu.
11 Dziko lonse lidzakhala bwinja ndi chipululu, ndipo mitundu ina idzatumikira mfumu ya ku Babuloni kwa 70.
Soge huluane da eno dunu fofogadigima: ne, wadela: lesidafa ba: mu. Amola na: iyado fi huluane da Ba: bilone hina bagade ea udigili hawa: hamosu ode 70 amoga hamomu.
12 “Koma zaka 70 zikadzatha, ndidzalanga mfumu ya ku Babuloni pamodzi ndi anthu ake, chifukwa cha zolakwa zawo,” akutero Yehova, “ndipo dziko lawo lidzakhala chipululu mpaka muyaya.
Amalalu, Na da Ba: bilone fi amola ilia hina bagade, ilia wadela: i hou dabema: ne, ilima se imunu. Na da ilia soge eso huluane mugului dagoi dialoma: ne, wadela: lesimu.
13 Ndidzachita zinthu zonse zimene ndinayankhula zotsutsa dzikolo, zonse zimene zalembedwa mʼbuku lino, ndiponso zonse zimene Yeremiya analosera zotsutsa anthu amenewa.
Na da Yelemaia ea lafidili amo fifi asi gala wadela: lesimu sia: i, amola e da amo wadela: su hou amo buga ganodini dedei. Amo wadela: su hou huluane Na da Ba: bilone fi ilima iasimu.
14 Iwo eni adzakhala akapolo a anthu a mitundu yochuluka ndi mafumu amphamvu. Ndidzawabwezera molingana ndi zochita zawo ndi ntchito za manja awo.”
Ba: bilone fi dunu da wadela: le hamobeba: le, Na da ilima dabema: ne se imunu. Amola fifi asi gala bagohame, amola hina bagade ilia da gasa fili, Ba: bilone fi dunu ilia udigili hawa: hamoma: ne sia: mu.’”
15 Yehova, Mulungu wa Israeli, anandiwuza kuti, “Tenga chikho ichi chodzaza ndi vinyo wa ukali wanga, ndipo ukamwetse anthu a mitundu yonse kumene ndikukutuma.
Hina Gode, Isala: ili fi ilia Gode, da nama amane sia: i, “Waini nasu faigelei amo Na ougiga nabai gala ba: ma! Amo gaguli asili, fifi asi gala amoga Na da di asula ahoa, ilima ilia amo waini nasu faigelei ganodini gala moma: ne sia: ma.
16 Akadzamwa adzayamba kudzandira ndi kuchita misala chifukwa cha nkhondo imene ndikuyitumiza pakati pawo.”
Ilia da amo nasea, feloale doula masunu. Bai Na da gegesu bagade ilima se ima: ne iasisa.”
17 Choncho ine ndinatenga chikhocho mʼdzanja la Yehova ndipo ndinamwetsa mitundu yonse ya anthu kumene Iye ananditumako:
Amaiba: le, na da faigelei Hina Gode Ea loboga lale, fifi asi gala amoga Hina Gode da na asunasi, ilima ianu, moma: ne sia: i.
18 Anandituma ku Yerusalemu ndi ku mizinda ya Yuda, kwa mafumu ake ndi nduna zake kuti ndikawasandutse ngati bwinja ndi chinthu chochititsa mantha ndi chonyozeka ndiponso chotembereredwa, monga mmene alili lero lino.
Na sia: beba: le, Yelusaleme fi amola Yuda moilai huluane ilia fi amola hina bagade ilia amola ouligisu dunu huluane da amoga mai. Bai Hina Gode da ilia soge wadela: lesili, bu hafoga: i soge agoane hamomusa: dawa: ma: ne. Amola ilia soge da beda: iwane fofogadigisu liligi ba: ma: ne. Amola dunu da ilia dioba: le, gagabusu aligimu ilegema: ne. Amola wali eso ilia mae fisili, ilia dioba: le gagabusu aligima: ne ilegesa.
19 Ananditumanso kwa Farao, mfumu ya ku Igupto, kwa atumiki ake, nduna zake ndi kwa anthu ake onse,
Eno fi amola dunu da amo faigeleiga wadela: su waini hano moma: ne sia: i, amo ilia dio da hagudu dedei, Idibidi hina bagade amola ea eagene ouligisu dunu amola fi ouligisu dunu; Idibidi fi dunu huluane amola ga fi huluane Idibidi soge ganodini esala; Ase soge hina bagade huluane; Filisidini moilai bai bagade huluane (A: siegelone, Gasa, Egelone amola A: siedode la: idi hame mugului) ilia hina bagade huluane; Idome amola Moua: be amola A: mone soge ilia fi dunu huluane; Daia amola Saidone moilai bai bagade elea hina bagade; Medidela: inia bega: soge huluane ilia hina bagade huluane; Dida: ne amola Dima amola Base moilai bai bagade huluane; Dunu huluane amo da ilia dialuma hinabo dunumuni dadamusa; Ala: ibia soge ea hina bagade huluane; Hafoga: i soge fi huluane ilia hina bagade huluane; Similai amola Ila: me amola Midia fi ilia hina bagade huluane; Amola gagoe (north) soge gadenene amola sedaga, ilia hina bagade huluane. Osobo bagade fifi asi gala huluanedafa da amo waini (Hina Gode Ea ougi) manusa: gala. Amasea, fa: nodafa, Ba: bilone hina bagade da amo faigeleiga waini hano manu.
20 ndi kwa anthu ena onse a mitundu yachilendo; mafumu onse a ku Uzi; mafumu onse a Afilisti, a ku Asikeloni, ku Gaza, ku Ekroni ndiponso kwa anthu a ku chigwa chotsala cha Asidodi;
21 Edomu, Mowabu ndi Amoni.
22 Ananditumanso kwa mafumu onse a ku Turo ndi ku Sidoni; kwa mafumu a kutsidya la nyanja;
23 ku Dedani, ku Tema, ku Buzi ndi kwa onse ometa chamʼmbali.
24 Ananditumanso kwa mafumu onse a ku Arabiya ndi mafumu onse a anthu achilendo amene amakhala mʼchipululu.
25 Anandituma kwa mafumu onse a ku Zimuri, Elamu ndi Mediya;
26 ndiponso kwa mafumu onse a kumpoto, akufupi ndi kutali omwe, mafumu onse a dziko lapansi. Ndipo potsiriza pake, idzamwenso ndi mfumu Sesaki.
27 “Ndipo uwawuze kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti: Imwani, ledzerani ndipo musanze, mugwe osadzukanso chifukwa cha nkhondo imene ndikutumiza pakati panu.’
Amalalu, Hina Gode da nama amane sia: i, “Dunu huluane ilima amane sia: ma! Na, Hina Gode Bagadedafa, da ilima gasa bagadewane ilia da amo waini hano moma: ne sia: sa. Ilia da amo nanu, feloale, isomu. Amasea, ilia da dafane, bu wa: legadomu gogolemu. Bai Na da gegesu bagade ilima iasisa.
28 Koma ngati akana kutenga chikhocho mʼdzanja lako ndi kumwa, uwawuze kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse akuti: Muyenera kumwa ndithu!’”
Be ilia da higa: iba: le, amo waini hano faigeleiga moma: ne, dia loboga hame gaguli nasea, ilima amane olelema, ‘Hina Gode Bagadedafa da dili moma: ne gasa bagade sia: sa.’
29 Taonani, tsopano ndiyamba kulanga mzinda uno umene umadziwika ndi dzina langa. Kodi inu muganiza kuti simudzalangidwa? Ayi, simudzapulumuka chifukwa ndikutumiza nkhondo pa onse okhala pa dziko lapansi, akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Na da Na wadela: lesimu hawa: hamosu amo Na moilai bai bagadedafa (Yelusaleme) amo ganodini muni hemomu. Yelusaleme fi ilia da se iasu hame lamu dawa: lala. Be ilia da se iasu ba: mu. Bai Na da osobo bagade dunu huluane ilima gegesu bagade iasimu. Na, Hina Gode Bagadedafa, da sia: i dagoi.
30 “Tsopano iwe nenera mawu owatsutsa ndipo uwawuze kuti, “‘Yehova adzabangula kumwamba; mawu ake adzamveka ngati bingu kuchokera ku malo ake opatulika. Adzabangula mwamphamvu kukalipira dziko lake. Iye adzafuwula ngati anthu oponda mphesa, kukalipira onse amene akukhala pa dziko lapansi.
Di Yelemaia! Na sia: huluane alofele sia: ma! Yuda fi ilima amane olelema, ‘Hina Gode da Hebene gado amoga humu, amola gugelebe agoane sia: mu. E da Ea fi ilima humu. E da dunu da waini fage amo osa: gisia wele sia: sa, amo defele wele sia: mu, amola dunu huluane osobo bagadega esala da Ea wele sia: su nabimu.
31 Phokoso lalikulu lidzamveka mpaka kumalekezero a dziko lonse lapansi, chifukwa Yehova adzazenga mlandu anthu a mitundu yonse; adzaweruza mtundu wonse wa anthu ndipo oyipa adzawapha ndi lupanga,’” akutero Yehova.
Amola amo wele sia: su da osobo bagade bega: bega: nabimu. Hina Gode da fifi asi gala ilima fofada: mu gala. E da dunu huluane ilima fofada: musa: Ema oule misunu, amola E da wadela: i hamosu dunu medole legemusa: sia: mu. Hina Gode da sia: i dagoi.’”
32 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Taonani! Mavuto akuti akachoka pa mtundu wina akukagwa pa mtundu wina; mphepo ya mkuntho ikuyambira ku malekezero a dziko.”
Hina Gode Bagadedafa da wadela: su amo da fifi asi gala afae ilima doaga: sea, fi eno fi eno ilima masunu, amane sia: sa. Amola fedege agoane, osobo bagade bega: bega: , isula bobodole bagadedafa gilisisa.
33 Pa tsiku limenelo, onse ophedwa ndi Yehova adzangoti mbwee ponseponse, pa dziko lonse lapansi. Palibe amene adzawalire kapena kusonkhanitsa mitemboyo kuti ikayikidwe mʼmanda, koma idzakhala mbwee ngati ndowe.
Amo esoga, dunu amo da Hina Gode da medole legei, amo ilia bogoi da: i hodo da osobo bagade la: idi asili eno la: idi ahoa, amoga afagogoi dialebe ba: mu. Dunu eno da ilima hame asigiba: le, hame didigia: mu. Ilia bogoi da: i hodo da hame uli dogonesi ba: mu. Be ilia da iga lelegela heda: i agoane osoboga dialebe ba: mu.
34 Khetsani misozi ndi kufuwula mwamphamvu, abusa inu; gubudukani pa fumbi, inu atsogoleri a nkhosa. Pakuti nthawi yanu yophedwa yafika; mudzagwa ndi kuphwanyika ngati mbiya yabwino kwambiri.
Dilia ouligisu dunu! Dilia Na sibi ouligisu dunu! Ha: giwane dima! Didigia: ma amola gulu da: iya bebesoma! Dilia medole legesu eso da doaga: i dagoi, amola dilia da sibi gawali agoane, medole legei dagoi ba: mu.
35 Abusa adzasowa kothawira, atsogoleri a nkhosa adzasowa malo opulumukira.
Dilia da hobeale masunu logo hame ba: mu.
36 Imvani kulira kwa abusa, atsogoleri a nkhosa akulira, chifukwa Yehova akuwononga msipu wawo.
37 Makola awo a nkhosa amene anali pamtendere adzasanduka bwinja chifukwa cha mkwiyo woopsa wa Yehova.
Dilia da gogonomasa amola digini wele sia: sa. Bai Hina Gode da ougiba: le, dilia fi wadela: lesi dagoi amola dilia musa: olofosu soge amo wadela: lesilalu asi.
38 Ngati mkango, Yehova wasiya phanga lake, pakuti dziko lawo lasanduka chipululu chifukwa cha nkhondo ya owazunza ndiponso chifukwa cha mkwiyo woopsa wa Yehova.
Laione wa: me da ea magufu gelabo yolesisa, amo defele Hina Gode da Ea fi dunu yolesi dagoi. Gegesu ea se bagade nabasu hou da soge huluane wadela: lesili, hafoga: i soge agoane hamoi dagoi.