< Yeremiya 23 >
1 “Tsoka kwa abusa amene akuwononga ndi kubalalitsa nkhosa za pabusa panga!” akutero Yehova.
Kaie saringnaw a pânae hmuen koe e kâkayeisakkung tukhoumnaw teh lungmathoe hanelah ao awh, telah BAWIPA ni a dei.
2 Nʼchifukwa chake Yehova, Mulungu wa Israeli, ponena za abusa amene akuweta anthu anga akuti, “Mwabalalitsa ndi kumwaza nkhosa zanga. Komanso simunazisamale bwino. Choncho ndidzakulangani chifukwa cha machimo anu,” akutero Yehova.
Hatdawkvah, BAWIPA Isarel Cathut ni ka taminaw ka khoum e tukhoumnaw kong dawkvah, hettelah a dei, ka saringhu hah na kâkayei sak awh, na pâlei awh teh, na khenyawn awh hoeh. Khenhaw! na sak awh e yonnae kecu dawk na tho sin han telah BAWIPA ni a dei.
3 “Pambuyo pake Ine mwini wakene ndidzasonkhanitsa nkhosa zanga zotsala, kuzichotsa ku mayiko onse kumene ndinazibalalitsira ndi kuzibweretsanso ku msipu wawo. Kumeneko zidzaswana ndi kuchulukana.
Ka saringhu, kacawirae ka saringhu hah ka pâlei ram dawk hoi ka pâkhueng vaiteh, ngai ka tho poung e a paw ka paw e lah awm awh vaiteh, a pungdaw awh han.
4 Ndidzazipatsa abusa amene adzaziweta, ndipo sizidzaopanso kapena kuchita mantha, ndipo palibe imene idzasochera,” akutero Yehova.
Ahnimouh ka kawk hane tukhoumnaw hah ka pouk pouh han, taki puennae awm hoeh toung vaiteh, kângairu awh mahoeh toe. Kahmat e hai awm mahoeh toe, telah BAWIPA ni a dei.
5 Yehova akuti, “Masiku akubwera, pamene ndidzaphukitsira Davide Nthambi yowongoka. Imeneyi ndiye mfumu imene idzalamulira mwanzeru, mwachilungamo ndi mosakondera mʼdziko.
Khenhaw! Devit hanelah kalan e cakang ka kangdue sak hane atueng hah a pha tawmlei toe, telah BAWIPA ni a dei. Siangpahrang buet touh ni a uk vaiteh, a hmacawn han, talai van lawkcengnae hoi lannae a kuep sak han.
6 Pa masiku a ulamuliro wake Yuda adzapulumuka ndipo Israeli adzakhala pamtendere. Dzina limene adzamutcha ndi ili: Yehova ndiye Chilungamo Chathu.
Ahnimae tueng nah Judah teh, rungngang lah ao vaiteh, Isarel teh karoumcalah ao han. Hahoi, a min teh BAWIPA teh kaimae lannae tie lah ao han.
7 Choncho, masiku akubwera,” akutero Yehova, “pamene anthu sadzanenanso polumbira kuti, ‘Pali Yehova wamoyo, amene anatulutsa Aisraeli ku Igupto,’
Hatdawkvah, khenhaw! atueng a pha tawmlei, BAWIPA ni ati. Isarelnaw Izip ram hoi ka tâcawtkhaikhung BAWIPA teh a hring e patetlah tet awh mahoeh toe.
8 koma adzanena kuti, ‘Pali Yehova wamoyo, amene anatulutsa zidzukulu za Israeli ku dziko lakumpoto ndi ku mayiko konse kumene anawabalalitsira.’ Ndipo iwo adzawabweretsa ku dziko lawolawo.”
Tung lae ram hoi a pâleinae ramnaw thung hoi Isarel imthung a tâcokhai teh, bout kabankhaikung BAWIPA a hring e patetlah tet awh vaiteh amamae ram dawk khosak awh han.
9 Kunena za aneneri awa: Mtima wanga wasweka; mʼnkhongono mwati zii. Ndakhala ngati munthu woledzera, ngati munthu amene wasokonezeka ndi vinyo, chifukwa cha Yehova ndi mawu ake opatulika.
Profetnaw kecu dawk ka lungthin thung vah a rek. Ka hrunaw hai koung kâhuet, yamu ka parui e tami patetlah doeh ka o, BAWIPA hoi kathounge a lawk kecu dawk yamu ni rektap e patetlah ka o.
10 Dziko ladzaza ndi anthu achigololo; lili pansi pa matemberero. Dziko lasanduka chipululu ndipo msipu wawuma. Aneneri akuchita zoyipa ndipo akugwiritsa ntchito mphamvu zawo molakwika.
Bangkongtetpawiteh, ram teh uicuknae hoi a kawi teh, thoebo e kecu dawk ram ni a khui awh. Kahrawng hmuen kahawi pueng koung a ka toe. A hringnae lamthung hah a payon teh, a thaonae hai lan hoeh.
11 “Mneneri ngakhale wansembe onse sapembedza Yehova. Amachita zoyipa ngakhale mʼnyumba yanga,” akutero Yehova.
Bangkongtetpawiteh, profetnaw hoi vaihmanaw ni CAthut hah bang lah noutna awh hoeh. Hawihoehnae naw hah ka imthung vah ka hmu telah BAWIPA ni a dei.
12 “Nʼchifukwa chake njira zawo zidzakhala zoterera; adzawapirikitsira ku mdima ndipo adzagwera kumeneko. Adzaona zosaona mʼnthawi ya chilango chawo,” akutero Yehova.
Hatdawkvah, a lamthung pueng teh khohmo vah ka pâhnan e lamthung patetlah ao han. Hote lamthung dawk pâlei e lah awm vaiteh, ka pâhnan e dawk koung a rawp awh han. Bangkongtetpawiteh, ahnimouh lathueng vah kathoute reknae hah ka pha sak han, telah BAWIPA ni a dei.
13 “Pakati pa aneneri a ku Samariya ndinaona chonyansa ichi: Ankanenera mʼdzina la Baala ndipo anasocheretsa anthu anga, Aisraeli.
Samaria profetnaw dawkvah, panuettho e hah ka hmu, Baal kampang lahoi lawk hah a dei awh teh, Isarelnaw hah lampaihei lah a ceikhai awh.
14 Ndipo pakati pa aneneri a ku Yerusalemu ndaonapo chinthu choopsa kwambiri: amachita chigololo, amanena bodza ndipo amalimbitsa mtima anthu ochita zoyipa. Choncho palibe amene amasiya zoyipa zake. Kwa Ine anthu onsewa ali ngati a ku Sodomu ndi Gomora.”
Jerusalem e profetnaw dawk hai takitho poung e hno hah ka hmu, a uicuknae dawk a luen awh teh, laithoe hoi kho a sak awh. Apihai a thoenae dawk hoi a ban awh hoeh nahanelah, yonnae kasaknaw e kut hah a thao sak awh. Kai hanelah teh Sodom khonaw patetlah doeh ao. A kho thung e taminaw pueng hai Gomorrah kho e taminaw hoi a kâvan awh.
15 Choncho ponena za aneneriwa Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ndidzawadyetsa zakudya zowawa ndi kuwamwetsa madzi a ndulu, chifukwa uchimo umene wafalikira mʼdziko lonse ndi wochokera kwa aneneri a ku Yerusalemuwa.”
Hatdawkvah, profetnaw kong dawk ransahu BAWIPA ni hettelah a dei, khenhaw! amamae cai kakhat hoi ka kawk vaiteh, kakhat e tui hah ka nei sak han. Bangkongtetpawiteh, Jerusalem e profetnaw kecu dawk ram thung pueng dawk Cathut taki teh bari hoeh nae hah a tâco.
16 Koma Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Musamvere zimene aneneri amenewa akulosera kwa inu; zomwe aloserazo nʼzachabechabe. Iwo akungoyankhula za masomphenya a mʼmitima mwawo basi, osati zochokera kwa Yehova.
Ransahu BAWIPA ni hettelah a dei, profet ni nangmouh koe a dei awh e lawk hah ngai pouh hanh awh. Bang hoeh e hah na cangkhai awh. BAWIPA e pahni dawk hoi ka tâcawt e nahoeh niteh, amamae lungpouk e hah ouk a dei awh.
17 Iwo amapita ndi kumakawuza amene amandinyoza Ine kuti, ‘zinthu zidzakuyenderani bwino.’ Kwa iwo amene amawumirira kutsata zofuna za mitima yawo amakawawuza kuti, ‘palibe choyipa chimene chidzakugwereni.’”
Kai na kadudamnaw koevah, roumnae ka hmu awh han, BAWIPA ni ati, telah pout laipalah rek a dei awh. Amamae lungthin thung a ngaihawi e patetlah kacetnaw koevah, thoenae nangmae lathueng vah phat mahoeh telah ati awh.
18 Ine ndikuti, “Koma ndani wa iwo amene anakhalapo mu msonkhano wa Yehova? Ndani anaonapo kapena kumvapo mawu ake? Ndani mwa iwo analabadirako za mawu ake ndi kuwamvera?
Bangkongtetpawiteh, BAWIPA khokhangnae hah apimaw ka hrawk boi, a lawk dawk hoi kapanuekkung apimaw kaawm. Hoeh pawiteh, a lawk teh lawkpui lah pouk teh apinimaw a thai boi vaw.
19 Taonani ukali wa Yehova uli ngati chimphepo chamkuntho, inde ngati namondwe. Ndipo adzakantha mitu ya anthu oyipa.
Khenhaw! ka patawpoung katang e, bongparui BAWIPA lungkhueknae bongparui hah a tâco toe, tamikathoutnaw e lû dawk ka patawpoung e lah a bo han.
20 Mkwiyo wa Yehova sudzaleka mpaka atachita zonse zimene anatsimikiza mu mtima mwake. Mudzazizindikira bwino zimenezi masiku akubwerawa.”
BAWIPA lungkhueknae teh ban mahoeh, a lungthung a noe tangcoung e teh, a kuep sak vaiteh, a cum hoehroukrak ban mahoeh toe. A hnuktengpoung e hnin ka kuepcalah na panue awh han doeh.
21 Yehova anati, “Ine sindinatume aneneri amenewa, komabe iwo athamanga uku ndi uku kulalikira uthenga wawo; Ine sindinawayankhule, komabe iwo ananenera.
Profet patoun ngai laipalah a yawng awh, ahnimouh koe ka dei pouh hoeh hai lawk a dei awh.
22 Iwo akanakhala pa msonkhano wanga ndiye kuti akanamayankhula mawu anga kwa anthu anga. Komanso bwenzi atawachotsa anthu anga mʼnjira zawo zoyipa kuti aleke machimo awo.”
Kaie khokhannae dawk awm van pawiteh, ka lawk heh ka taminaw koe pâpho van vaiteh, a yonnae dawk hoi pankângai awh han ei.
23 Yehova akuti, “Kodi ndimakhala Mulungu pokhapokha ndikakhala pafupi, ndiye sindine Mulungu?
Kahlat lah kaawm e Cathut nahoeh niteh, a hnaicanae koe kaawm e CAthut lah maw ka o, telah BAWIPA ni a dei.
24 Kodi wina angathe kubisala Ine osamuona?” “Kodi Ine sindili ponseponse kumwamba ndi dziko lapansi?” Akutero Yehova.
Ka hmu thai hoeh nahanlah ka kâhrawk thai e ao awh maw, telah BAWIPA ni a dei. Talai hoi kalvan dawk ka kawi nahoehmaw, telah BAWIPA ni a dei.
25 “Ndamva zimene aneneri akuyankhula. Iwo amalosera zabodza mʼdzina langa nʼkumati, ‘Ndalota! Ndalota!’
Mang ka mang, mang ka mang ti teh ka min lahoi laithoe ka dei e profetnaw ni dei e lawk hah ka thai.
26 Kodi zabodzazi zidzakhalabe mʼmitima ya aneneriwa mpaka liti? Iwotu amalosera zonyenga za mʼmitima yawo.
Laithoe ouk ka dei e profet a ma hoi a lungthin a kâdum teh lawk ouk ka dei e lungthin dawk nâtotouh maw ao han.
27 Aneneriwa amakhulupirira kuti anthu anga adzayiwala mawu anga akamamva za maloto awo amene amayankhulana ngati mmene anachitira makolo awo popembedza Baala.
Ahni ni a imri koe a mang lah a dei pouh teh, a napanaw ni Baal kecu dawk ka min a pahnim e patetlah ka taminaw hah ka min pahnim sak hanelah a kâcai awh.
28 Mneneri amene ali ndi maloto afotokoze malotowo. Koma iye amene ali ndi mawu anga alalikire mawuwo mokhulupirika. Kodi phesi lingafanane ndi chimanga?
Mang ka tawn e profet ni a mang hah dei naseh, kaie lawk ka tawn e profet ni kaie lawk hah yuemkamcu lah dei naseh, cahik hoi cahuem ni bangne kâvannae a tawn, telah BAWIPA ni a dei.
29 Kodi suja mawu anga amatentha ngati moto? Suja mawu anga amaphwanya monga ichitira nyundo kuphwanya miyala?” Akutero Yehova.
Ka lawk teh hmai patetlah talung rekkâbawng lah ka dêi thai e cakkin patetlah awm hoeh namaw, telah BAWIPA ni a dei.
30 Yehova akuti, “Nʼchifukwa chake, Ine ndikudana nawo aneneri amene amaberana okhaokha mawu nʼkumati mawuwo ndi a Yehova.”
Hatdawkvah, thai awh haw! kaie lawk ouk ka parawt e profet hah ka taran doeh, telah BAWIPA ni a dei.
31 Yehova akuti, “Inde, Ine ndikudana ndi aneneri amene amakonda kuyankhula zabodza nʼkumanena kuti, ‘Amenewa ndi mawu a Yehova.’”
Khenhaw! a lai ka pâhnan e profet BAWIPA ni a dei, ka tet e hah ka taran doeh, telah BAWIPA ni a dei.
32 Yehova akuti, “Ndithudi, Ine ndikudana ndi aneneri a maloto abodzawa. Iwo amafotokoza malotowo nʼkumasocheretsa anthu anga ndi bodza lawo losachita nalo manyazilo, chonsecho Ine sindinawatume kapena kuwalamula. Iwo sathandiza anthuwa ndi pangʼono pomwe,” akutero Yehova.
Khenhaw! a mang hah laithoe a dei teh, kâhat laipalah a dei awh e laithoe lahoi, lam teng lah ka taminaw kacetsakkung, profet hah ka taran doeh telah BAWIPA ni a dei. Hateiteh, ahnimouh ka patoun teh kâ ka poe hoeh. Hatdawkvah, taminaw hawinae poe kalawn hoeh, telah BAWIPA ni a dei.
33 Yehova anawuza Yeremiya kuti, “Anthu awa, kapena mneneri, kapenanso wansembe, akakufunsa kuti, ‘Kodi uthenga wolemetsa wa Yehova ukuti chiyani?’ uwawuze kuti, ‘Inuyo ndinu katundu wolemetsa Yehova, ndipo adzakutayani.’
Tamimaya thungup hoi thoseh, profetnaw thung hoi thoseh, vaihmanaw thung hoi thoseh, BAWIPA ni a pâpho e bangne telah na pacei awh pawiteh, hettelah na dei pouh han, bang lawk pâpho e maw, nangmanaw totouh na ceitakhai awh han, telah BAWIPA ni a dei.
34 Ngati mneneri kapena wansembe kapenanso munthu wina aliyense anena kuti, ‘Uthenga wolemetsa wa Yehova ndi uwu,’ Ine ndidzalanga munthu ameneyo pamodzi ndi banja lake.
Profet thoseh, vaihma thoseh, tami buetbuet touh thoseh, BAWIPA e pâpho lawk ao ka tet e tami awm pawiteh, hote tami hoi a imthung hah kai ni ka rek han.
35 Koma chimene aliyense wa inu azifunsa kwa mnzake kapena mʼbale wake ndi ichi: ‘Kodi Yehova wayankha chiyani?’ kapena ‘Yehova wayankhula chiyani?’
Hottelah tami bangpatet nihai, a imri thoseh, a hmaunawngha koe thoseh, BAWIPA ni bangtelamaw a pathung, BAWIPA ni bangne a dei telah a pacei awh han.
36 Koma musanenenso kuti ‘nawu uthenga wolemetsa wa Yehova,’ chifukwa mawu a munthu aliyense ndiwo uthenga wa iye mwini, kotero kuti inu mumakhotetsa mawu a Mulungu wamoyo, Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wathu.
BAWIPA ni a pâpho e doeh katetkung hah teh, na dei awh mahoeh toe. Bangkongtetpawiteh, tami bangpatet hai amae lawk hah ama hanelah a pâpho e lah kaawm han.
37 Tsono iwe Yeremiya udzamufunse mneneri kuti, ‘Kodi Yehova wakuyankha chiyani?’ kapena, ‘Kodi Yehova wayankhula chiyani?’
Profet koevah, BAWIPA ni bangtelamaw na pathung, BAWIPA ni bangmaw a dei, na ti pouh han.
38 Ngati mudzanena kuti, ‘Nawu uthenga wolemetsa wa Yehova,’ ndiye tsono Yehova akuti, ‘Popeza mwagwiritsa ntchito mawu akuti: Nawu uthenga wolemetsa wa Yehova, mawu amene ndinakuletsani kuti musawatchule,
Nangmouh ni BAWIPA e pâpho lawk doeh na ti awh dawkvah, BAWIPA ni a dei e teh, BAWIPA e pâpho lawk ao na ti awh hoeh nahanlah, kai ni kâ na poe awh eiteh, nangmouh ni BAWIPA e pâpho lawk ao na ti awh e lawk na hno awh dawkvah,
39 ndiye kuti Ine ndidzakunyamulani ngati katundu nʼkukuponyani kutali. Ndidzakuchotsani pamaso panga, inuyo pamodzi ndi mzinda umene ndinakupatsani inu ndi makolo anu.
thaihaw! betbet na sawn awh han. Kai koe na onae koehoi na tâkhawng awh han, nangmouh hoi na khopui, nangmouh koe thoseh, na mintoenaw koe thoseh, na poe awh e hoi,
40 Ndidzakunyozani mpaka muyaya. Ndidzakuchititsani manyazi osayiwalika.’”
a yungyoe pathoenae hoi kayayeirai pahnim thai e lah kaawm hoeh e hah nangmouh koe ka pha sak han.