< Yeremiya 21 >
1 Mfumu Zedekiya inatuma Pasuri mwana wa Malikiya ndi wansembe Zefaniya mwana wa Maseya kwa Yeremiya.
Ilizwi lafika kuJeremiya livela kuThixo lapho uZedekhiya inkosi wayethume kuye uPhashuri indodana kaMalikhija lomphristi uZefaniya indodana kaMaseya. Bathi:
2 Iwo amati akanene kwa Yeremiya mawu akuti, “Tinenere kwa Yehova chifukwa Nebukadinezara mfumu ya Babuloni akutithira nkhondo. Mwina mwake Yehova nʼkutichitira zodabwitsa kuti Nebukadinezarayo achoke kwathu kuno.”
“Ake usibuzele kuThixo khathesi nje, ngoba uNebhukhadineza inkosi yaseBhabhiloni uyasihlasela. Mhlawumbe uThixo angasenzela izimanga njengasezikhathini ezedlulayo ukuze asuke kithi.”
3 Koma Yehova anawuza Yeremiya kuti ayankhe Pasuri ndi Zefaniya kuti, “Kamuwuzeni Zedekiya kuti,
Kodwa uJeremiya wathi kubo, “Tshelani uZedekhiya lithi:
4 ‘Yehova, Mulungu wa Israeli akuti ndikulandeni zida zimene zili mʼmanja mwanu zimene mukugwiritsa ntchito polimbana ndi mfumu ya ku Babuloni ndi ankhondo ake amene akuzingani kunja kwa lingali. Ndipo ndidzasonkhanitsa zidazo mʼkati mwa mzindawu.
‘UThixo, uNkulunkulu ka-Israyeli, uthi: Sekuseduze ukuthi ngiziphendulele kuwe izikhali zempi ezisezandleni zakho, ozisebenzisayo ekulweni lenkosi yaseBhabhiloni lamaKhaladiya angaphandle komduli ekuvimbezele. Njalo ngizawaqoqa phakathi kwalelidolobho.
5 Ineyo mwini wakene ndi mkono wotambasula ndi dzanja lamphamvu, ndidzachita nanu nkhondo ndili wokwiya, wokalipa ndi waukali.
Mina uqobo ngizakulwa lawe ngesandla eseluliweyo langengalo elamandla ngentukuthelo langokufuthelana kanye lolaka olukhulu.
6 Ndidzakantha amene amakhala mu mzinda muno, anthu pamodzi ndi zirombo, ndipo zidzafa ndi mliri woopsa.
Ngizabatshaya abahlala kulelidolobho, abantu lezifuyo njalo bazabulawa yisifo esesabekayo.
7 Pambuyo pake, ndidzapereka Zedekiya mfumu ya ku Yuda, nduna zake pamodzi ndi anthu a mu mzinda muno amene adzapulumuke pa nthawi ya mliri, lupanga ndi njala kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni ndi kwa adani awo amene ankafuna kuwapha. Iye adzawapha ndi lupanga. Sadzawachitira chifundo kapena kuwamvera chisoni kapenanso kuwakomera mtima.’
Emva kwalokho, kutsho uThixo, uZedekhiya inkosi yakoJuda, lezikhulu zakhe kanye labantu bakulelidolobho abaphepha emkhuhlaneni, enkembeni lasendlaleni, ngizabanikela kuNebhukhadineza inkosi yaseBhabhiloni lasezitheni zabo ezifuna ukubabulala. Uzababulala ngenkemba; kayikuba lomusa kumbe uzwelo loba isihawu.’
8 “Yehova anati ndiwawuzenso anthu amenewa kuti asankhe pakati pa moyo ndi imfa.
Phezu kwalokho, abantu batshele uthi, ‘UThixo uthi: Khangelani, ngiyalimisela phambi kwenu indlela yokuphila lendlela yokufa.
9 Aliyense amene akhale mu mzinda muno adzaphedwa ndi lupanga, njala kapena mliri. Koma aliyense amene apite kukadzipereka kwa Ababuloni amene akuzinganiwa adzakhala ndi moyo, adzapulumuka.
Loba ngubani osala kulelidolobho uzabulawa ngenkemba, yindlala loba ngumkhuhlane. Kodwa loba ngubani ophumayo kulo ayezinikela kumaKhaladiya alivimbezeleyo uzasila, aphunyuke lokuphila kwakhe.
10 Ine ndatsimikiza kuchitira mzinda uno choyipa osati chabwino, akutero Yehova. Udzaperekedwa mʼdzanja la mfumu ya ku Babuloni, ndipo iyeyo adzawutentha ndi moto.
Sengiqonde ukwenza okubi kulelidolobho hatshi okuhle, kutsho uThixo. Lizanikelwa ezandleni zenkosi yaseBhabhiloni, ezalitshabalalisa ngomlilo.’
11 “Komanso, uwuze banja laufumu la Yuda kuti, ‘Imva mawu a Yehova;
Phezu kwalokho, wothi endlini yenkosi yakoJuda, ‘Zwanini ilizwi likaThixo;
12 inu a mʼbanja la Davide, Yehova akuti, “‘Weruzani mwachilungamo mmawa uliwonse; pulumutsani mʼdzanja la wozunza aliyense amene walandidwa katundu wake, kuopa kuti ukali wanga ungabuke ndi kuyaka ngati moto wosazimitsika chifukwa cha zoyipa zimene mwachita.
lina abendlu kaDavida, uThixo uthi: Yenzani ukulunga insuku zonke ekuseni; mhlengeni esandleni somncindezeli wakhe lowo ophangiweyo, hlezi ulaka lwami luqubuke, lutshise njengomlilo ngenxa yobubi elibenzileyo, lutshise engekho ongalucitsha.
13 Ndidzalimbana nanu, inu amene mukukhala pamwamba pa chigwa, inu okhala ngati thanthwe lapachidikha, akutero Yehova. Inu amene mumanena kuti, ‘Ndani amene angabwere kudzalimbana nafe? Ndani amene angathe kulowa mʼmalinga mwathu?’
Ngimelane lawe, Jerusalema, wena ohlala ngaphezu kwalesisigodi, emagcekeni alamadwala, kutsho uThixo, lina elithi, “Ngubani ongazasihlasela na? Ngubani ongangena esiphephelweni sethu na?”
14 Ndidzakulangani molingana ndi ntchito zanu, akutero Yehova. Ndidzatentha nkhalango zanu; moto udzapsereza zonse zimene zakuzungulirani.’”
Ngizalijezisa njengokufanele izono zenu, kutsho uThixo. Ngizaphemba umlilo emahlathini enu ozalobisa konke okuseduze lani.’”