< Yeremiya 21 >

1 Mfumu Zedekiya inatuma Pasuri mwana wa Malikiya ndi wansembe Zefaniya mwana wa Maseya kwa Yeremiya.
BOEIPA taeng lamkah ol te Jeremiah taengla ha pawk. Te vaengah manghai Zedekiah loh anih taengla Malkhiah capa Pashur neh khosoih Maaseiah capa Zephaniah te a tueih tih,
2 Iwo amati akanene kwa Yeremiya mawu akuti, “Tinenere kwa Yehova chifukwa Nebukadinezara mfumu ya Babuloni akutithira nkhondo. Mwina mwake Yehova nʼkutichitira zodabwitsa kuti Nebukadinezarayo achoke kwathu kuno.”
“Babylon manghai Nebukhanezar loh Mamih m'vathoh thil coeng dongah BOEIPA te mamih ham dawt pawn saeh. Amah khobaerhambae cungkuem he BOEIPA loh mamih ham a saii khaming, tedae mamih taeng lamloh nong mai saeh,” a ti nah.
3 Koma Yehova anawuza Yeremiya kuti ayankhe Pasuri ndi Zefaniya kuti, “Kamuwuzeni Zedekiya kuti,
Tedae amih te Jeremiah loh, “He he Zedekiah taengah thui pah,” a ti nah.
4 ‘Yehova, Mulungu wa Israeli akuti ndikulandeni zida zimene zili mʼmanja mwanu zimene mukugwiritsa ntchito polimbana ndi mfumu ya ku Babuloni ndi ankhondo ake amene akuzingani kunja kwa lingali. Ndipo ndidzasonkhanitsa zidazo mʼkati mwa mzindawu.
Israel Pathen BOEIPA he ni a thui. Na kut dongkah caemtloek hnopai te nangmih aka vathoh thil Babylon manghai taeng neh vongvoel lamloh vongtung duela nangmih aka dum Khalden taengla ka mael ne. Te dongah amih te he khopuei laklung ah ka kuk ni.
5 Ineyo mwini wakene ndi mkono wotambasula ndi dzanja lamphamvu, ndidzachita nanu nkhondo ndili wokwiya, wokalipa ndi waukali.
Nangmih taengah kut ka thueng vetih, ka tlungluen ban neh, thintoek neh, kosi neh, thinhul bat la kan vathoh thil ni.
6 Ndidzakantha amene amakhala mu mzinda muno, anthu pamodzi ndi zirombo, ndipo zidzafa ndi mliri woopsa.
He khopuei kah khosa rhoek neh hlang khaw rhamsa khaw ka ngawn vetih duektahaw neh mat duek uh ni.
7 Pambuyo pake, ndidzapereka Zedekiya mfumu ya ku Yuda, nduna zake pamodzi ndi anthu a mu mzinda muno amene adzapulumuke pa nthawi ya mliri, lupanga ndi njala kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni ndi kwa adani awo amene ankafuna kuwapha. Iye adzawapha ndi lupanga. Sadzawachitira chifundo kapena kuwamvera chisoni kapenanso kuwakomera mtima.’
Te phoeikah te khaw BOEIPA kah olphong ni. Judah manghai Zedekiah neh a sal rhoek, pilnam neh he khopuei khuiah duektahaw lamloh, cunghang lamloh, khokha lamloh aka sueng te Babylon manghai Nebukhanezar kut dongah, a thunkha kut dongah, a hinglu aka toem kut dongah ka paek ni. Te vaengah amih te cunghang ha neh a ngawn vetih amih te rhen mahpawh, hnaih mahpawh, haidam mahpawh.
8 “Yehova anati ndiwawuzenso anthu amenewa kuti asankhe pakati pa moyo ndi imfa.
Tedae he pilnam taengah BOEIPA loh a thui he thui pah. Kai loh nangmih mikhmuh ah hingnah longpuei neh dueknah longpuei kang khueh coeng he.
9 Aliyense amene akhale mu mzinda muno adzaphedwa ndi lupanga, njala kapena mliri. Koma aliyense amene apite kukadzipereka kwa Ababuloni amene akuzinganiwa adzakhala ndi moyo, adzapulumuka.
He khopuei khuikah khosa rhoek tah cunghang neh, khokha neh, duektahaw neh duek ni. Tedae aka coe tih nangmih aka dum Khalden taengah aka kuep tah hing rhoe hing vetih a hinglu te amah taengah kutbuem bangla a khueh ni.
10 Ine ndatsimikiza kuchitira mzinda uno choyipa osati chabwino, akutero Yehova. Udzaperekedwa mʼdzanja la mfumu ya ku Babuloni, ndipo iyeyo adzawutentha ndi moto.
A then ham pawt tih a thae ham ni he khopuei soah ka maelhmai ka khueh he BOEIPA kah olphong ni. Babylon manghai kut dongah a tloeng vetih hmai neh a hoeh ni.
11 “Komanso, uwuze banja laufumu la Yuda kuti, ‘Imva mawu a Yehova;
Judah manghai imkhui te khaw BOEIPA ol hnatun uh.
12 inu a mʼbanja la Davide, Yehova akuti, “‘Weruzani mwachilungamo mmawa uliwonse; pulumutsani mʼdzanja la wozunza aliyense amene walandidwa katundu wake, kuopa kuti ukali wanga ungabuke ndi kuyaka ngati moto wosazimitsika chifukwa cha zoyipa zimene mwachita.
David imkhui aw, BOEIPA loh he ni a thui. Mincang ah a tiktamnah neh laitloek. Hnaemtaek kut loh a reth te huul laeh. Ka kosi he hmai bangla puek vetih n'hlawp ve. Na khoboe kah khoboe thaenah dongah thi pawt ve.
13 Ndidzalimbana nanu, inu amene mukukhala pamwamba pa chigwa, inu okhala ngati thanthwe lapachidikha, akutero Yehova. Inu amene mumanena kuti, ‘Ndani amene angabwere kudzalimbana nafe? Ndani amene angathe kulowa mʼmalinga mwathu?’
He tah BOEIPA kah olphong coeng ni. 'Unim mamih ka et vetih unim mamih kah khodun la aka pawk eh? ' aka ti rhoek, tlangkol lungpang kol kah khosa nangmih te kam pai thil coeng he.
14 Ndidzakulangani molingana ndi ntchito zanu, akutero Yehova. Ndidzatentha nkhalango zanu; moto udzapsereza zonse zimene zakuzungulirani.’”
He tah BOEIPA olphong ni. Na khoboe thaihtae bangla nangmih te kan cawh ni. A duup ah hmai ka hlup vetih a kaepvai boeih te boeih a hlawp ni.

< Yeremiya 21 >