< Yeremiya 2 >

1 Yehova anandiwuza kuti,
و کلام خداوند بر من نازل شده، گفت:۱
2 “Pita ukalengeze kwa anthu a ku Yerusalemu kuti Yehova akuti, “‘Ine ndikukumbukira mmene umakhulupirikira pa unyamata wako, mmene unkandikondera ngati momwe amachitira mkwatibwi, mmene unkanditsata mʼchipululu muja; mʼdziko losadzalamo kanthu.
«برو و به گوش اورشلیم ندا کرده، بگوخداوند چنین می‌گوید: غیرت جوانی تو ومحبت نامزد شدن تو را حینی که از عقب من دربیابان و در زمین لم یزرع می‌خرامیدی برایت به‌خاطر می‌آورم.۲
3 Israeli anali wopatulika wa Yehova, anali ngati zipatso zake zoyamba kucha pa nthawi yokolola; onse amene anamuzunza anapezeka kuti ndi olakwa ndipo mavuto anawagwera,’” akutero Yehova.
اسرائیل برای خداوند مقدس ونوبر محصول او بود. خداوند می‌گوید: آنانی که اورا بخورند مجرم خواهند شد و بلا بر ایشان مستولی خواهد گردید.»۳
4 Imvani mawu a Yehova, inu zidzukulu za Yakobo, inu mafuko onse a Israeli.
‌ای خاندان یعقوب و جمیع قبایل خانواده اسرائیل کلام خداوند را بشنوید!۴
5 Yehova akuti, “Kodi makolo anu anandipeza nʼcholakwa chanji, kuti andithawe? Iwo anatsata milungu yachabechabe, nawonso nʼkusanduka achabechabe.
خداوند چنین می‌گوید: «پدران شما در من چه بی‌انصافی یافتندکه از من دوری ورزیدند و اباطیل را پیروی کرده، باطل شدند؟۵
6 Iwo sanafunse nʼkomwe kuti, ‘Kodi Yehova ali kuti, amene anatitulutsa mʼdziko la Igupto natitsogolera mʼchipululu mʼdziko lowuma ndi lokumbikakumbika, mʼdziko lopanda mvula ndi la mdima, dziko limene munthu sadutsamo ndipo simukhala munthu aliyense?’
و نگفتند: یهوه کجا است که ما رااز زمین مصر برآورد و ما را در بیابان و زمین ویران و پر از حفره‌ها و زمین خشک و سایه موت وزمینی که کسی از آن گذر نکند و آدمی در آن ساکن نشود رهبری نمود؟۶
7 Ndinakufikitsani ku dziko lachonde kuti mudye zipatso zake ndi zabwino zake zina. Koma inu mutafika munaliyipitsa dziko langa ndi kusandutsa cholowa changa kukhala chonyansa.
و من شما را به زمین بستانها آوردم تا میوه‌ها و طیبات آن را بخورید، اما چون داخل آن شدید زمین مرا نجس ساختیدومیراث مرا مکروه گردانیدید.۷
8 Ansembe nawonso sanafunse kuti, ‘Yehova ali kuti?’ Iwo amene amaphunzitsa malamulo sanandidziwe; atsogoleri anandiwukira. Aneneri ankanenera mʼdzina la Baala, ndi kutsatira mafano achabechabe.
کاهنان نگفتند: یهوه کجاست و خوانندگان تورات مرا نشناختندو شبانان بر من عاصی شدند و انبیا برای بعل نبوت کرده، در عقب چیزهای بی‌فایده رفتند.۸
9 “Chifukwa chake Ine ndidzakuyimbaninso mlandu,” akutero Yehova. “Ndipo ndidzayimbanso mlandu zidzukulu zanu.
بنابراین خداوند می‌گوید: بار دیگر با شما مخاصمه خواهم نمود و با پسران پسران شما مخاصمه خواهم کرد.۹
10 Pitani kumadzulo ku chilumba cha Kitimu, ndipo mukaone, tumizani anthu ku Kedara kuti akafufuze bwino; ndipo muona kuti zinthu zoterezi sizinachitikepo nʼkale lomwe:
پس به جزیره های کتیم گذرکرده، ملاحظه نمایید و به قیدار فرستاده به دقت تعقل نمایید و دریافت کنید که آیا حادثه‌ای مثل این واقع شده باشد؟۱۰
11 Kodi ulipo mtundu wa anthu uliwonse umene unasinthapo milungu yake? (Ngakhale kuti si milungu nʼkomwe). Koma anthu anga asinthitsa Mulungu wawo waulemerero ndi mafano achabechabe.
که آیا هیچ امتی خدایان خویش را عوض کرده باشند با آنکه آنها خدانیستند؟ اما قوم من جلال خویش را به آنچه فایده‌ای ندارد عوض نمودند.۱۱
12 Inu mayiko akumwamba, dabwani ndi zimenezi, ndipo njenjemerani ndi mantha aakulu,” akutero Yehova.
پس خداوندمی گوید: ای آسمانها از این متحیر باشید و به خود لرزیده، به شدت مشوش شوید!۱۲
13 “Popeza anthu anga achita machimo awiri: Andisiya Ine kasupe wa madzi a moyo, ndi kukadzikumbira zitsime zawo, zitsime zongʼaluka, zomwe sizingathe kusunga madzi.
زیرا قوم من دو کار بد کرده‌اند. مرا که چشمه آب حیاتم ترک نموده و برای خود حوضها کنده‌اند، یعنی حوضهای شکسته که آب را نگاه ندارد.۱۳
14 Israeli si wantchito kapena kapolo wobadwira mʼnyumba, ayi. Nanga nʼchifukwa chiyani amuwononga chotere?
آیااسرائیل غلام یا خانه زاد است پس چرا غارت شده باشد؟۱۴
15 Adani ake abangulira ndi kumuopseza ngati mikango. Dziko lake analisandutsa bwinja; mizinda yake anayitentha popanda wokhalamo.
شیران ژیان بر او غرش نموده، آواز خود را بلند کردند و زمین او را ویران ساختند و شهرهایش سوخته و غیرمسکون گردیده است.۱۵
16 Ndiponso Aigupto a ku Mefisi ndi a ku Tapanesi akuphwanyani mitu.
و پسران نوف و تحفنیس فرق تورا شکسته‌اند.۱۶
17 Zimenezitu zakuchitikirani chifukwa munasiya Yehova Mulungu wanu pamene Iye ankakutsogolerani pa njira yanu?
آیا این را بر خویشتن واردنیاوردی چونکه یهوه خدای خود را حینی که تورا رهبری می‌نمود ترک کردی؟۱۷
18 Tsopano mudzapindula chiyani mukapita ku Igupto, kukamwa madzi a mu Sihori? Ndipo mudzapindulanji mukapita ku Asiriya, kukamwa madzi a mu mtsinje wa Yufurate?
و الان تو را باراه مصر چه‌کار است تا آب شیحور را بنوشی؟ وتو را با راه آشور چه‌کار است تا آب فرات رابنوشی؟»۱۸
19 Kuyipa kwanuko kudzakulangani; kubwerera mʼmbuyo kwanuko kudzakutsutsani. Tsono ganizirani bwino, popeza ndi chinthu choyipa kundisiya Ine Yehova Mulungu wanu; ndi chinthu chowawa ndithu kusandiopa Ine Mulungu wanu. Akutero Ambuye Yehova Wamphamvuzonse.
خداوند یهوه صبایوت چنین می‌گوید: «شرارت تو، تو را تنبیه کرده و ارتداد تو، تو راتوبیخ نموده است پس بدان و ببین که این امرزشت و تلخ است که یهوه خدای خود را ترک نمودی و ترس من در تو نیست.۱۹
20 “Kuyambira kalekale inu munathyola goli lanu ndi kudula msinga zanu; munanena kuti, ‘Sitidzakutumikirani!’ Ndithudi, inu mwakhala ngati mkazi wachiwerewere. Mukupembedza milungu ina pa phiri lililonse lalitali ndiponso pansi pa mtengo uliwonse wa masamba ambiri.
زیرا از زمان قدیم یوغ تو را شکستم و بندهای تو را گسیختم وگفتی بندگی نخواهم نمود زیرا بر هر تل بلند وزیر هر درخت سبز خوابیده، زنا کردی.۲۰
21 Ine ndinakudzala iwe ngati mtengo wampesa wosankhika; unali mpesa wabwino kwambiri ndi wodalirika. Nanga nʼchifukwa chiyani wasanduka mpesa wachabechabe wonga wa kutchire?
و من تو را مو اصیل و تخم تمام نیکو غرس نمودم پس چگونه نهال مو بیگانه برای من گردیده‌ای؟۲۱
22 Ngakhale utasamba ndi soda kapena kusambira sopo wambiri, kuthimbirira kwa machimo ako kumaonekabe pamaso panga,” akutero Ambuye Yehova.
پس اگر‌چه خویشتن را با اشنان بشویی و صابون برای خود زیاده بکار بری، اما خداوند یهوه می‌گویدکه گناه تو پیش من رقم شده است.۲۲
23 “Iwe ukunena bwanji kuti, ‘Ine sindinadziyipitse; sindinatsatire Abaala’? Takumbukira mmene unkandichimwira mʼchigwa muja; zindikira bwino zomwe wachita. Iwe uli ngati ngamira yayikazi yaliwiro yomangothamanga uku ndi uku,
چگونه می‌گویی که نجس نشدم و در عقب بعلیم نرفتم؟ طریق خویش را در وادی بنگر و به آنچه کردی اعتراف نما‌ای شتر تیزرو که در راههای خودمی دوی!۲۳
24 wakhala ngati mbidzi yozolowera mʼchipululu, yonka ninunkhiza pa nthawi yachisika. Ndani angayiretse chilakolako chakecho? Mphongo iliyonse yoyikhumba sidzavutika. Pa nthawi yachisika chakecho mphongoyo idzayipeza.
مثل گورخر هستی که به بیابان عادت داشته، در شهوت دل خود باد را بو می‌کشد. کیست که از شهوتش او را برگرداند؟ آنانی که اورا می‌طلبند خسته نخواهند شد و او را در ماهش خواهند یافت.۲۴
25 Iwe usathamange, nsapato zingakuthere kuphazi ndi kukhosi kwako kuwuma ndi ludzu. Koma unati, ‘Zamkutu! Ine ndimakonda milungu yachilendo, ndipo ndidzayitsatira.’
پای خود را از برهنگی و گلوی خویش را از تشنگی باز دار. اما گفتی نی امیدنیست زیرا که غریبان را دوست داشتم و از عقب ایشان خواهم رفت.۲۵
26 “Monga momwe mbala imachitira manyazi pamene yagwidwa, moteronso nyumba ya Israeli idzachita manyazi; Aisraeliwo, mafumu ndi akuluakulu awo, ansembe ndi aneneri awo.
مثل دزدی که چون گرفتارشود خجل گردد. همچنین خاندان اسرائیل باپادشاهان و سروران و کاهنان و انبیای ایشان خجل خواهند شد.۲۶
27 Iwo amawuza mtengo kuti, ‘Iwe ndiwe abambo athu,’ ndipo amawuza mwala kuti, ‘Iwe ndiye amene unatibala.’ Iwo andifulatira Ine, ndipo safuna kundiyangʼana; Koma akakhala pa mavuto amati, ‘Bwerani mudzatipulumutse!’
که به چوب می‌گویند توپدر من هستی و به سنگ که تو مرا زاییده‌ای زیراکه پشت به من دادند و نه رو. اما در زمان مصیبت خود می‌گویند: برخیز و ما را نجات ده.۲۷
28 Nanga ili kuti milungu yanu imene munadzipangira nokha? Ibweretu ngati ingathe kukupulumutsani pamene muli pamavuto! Inu anthu a ku Yuda, milungu yanu ndi yambiri kuchuluka kwake ngati mizinda yanu.
پس خدایان تو که برای خود ساختی کجایند؟ ایشان در زمان مصیتت برخیزند و تو را نجات دهند. زیرا که‌ای یهودا خدایان تو به شماره شهرهای تومی باشند.»۲۸
29 “Kodi mukundizengeranji mlandu? Nonse mwandiwukira,” akutero Yehova.
خداوند می‌گوید: «چرا با من مخاصمه می‌نمایید جمیع شما بر من عاصی شده‌اید.۲۹
30 “Ine ndinalanga anthu ako popanda phindu; iwo sanaphunzirepo kanthu. Monga mkango wolusa, lupanga lanu lapha aneneri anu.
پسران شما را عبث زده‌ام زیرا که تادیب رانمی پذیرند. شمشیر شما مثل شیر درنده انبیای شما را هلاک کرده است.۳۰
31 “Inu anthu a mʼbado uno, ganizirani bwino mawu a Yehova: “Kodi Ine ndinakhalapo ngati chipululu kwa Israeli kapena ngati dziko la mdima wandiweyani? Chifukwa chiyani anthu anga akunena kuti, ‘Ife tili ndi ufulu omayendayenda; sitidzabweranso kwa Inu’?
‌ای شما که اهل این عصر می‌باشید کلام خداوند را بفهمید! آیا من برای اسرائیل مثل بیابان یا زمین ظلمت غلیظشده‌ام؟ پس قوم من چرا می‌گویند که روسای خود شده‌ایم و بار دیگر نزد تو نخواهیم آمد.۳۱
32 Kodi namwali amayiwala zokongoletsera zake, kapena kuyiwala zovala zake za ukwati? Komatu anthu anga andiyiwala masiku osawerengeka.
آیا دوشیزه زیور خود را یا عروس آرایش خود را فراموش کند؟ اما قوم من روزهای بیشمارمرا فراموش کرده‌اند.۳۲
33 Mumadziwa bwino njira zopezera zibwenzi! Choncho ngakhale akazi oyipa omwe mumawaphunzitsa njira zanu.
چگونه راه خود را مهیامی سازی تا محبت را بطلبی؟ بنابراین زنان بد رانیز به راههای خود تعلیم دادی.۳۳
34 Ngakhale pa zovala zako anthu amapezapo magazi a anthu osauka osalakwa. Anthuwo simunawapeze akuthyola nyumba. Komabe ngakhale zinthu zili chomwechi,
در دامنهای تونیز خون جان فقیران بی‌گناه یافته شد. آنها را درنقب زدن نیافتم بلکه بر جمیع آنها.۳۴
35 inu mukunena kuti, ‘Ndife osalakwa, sadzatikwiyira.’ Ndidzakuyimbani mlandu chifukwa mukunena kuti, ‘Ife sitinachimwe.’
و می‌گویی: چونکه بی‌گناه هستم غضب او از من برگردانیده خواهد شد. اینک به‌سبب گفتنت که گناه نکرده‌ام بر تو داوری خواهم نمود.۳۵
36 Chifukwa chiyani mukunkabe nimusinthasintha njira zanu? Aigupto adzakukhumudwitsani monga momwe Asiriya anakuchititsani manyazi.
چرا اینقدرمی شتابی تا راه خود را تبدیل نمایی؟ چنانکه ازآشور خجل شدی همچنین از مصر نیز خجل خواهی شد.۳۶
37 Mudzachokanso kumeneko manja ali kunkhongo. Popeza Ine Yehova ndawakana anthu amene munkawadalira, choncho sadzakuthandizani konse.
از این نیز دستهای خود را برسرت نهاده، بیرون خواهی آمد. چونکه خداونداعتماد تو را خوار شمرده است پس از ایشان کامیاب نخواهی شد.»۳۷

< Yeremiya 2 >