< Yeremiya 15 >
1 Kenaka Yehova anandiwuza kuti, “Ngakhale Mose ndi Samueli akanayima pamaso panga kupempherera anthu awa, Ine sindikanawachitira chisoni. Achotseni ndipo ndisawaonenso! Aleke apite!
Eka Jehova Nyasaye nowachona kama: “Kata dabed ni Musa gi Samuel ema nyalo chungʼ e nyima, to ok anyal weyonegi richogi. Golgi oko e nyima! Wegi gidhi!
2 Ndipo ngati akufunsa iwe kuti, ‘Kodi tipite kuti?’ uwawuze kuti, ‘Yehova akuti, “‘Oyenera kufa adzafa; oyenera kufa ndi lupanga adzafa ndi lupanga; oyenera kufa ndi njala adzafa ndi njala; oyenera kupita ku ukapolo adzapita ku ukapolo.’
To ka gipenji ni, ‘Ere kama wanyalo dhiyoe?’ To nyisgi ni, ‘Ma e gima Jehova Nyasaye wacho: “‘Mago matho ochomo, tho nonegi; mago ma ligangla ochomo, noneg gi ligangla; to mago ma kech ochomo, kech nonegi; to mago ma twech ochomo, noter e twech.’”
3 “Ine ndidzawatumizira mitundu inayi ya zinthu zowononga,” akutero Yehova, “lupanga lowapha, agalu owaluma, mbalame zamumlengalenga ndiponso zirombo zoti ziwadye ndi kuwawononga.
Jehova Nyasaye owacho niya, “Abiro oro masiche angʼwen mopogore opogore, ma gin ligangla mar nek kod guogi maywayo gi mabor gi winy mafuyo e kor polo gi ondiegi mag bungu mondo okidhgi kendo tiekogi.
4 Ndidzawasandutsa kukhala chinthu chonyansa kwa anthu a maufumu onse a dziko lapansi chifukwa cha zimene Manase mwana wa Hezekiya mfumu ya Yuda anachita mu Yerusalemu.
Anami pinjeruodhi duto mag piny bed gibuok kuomgi nikech gima Manase wuod Hezekia ruodh Juda notimo e Jerusalem.
5 “Kodi adzakumvera chisoni ndani, Yerusalemu? Kodi adzakulira ndani? Kodi ndani amene adzapatuka kufunsa za moyo wako?
“Ere ngʼama nokechi, yaye Jerusalem? Ere ngʼama biro ywagi? Ere ngʼama nochungʼ ma penji kaka idhi?”
6 Inu mwandikana Ine,” akutero Yehova. “Inu mukubwererabe mʼmbuyo. Choncho Ine ndidzakukanthani. Ndatopa ndi kukuchitirani chifundo.
Jehova Nyasaye owacho niya, “Isedaga. Isiko mana kibaro iweyo yo. Omiyo anaket lweta kuomi kendo tieki; ok anatimni ngʼwono kendo.
7 Ine ndidzakubalalitsani kukuchotsani mʼmizinda ya mʼdzikomo monga mmene amachitira ndi mankhusu popeta ndi lichero. Anthu anga ndinawaliritsa ndi kuwawononga chifukwa sanasinthe makhalidwe awo oyipa.
Anapiedhgi gi odhech pietho e dhorangeye mag dala maduongʼ mar piny. Anakel lit kod kethruok ne joga, nimar gitamore loko yoregi.
8 Ndinachulukitsa amayi awo amasiye kupambana mchenga wa kunyanja. Amayiwo ndinawawonongera ana awo aamuna dzuwa lili pamutu. Mwadzidzidzi ndinawagwetsera kuwawa mtima ndi mantha.
Anami mon ma chwogi otho mag-gi bedo mathoth moloyo kwoyo manie dho nam. E odiechiengʼ tir anakel ngʼama nego mana rowere; kendo apoya nono anakelnegi lit kod bwok maduongʼ.
9 Mayi wa ana asanu ndi awiri wakomoka ndipo akupuma wefuwefu. Dzuwa lake lalowa ukanali usana; anamuchititsa manyazi ndipo wathedwa nzeru. Otsala ndidzawapereka mʼmanja mwa adani awo kuti awaphe ndi lupanga,” akutero Yehova.
Miyo man-gi nyithindo abiriyo nobed mool matho. To chiengʼ marienyne nopodhi kapod en odiechiengʼ; wiye nokuodi kendo chunye nochandre. Ananeg jogo motony gi ligangla, e nyim wasikgi,” Jehova Nyasaye owacho.
10 Kalanga ine, amayi pakuti munandibereka ine, munthu amene ndikutsutsana ndi kulimbana ndi anthu pa dziko lonse! Ine sindinakongoze kapena kukongola kanthu, komatu aliyense akunditemberera.
Wuololo, minwa, angʼo momiyo ne inywola, an ngʼat ma piny ngima piemgo kendo kedogo! Pok aholo ngʼato kata an bende pok ohola, to kata kamano ji duto kwongʼa.
11 Yehova anati, “Ndithudi, Ine ndidzakulanditsa kuti upeze bwino. Ndithudi, adani ako adzakupempha pa nthawi ya tsoka ndi ya mavuto awo.
Jehova Nyasaye nowacho, “Adier anaresi gi gima omiyo maber; adier anami wasiki sayi, e kinde mag masira kod kinde mag thagruok.
12 “Palibe munthu amene angathe kudula chitsulo, makamaka chitsulo chochokera kumpoto chosakaniza ndi mkuwa.
“Bende dhano nyalo turo chuma, chuma moa yo nyandwat kata mula?
13 Anthu ako ndi chuma chako ndidzazipereka kwa ofunkha popanda malipiro, chifukwa cha machimo anu onse a mʼdziko lanu lonse.
“Mwandu magu kod mago ma ukano anachiw mondo yaki, maonge chudo, nikech richo magu duto e pinyu mangima.
14 Ndidzakusandutsani akapolo a adani anu mʼdziko limene inu simulidziwa, chifukwa mkwiyo wanga wayaka ngati moto umene udzakutenthani.”
Anaketu ubed wasumbini ne wasiku e piny ma ok ungʼeyo, nimar mirimba biro moko mach mabiro wangʼou.”
15 Ine ndinati, “Inu Yehova, mumadziwa zonse; kumbukireni ndi kundisamalira. Ndilipsireni anthu ondizunza. Ndilezereni mtima musandilande moyo wanga. Onani momwe ndi kuvutikira chifukwa cha Inu.
In ingʼeyo, yaye Jehova Nyasaye; para kendo konya. Chul kuor ne joma sanda. Isenano koda omiyo kik iweya; par kaka osesanda kochaya nikech in.
16 Munandiyankhula ndipo mawu anu ndinawalandira bwino. Mawu anu anandipatsa chimwemwe ndipo mtima wanga unasangalala. Paja ine, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, ndimadziwika ndi dzina lanu.
Ka wechegi nobiro, ne achamogi; ne gin morna, kendo ilo mar chunya, nimar iluonga gi nyingi, yaye Jehova Nyasaye Maratego.
17 Sindinakhale nawo mʼgulu la anthu amadyera, sindinasangalale nawo anthu amenewo. Ndinakhala ndekha chifukwa choti dzanja lanu linali pa ine ndipo munadzaza mu mtima mwanga ndi mkwiyo.
Ne ok abedo e kanyakla mar jojaro, ne ok atimo nyasi kodgi; to ne abedo kenda nikech lweti ne ni kuoma kendo ne ipongʼa gi mirima.
18 Nanga nʼchifukwa chiyani mavuto anga sakutha? Bwanji chilonda changa sichikupola? Kodi inu mudzakhala ngati mtsinje wowuma nthawi yachilimwe, kapena ngati kasupe wopanda madzi?”
Angʼo momiyo rem mara ok rum kendo adhonda lich ma ok nyal thiedhore? Bende inyalo bedona ka aora modwono, mana ka soko motwo?
19 Tsono Yehova anandiyankha kuti, “Ukabwerera kwa Ine, ndidzakulandiranso ndipo udzakhalanso mtumiki wanga. Ngati udzayankhula mawu oyenera osati achabechabe, udzakhalanso mneneri wanga. Anthu adzabwera kwa iwe ndipo sipadzafunika kuti iwe upite kwa iwo.
Emomiyo ma e gima Jehova Nyasaye wacho: “Ka ilokori iweyo richoni, anaduogi mondo itina; ka iwacho weche mowinjore, ma ok manono, to ni inibed ngʼat ma wuoyo e loya. We jogi oduog ira, to in kik idog irgi.
20 Ndidzakusandutsa ngati khoma lolimba ngati mkuwa kwa anthu awa. Adzalimbana nawe koma sadzakugonjetsa, pakuti Ine ndili nawe kukulanditsa ndi kukupulumutsa,” akutero Yehova.
Anaketi ibed ohinga ne jogi, ohinga moger motegno mar mula; giniked kodi to ok gini loyi, nimar an kodi mondo akonyi kendo resi,” Jehova Nyasaye owacho.
21 “Ndidzakupulumutsa mʼdzanja la anthu oyipa ndipo ndidzakuwombola kwa anthu ankhanza.”
“Anaresi e lwet joma timbegi mono kendo akonyi e lwet joma ger.”