< Yeremiya 10 >

1 Inu Aisraeli, imvani zimene Yehova akunena.
Muntie nea Awurade ka kyerɛ mo, Israelfi.
2 Yehova akuti, “Musatsatire makhalidwe a anthu a mitundu ina kapena kuchita mantha ndi zizindikiro zamlengalenga, ngakhale anthu a mitundu ina amachita nazo mantha.
Sɛɛ na Awurade se: “Munnsua amanaman no akwan anaa momma wim nsɛnkyerɛnne mmɔ mo hu, ɛwɔ mu sɛ wɔbɔ amanaman no hu.
3 Pakuti miyambo ya mitundu inayo ndiyachabechabe. Iwo amakadula mtengo ku nkhalango ndipo mmisiri amawusema ndi sompho.
Na nkurɔfo no amanne nka hwee; wotwa dua fi kwae mu, na odwumfo de ne fitii asen.
4 Amakongoletsa chosemacho ndi siliva ndi golide; kenaka amachikhomerera ndi misomali kuti chisagwedezeke.
Wɔde dwetɛ ne sikakɔkɔɔ hyehyɛ no; wɔde nnadewa ne asae bobɔ si hɔ sɛnea ɛrenhwe fam.
5 Mafano awo ali ngati mtengo wakanjedza woopsezera mbalame mʼmunda wa minkhaka. Mafanowo sangathe nʼkuyankhula komwe ndipo ayenera kunyamulidwa popeza sangathe nʼkuyenda komwe. Musachite nawo mantha popeza sangathe kukuchitani choyipa ndiponso alibe mphamvu yochitira chabwino chilichonse.”
Ɛte sɛ kaakaabotoni a esi ɛfere mfikyifuw mu, wɔn ahoni no ntumi nkasa; ɛsɛ sɛ wɔsoa wɔn efisɛ wontumi nnantew. Munnsuro wɔn; wɔrentumi nhaw mo na wɔrentumi nyɛ ade pa biara nso.”
6 Palibe wofanana nanu, Inu Yehova; Inu ndinu wamkulu, ndipo dzina lanu lili ndi mphamvu yayikulu.
Obiara nte sɛ wo, Awurade; woyɛ ɔkɛse na wo din so wɔ tumi mu.
7 Ndani amene angaleke kukuopani, inu Mfumu ya mitundu ya anthu? Chimenechi ndicho chokuyenerani. Pakati pa anthu anzeru onse komanso mafumu onse a mitundu ya anthu, palibe wina wofanana nanu.
Hena na ɛnsɛ sɛ odi wo ni, Amansanhene? Eyi na ɛfata wo. Amanaman no so anyansafo nyinaa mu ne wɔn ahenni nyinaa mu, obiara ne wo nsɛ.
8 Onsewo ndi opusa ndi opanda nzeru; malangizo awo amawatenga kuchokera kwa mafano achabechabe opanga ndi mitengo.
Wɔn nyinaa yɛ adwenharefo ne nkwaseafo; dua ahoni a so nni mfaso na ɛma wɔn nkyerɛkyerɛ.
9 Siliva wosula amabwera naye kuchokera ku Tarisisi ndipo golide amachokera naye ku Ufazi. Mafanowo ndi ntchito ya anthu aluso ndi odziwa kuzokota golide. Tsono mafanowo amawaveka zovala za mtundu wamtambo ndi pepo. Yonseyo ndi ntchito ya anthu a luso.
Wɔde dwetɛ a wɔaboro fi Tarsis ba, ne sikakɔkɔɔ nso fi Ufas ba. Ɛyɛ nea odwumfo ne sika dwumfo ayɛ a wɔde ntama bibiri ne beredum afura no, ne nyinaa yɛ adwumfo anyansafo nsa ano nnwuma.
10 Koma Yehova ndiye Mulungu woona; Iyeyo ndiye Mulungu wamoyo, Mfumu yamuyaya. Akakwiya, dziko limagwedezeka; anthu a mitundu ina sangathe kupirira ukali wakewo.
Nanso Awurade ne nokware Onyankopɔn no; ɔno ne Onyankopɔn teasefo, daapem Hene no. Sɛ ne bo fuw a asase wosow; na amanaman no ntumi nnyina nʼabufuwhyew ano.
11 “Awuze anthu awa kuti, ‘Milungu iyi, imene sinalenge dziko lakumwamba ndi dziko lapansi, idzawonongeka pa dziko lapansi ndi pansi pa thambo.’”
“Ka eyi kyerɛ wɔn: ‘Saa anyame a ɛnyɛ wɔn na wɔyɛɛ ɔsoro ne asase no bɛyera afi asase so ne ɔsorosoro ase.’”
12 Koma Mulungu analenga dziko lapansi ndi mphamvu zake; Iye anapanga dziko lonse ndi nzeru zake ndipo anayala thambo mwaluso lake.
Nanso Onyankopɔn de ne tumi bɔɔ asase; ɔtoo wiase fapem wɔ ne nyansa mu, na ɔde ne nhumu trɛw ɔsorosoro mu.
13 Iye akayankhula, kumamveka mkokomo wamadzi akumwamba; Iyeyo amabweretsa mitambo kuchokera ku malekezero a dziko lapansi. Amabweretsa mphenzi pamodzi ndi mvula ndi kutulutsa mphepo yamkuntho kumalo kumene osungirako.
Sɛ ɔpaapae aprannaa a ɔsorosoro nsu bobɔ mu; ɔma omununkum ma ne ho so fi nsase ano. Ɔde anyinam ka osu ho ba, na ogyaa mframa mu fi nʼadekoradan mu.
14 Anthu onse ndi opusa ndiponso opanda nzeru; mmisiri aliyense wosula golide akuchita manyazi ndi mafano ake. Mafano akewo ndi abodza; alibe moyo mʼkati mwawo.
Onipa biara nnim nyansa, na onni nimdeɛ; sikadwumfo biara anim gu ase, esiane nʼahoni nti. Ne nsɛsode yɛ atoro; wonni ɔhome biara wɔ wɔn mu.
15 Mafanowo ndi achabechabe, zinthu zosekedwa nazo. Pamene anthuwo azidzaweruzidwa, mafanowo adzawonongedwa.
Wɔn so nni mfaso, wɔn ho yɛ serew; sɛ wɔn atemmu du so a, wɔbɛyera.
16 Koma Yehova amene ndi Cholowa cha Yakobo sali ngati mafanowo. Iyeyu ndi Mlengi wa zinthu zonse kuphatikizapo Israeli, mtundu umene anawusankha kuti ukhale anthu ake. Dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse.
Nea ɔyɛ Yakob Kyɛfa no nte sɛ eyinom, efisɛ ɔno ne ade nyinaa Yɛfo a Israel, abusua a ɛyɛ nʼagyapade nso ka ho, Asafo Awurade ne ne din.
17 Sonkhanitsani katundu wanu, inu amene mukukhala mʼlinga la ankhondo.
Mommoaboa mo ahode ano mfi asase no so, mo a motete nkurow a wɔatua wɔn ano mu.
18 Pakuti Yehova akuti, “Tsopano Ine ndidzachotsa anthu onse amene akukhala mʼdziko lino; adzakhala pa mavuto mpaka adzamvetsa.”
Na sɛɛ na Awurade se: “Saa bere yi mɛtow wɔn a wɔtete asase yi so agu; mede amanehunu bɛba wɔn so sɛnea wɔbɛfa wɔn nnommum.”
19 Aliyense ankangoti, “Mayo ine, chifukwa cha kupweteka kwanga! Chilonda changa nʼchachikulu!” Koma ine ndinkaganiza kuti, “Ndithu, ili ndi vuto langa basi, choncho ndingolipirira.”
Me pira yi nti minnue, mʼapirakuru yɛ akisikuru! Nanso mehyɛɛ me ho den sɛ, “Eyi ne me yare, na ɛsɛ sɛ mimia mʼani.”
20 Tenti yanga yawonongeka, zingwe zake zonse zaduka. Ana anga andisiya ndipo kulibenso. Palibenso amene adzandimangire tenti, kapena kufunyulula nsalu yake.
Wɔasɛe me ntamadan; wɔatwitwa nʼahama nyinaa mu. Wɔafa me mma nyinaa kɔ a merenhu wɔn bio; anka obiara a obesi me ntamadan anaa obesiesie me suhyɛ.
21 Abusa ndi opusa ndipo sanapemphe nzeru kwa Yehova; choncho palibe chimene anapindula ndipo nkhosa zawo zonse zabalalika.
Nguanhwɛfo no yɛ adwenharefo wommisa Awurade akyi kwan; ɛno nti wɔnkɔ so na wɔn nguankuw no abɔ ahwete.
22 Tamvani! kukubwera mphekesera, phokoso lalikulu la gulu la a ankhondo likumveka kuchokera kumpoto! Lidzasandutsa bwinja mizinda ya ku Yuda, malo okhala nkhandwe.
Muntie! Amanneɛ no reba, basabasayɛ kɛse a efi atifi fam asase bi so! Ɛbɛma Yuda nkurow ada mpan, na ayɛ sakraman atu.
23 Inu Yehova, ndikudziwa kuti moyo umene munthu ali nawo si wake; munthuyo sangathe kuwongolera mayendedwe ake.
Awurade, minim sɛ, onipa nkwa nyɛ ne de; na ɛnyɛ onipa na ɔkyerɛkyerɛ nʼanammɔntu.
24 Inu Yehova, langizeni, komatu mwachilungamo, osati ndi mkwiyo wanu, mungandiwononge kotheratu.
Teɛ me so, Awurade, wɔ trenee mu, mfi wʼabufuw mu nyɛ; anyɛ saa a wobɛdwerɛw me.
25 Tsanulirani ukali wanu pa mitundu ya anthu amene sakudziwani, ndiye kuti mitundu ya anthu amene satama pa dzina lanu mopemba. Iwo aja anasakaza Yakobo; amusakaza kotheratu ndipo awononga dziko lake.
Hwie wʼabufuwhyew no gu amanaman a wonnye wo nto mu no so, nnipa a wɔmmɔ wo din no so. Efisɛ, wɔasɛe Yakob wɔasɛe no koraa na wɔasɛe nʼasase a wɔwoo no too so no.

< Yeremiya 10 >