< Yesaya 64 >

1 Inu Yehova, bwanji mukanangongʼamba mlengalenga ndi kutsika pansi, kuti mapiri agwedezeke pamaso panu!
Mad ibar polo mondo ilor piny, mondo gode otetni e nyimi,
2 Monga momwe moto umatenthera tchire ndiponso kuwiritsa madzi, tsikani kuti adani anu adziwe dzina lanu, ndiponso kuti mitundu ya anthu injenjemere pamaso panu.
mana kaka mach wangʼo yugi kendo yienyo pi, lor piny mondo wasiki ongʼe ni intie, kendo imi ogendini otetni e nyimi!
3 Pakuti nthawi ina pamene munatsika munachita zinthu zoopsa zimene sitinaziyembekezere, ndipo mapiri anagwedezeka pamaso panu.
Nimar kane itimo gik madongo mane ok wapar, ne ilor piny ma gode ne oyiengni e nyimi,
4 Chikhalire palibe ndi mmodzi yemwe anamvapo kapena kuona Mulungu wina wonga Inu, amene amachitira zinthu zotere amene amadikira pa Iye.
nyaka aa nene onge ngʼama osewinjo, kendo onge it mosewinjo, bende onge wangʼ moseneno Nyasaye moro amora ma ok in, moserito joge mogeno kuome.
5 Inu mumabwera kudzathandiza onse amene amakondwera pochita zolungama, amene amakumbukira njira zanu. Koma Inu munakwiya, ife tinapitiriza kuchimwa. Kodi nanga tingapulumutsidwe bwanji?
Ikonyo joma nigi mor mar timo gik makare, ma gin joma paro yoregi. To kane wadhi nyime gi ketho e nyimi, to iyi nowangʼ. To koro ere kaka inyalo reswa?
6 Tonsefe takhala ngati anthu amene ndi odetsedwa, ndipo ntchito zathu zili ngati sanza za msambo; tonse tafota ngati tsamba, ndipo machimo athu akutiwuluzira kutali ngati mphepo.
Waduto wasebedo ka jok mogak, kendo timbewa duto mabeyo chalo mana gi lewni mochido; waduto wasener mana ka it oboke, kendo richowa mamono kwadhowa oko mabor mana ka yamo.
7 Palibe amene amapemphera kwa Inu kutekeseka kuti apemphe chithandizo kwa Inu; pakuti mwatifulatira ndi kutisiya chifukwa cha machimo athu.
Onge ngʼato angʼata maluongo nyingi, kata matemo mondo opadre kuomi, nimar isepandonwa wangʼi kendo ijwangʼowa mabor nikech richo magwa.
8 Komabe, Inu Yehova ndinu Atate athu. Ife ndife chowumba, Inu ndinu wowumba; ife tonse ndi ntchito ya manja anu.
Kata kamano, yaye Jehova Nyasaye, in e Wuonwa. Wan e lop chwech, to ine jachwechwa; kendo wan duto wan tich lweti.
9 Inu Yehova, musatikwiyire kopitirira muyeso musakumbukire machimo athu mpaka muyaya. Chonde, mutiganizire, ife tikupempha, pakuti tonsefe ndi anthu anu.
Yaye Jehova Nyasaye, kik ibed gi mirima mokadho apima, kik ipar richowa ndalo duto. Yaye Jehova Nyasaye, wakwayi, yie irangwa, nimar wan duto wan jogi.
10 Mizinda yanu yopatulika yasanduka chipululu; ngakhaletu Ziyoni wasanduka chipululu, Yerusalemu ndi wamasiye.
Miechi madongo maler olokore thim, kata mana Sayun owuon bende olokore thim, kendo Jerusalem odongʼ gunda.
11 Nyumba yanu yopatulika ndi yaulemu, kumene makolo athu ankakutamandani, yatenthedwa ndi moto ndipo malo onse amene tinkawakonda asanduka bwinja.
Hekalu marwa maler, kendo man-gi duongʼ mane kwerewa opakie, osewangʼ gi mach, kendo mwanduwa duto osekethore.
12 Inu Yehova, zonse zachitikazi, kodi mungokhala osatithandiza? Kodi mudzapitirizabe kukhala chete ndi kutilangabe mopitirira muyeso?
Bangʼ magi duto, yaye Jehova Nyasaye, bende pod inyalo mana jwangʼowa? Adier dilingʼ thi kikumowa mokadho apima?

< Yesaya 64 >