< Yesaya 63 >
1 Kodi ndani uyo akubwera kuchokera ku Edomu, atavala zovala za ku Bozira za madontho ofiira? Kodi uyu ndani, amene wavala zovala zokongola, akuyenda mwa mphamvu zake? “Ndi Ineyo, woyankhula zachilungamo ndiponso wamphamvu zopulumutsa.”
O WAI keia e hele mai nei, mai Edoma mai? Me ka aahu i hooluuulaia, mai Bozera mai? O keia mea hoi i nani kona lole komo, E hele ana me ka manomano o kona ikaika? Owau, ka mea hai i ka pono, ka mea mana loa i ka hoola.
2 Nanga bwanji zovala zanu zili psuu, ngati za munthu wofinya mphesa?
No ke aha la i ulaula ai kou lole komo, A like hoi kou lole komo, me ka mea hahi maloko o kahi kaomi waina?
3 “Ndapondereza ndekha anthu a mitundu ina ngati mphesa, palibe ndi mmodzi yemwe anali nane. Ndinawapondereza ndili wokwiya ndipo ndinawapondereza ndili ndi ukali; magazi awo anadothera pa zovala zanga, ndipo zovala zanga zonse zinathimbirira.
Ua hahi no wau i kahi kaomi waina, owau wale, Aohe mea o na kanaka pu me au. E hehi no wau ia lakou i ko'u ukiuki, E hahahi no wau ia lakou i ko'u inaina. E kapipi no ko lakou koko i ko'u mau lole komo, A hoopalahea no wau i ko'u aahu a pau.
4 Pakuti ndinatsimikiza mu mtima mwanga kuti lafika tsiku lolipsira anthu anga; ndipo chaka cha kuwomboledwa kwanga chafika.
No ka mea, aia no iloko o ko'u naau ka la o ka hoopai ana, Ua hiki mai hoi ka makahiki o ko'u poe hoolapanaiia.
5 Ndinayangʼana ndipo panalibe munthu wondithandiza. Ndinadabwa kwambiri kuti panalibe wondichirikiza; choncho ndinapambana ndi mphamvu zanga, ndipo mkwiyo wanga unandilimbitsa.
Nana aku la au, aohe mea nana e kokua; A haohao iho la au, no ka mea ole nana e koo: Nolaila, na ko'u lima no i hoola no'u iho, A o kuu inaina, oia ka i koo mai ia'u.
6 Ndinapondereza mitundu ya anthu ndili wokwiya; ndipo ndinawasakaza ndipo ndinathira magazi awo pansi.”
Ua hahi no au i na kanaka ilalo i kuu ukiuki, Ua haawi aku no au e ona lakou i ko'u inaina, A hoohaahaa au i ko lakou koko ilalo a ka honua.
7 Ndidzafotokoza za kukoma mtima kwa Yehova, ntchito zimene Iye ayenera kutamandidwa. Ndidzatamanda Yehova chifukwa cha zonse zimene watichitira. Inde, mwa chifundo ndi kukoma mtima kwake Yehova wachitira nyumba ya Israeli zinthu zabwino zambiri.
O ke aloha o Iehova ka'u o hoikeike aku ai, O na mea nani hoi o Iehova, E like me na mea a pau a Iehova i hana mai ai ia makou, A me ka lokomaikai nui i ko ka hale o Iseraela, Ka mea ana i hana mai ai, ma kona lokomaikai, A ma ka nui loa hoi o kona aloha.
8 Yehova anati, “Ndithu awa ndi anthu anga, ana anga amene sadzandinyenga Ine.” Choncho anawapulumutsa.
No ka mea, olelo mai no oia, He oiaio, o ko'u poe kanaka lakou, he poe keiki wahahee ole; Nolaila oia i lilo ai i mea hoola no lakou.
9 Iyenso anasautsidwa mʼmasautso awo onse, ndipo mngelo wochokera kwa Iye anawapulumutsa. Mwa chikondi ndi chifundo chake iye anawapulumutsa, anawanyamula ndikuwatenga kuyambira kale lomwe.
I ko lakou popilikia a pau, aole ia he enemi, Aka, na ka anela o kona alo lakou i hoola; A no kona aloha, a no kona lokomaikai, hoolapanai oia ia lakou; A hapai ae la oia, a kaikai aku la ia lakou, i na la a pau o ka wa kahiko.
10 Komabe iwo anawukira ndi kumvetsa chisoni Mzimu Woyera. Motero Yehova anatembenuka nakhala mdani wawo ndipo Iye mwini anamenyana nawo.
Aka, kipi no lakou, a hoeha aku la i kona Uhane Hemolele; Nolaila oia i huli ai i enemi no lakou, A kaua mai no hoi ia lakou.
11 Pamenepo anthu ake anakumbukira masiku amakedzana, masiku a Mose mtumiki wake; ndipo anafunsa kuti, “Ali kuti Yehova amene anawawolotsa pa nyanja, pamodzi ndi Mose mʼbusa wawo? Ali kuti Iye amene anayika Mzimu Woyera pakati pawo?
Alaila, hoomanao iho la kona poe kanaka i na la kahiko ia Mose, Auhea ka mea nana lakou i lawe, mai loko mai o ke kai, Me ke kahu ohana hipa? Auhea hoi ka mea nana i waiho i kona Uhane Hemolele iwaenakonu ona?
12 Ali kuti amene anachita zinthu zodabwitsa ndi mphamvu zake zazikulu kudzera mwa Mose? Ali kuti amene anagawa madzi pa nyanja anthu ake akuona, kuti dzina lake limveke mpaka muyaya,
Ka mea i alakai ia lakou me ka lima akau o Mose, O ka lima no ia o kona nani, Ka mea i hookaawale i ka wai imua o ko lakou alo, I mea e hookaulana mau loa ia'i kona inoa?
13 amene anawayendetsa pa nyanja yozama? Monga kavalo woyendayenda mʼchipululu, iwo sanapunthwe;
E alakai ana ia lakou maloko o ka hohonu, E like me ka lio ma ka waoakua, I ole lakou e kulanalana?
14 Mzimu Woyera unawapumulitsa ngati mmene ngʼombe zimapumulira. Umu ndi mmene Inu munatsogolera anthu anu kuti dzina lanu lilemekezeke.”
E like me ka bipi, i iho ilalo i kahawai, Pela no i hoomaha ai ka Uhane o Iehova ia ia; Pela hoi kau i alakai ai i kou poe kanaka, I mea e hana'i i inoa kaulana loa nou.
15 Inu Yehova amene muli kumwambako, pa mpando wanu wolemekezeka, wopatulika ndi waulemerero, tiyangʼaneni ife. Kodi changu chanu ndi mphamvu zanu zili kuti? Simukutionetsanso kukoma mtima kwanu ndi chifundo chanu.
E nana mai oe, mai ka lani mai, E ike mai hoi, mai kahi noho ai o kou pono, a me kou hanohano; Auhea kou manao nui ana, a me kou ikaika? Ke kani ana o kou opu, a me kou aloha ia'u? Ua uumiia anei ia?
16 Koma Inu ndinu Atate athu, ngakhale Abrahamu satidziwa kapena Israeli kutivomereza ife; Inu Yehova, ndinu Atate athu, kuyambira kale dzina lanu ndinu Mpulumutsi wathu.
He oiaio no, o oe no ko makou Makua, Aole nae i ike mai o Aberahama ia makou, Aole hoomaopopo mai o Iseraela ia makou; O oe, o Iehova no ko makou Makua, a me ko makou Hoolapanai, Mai ka wa kahiko loa mai no kou inoa.
17 Chifukwa chiyani, Inu Yehova, mukutisocheretsa pa njira zanu? Bwanji mukutilola kuti tikhale owuma mitima kotero kuti sitikukuopaninso? Bwererani chifukwa cha atumiki anu; mafuko a anthu amene ali cholowa chanu.
E Iehova, no ke aha la oe i hooauwana ia makou mai kou mau aoao aku? A ua hoopaakiki hoi i ko makou naau, i makau ole aku ai ia oe? E hoi mai oe, no kau mau kauwa, A no na ohana o kou hooilina.
18 Anthu anu atangokhala pa malo anu opatulika pa kanthawi kochepa, adani athu anasakaza malo anu opatulika.
Ua noho iki wale no kou poe kanaka laa, Ua hahi ko makou poe enemi maluna o kou wahi hoano.
19 Ife tili ngati anthu amene simunawalamulirepo ngati iwo amene sanakhalepo anthu anu.
Mai ka wa kahiko mai makou; Aole noho alii oe maluna o lakou, Ka poe i kapa ole ia ma kou inoa.