< Yesaya 63 >
1 Kodi ndani uyo akubwera kuchokera ku Edomu, atavala zovala za ku Bozira za madontho ofiira? Kodi uyu ndani, amene wavala zovala zokongola, akuyenda mwa mphamvu zake? “Ndi Ineyo, woyankhula zachilungamo ndiponso wamphamvu zopulumutsa.”
Who? this - [is] coming from Edom red of garments from Bozrah this one [is] adorned in clothing his [is] stooping in [the] greatness of strength his I [am] speaking in righteousness great to save.
2 Nanga bwanji zovala zanu zili psuu, ngati za munthu wofinya mphesa?
Why? [does] redness [belong] to clothing your and [are] garments? your like [one who] treads in a winepress.
3 “Ndapondereza ndekha anthu a mitundu ina ngati mphesa, palibe ndi mmodzi yemwe anali nane. Ndinawapondereza ndili wokwiya ndipo ndinawapondereza ndili ndi ukali; magazi awo anadothera pa zovala zanga, ndipo zovala zanga zonse zinathimbirira.
[the] winepress - I have trodden to alone me and from peoples not anyone [was] with me and I trod them in anger my and I trampled them in rage my and it spattered blood their on garments my and all clothes my I have defiled.
4 Pakuti ndinatsimikiza mu mtima mwanga kuti lafika tsiku lolipsira anthu anga; ndipo chaka cha kuwomboledwa kwanga chafika.
For a day of vengeance [was] in heart my and [the] year of redemption my it had come.
5 Ndinayangʼana ndipo panalibe munthu wondithandiza. Ndinadabwa kwambiri kuti panalibe wondichirikiza; choncho ndinapambana ndi mphamvu zanga, ndipo mkwiyo wanga unandilimbitsa.
And I may look and there not [was] a helper and I may be appalled and there not [was] a sustainer and it gave victory to me arm my and rage my it it sustained me.
6 Ndinapondereza mitundu ya anthu ndili wokwiya; ndipo ndinawasakaza ndipo ndinathira magazi awo pansi.”
And I may tread down peoples in anger my and I made drunk them in rage my so I may bring down to the ground blood their.
7 Ndidzafotokoza za kukoma mtima kwa Yehova, ntchito zimene Iye ayenera kutamandidwa. Ndidzatamanda Yehova chifukwa cha zonse zimene watichitira. Inde, mwa chifundo ndi kukoma mtima kwake Yehova wachitira nyumba ya Israeli zinthu zabwino zambiri.
[the] covenant loyalti of Yahweh - I will bring to remembrance [the] praises of Yahweh as on all that he has dealt out to us Yahweh and [the] greatness of goodness to [the] house of Israel which he has dealt out to them according to compassion his and according to [the] greatness of covenant loyalti his.
8 Yehova anati, “Ndithu awa ndi anthu anga, ana anga amene sadzandinyenga Ine.” Choncho anawapulumutsa.
And he said surely [are] people my they children [who] not they will deal falsely and he became of them a deliverer.
9 Iyenso anasautsidwa mʼmasautso awo onse, ndipo mngelo wochokera kwa Iye anawapulumutsa. Mwa chikondi ndi chifundo chake iye anawapulumutsa, anawanyamula ndikuwatenga kuyambira kale lomwe.
In all distress their - ([belonged] to him *Q(K)*) distress and [the] angel of presence his it saved them in love his and in mercy his he he redeemed them and he lifted up them and he carried them all [the] days of antiquity.
10 Komabe iwo anawukira ndi kumvetsa chisoni Mzimu Woyera. Motero Yehova anatembenuka nakhala mdani wawo ndipo Iye mwini anamenyana nawo.
And they they rebelled and they grieved [the] spirit of holiness his and he changed himself of them into an enemy he he fought against them.
11 Pamenepo anthu ake anakumbukira masiku amakedzana, masiku a Mose mtumiki wake; ndipo anafunsa kuti, “Ali kuti Yehova amene anawawolotsa pa nyanja, pamodzi ndi Mose mʼbusa wawo? Ali kuti Iye amene anayika Mzimu Woyera pakati pawo?
And it remembered [the] days of antiquity Moses people his where? - [is] who brought up them from [the] sea with [the] shepherds of flock his where? [is] the [one who] put in midst its [the] spirit of holiness his.
12 Ali kuti amene anachita zinthu zodabwitsa ndi mphamvu zake zazikulu kudzera mwa Mose? Ali kuti amene anagawa madzi pa nyanja anthu ake akuona, kuti dzina lake limveke mpaka muyaya,
[who] caused to go To [the] right [hand] of Moses [the] arm of splendor his [who] split open [the] waters from before them to make for himself a name of perpetuity.
13 amene anawayendetsa pa nyanja yozama? Monga kavalo woyendayenda mʼchipululu, iwo sanapunthwe;
[who] caused to walk Them in the deeps like horse in the wilderness not they stumbled.
14 Mzimu Woyera unawapumulitsa ngati mmene ngʼombe zimapumulira. Umu ndi mmene Inu munatsogolera anthu anu kuti dzina lanu lilemekezeke.”
Like livestock [which] in the valley it goes down [the] spirit of Yahweh it gave rest it so you led people your to make for yourself a name of splendor.
15 Inu Yehova amene muli kumwambako, pa mpando wanu wolemekezeka, wopatulika ndi waulemerero, tiyangʼaneni ife. Kodi changu chanu ndi mphamvu zanu zili kuti? Simukutionetsanso kukoma mtima kwanu ndi chifundo chanu.
Look from heaven and see from [the] lofty abode of holiness your and splendor your where? [are] zeal your and mighty deeds your [the] tumult of inward parts your and compassion your to me they have restrained themselves.
16 Koma Inu ndinu Atate athu, ngakhale Abrahamu satidziwa kapena Israeli kutivomereza ife; Inu Yehova, ndinu Atate athu, kuyambira kale dzina lanu ndinu Mpulumutsi wathu.
For you [are] father our for Abraham not he knows us and Israel not he acknowledges us you O Yahweh [are] father our [is] redeemer our from long ago name your.
17 Chifukwa chiyani, Inu Yehova, mukutisocheretsa pa njira zanu? Bwanji mukutilola kuti tikhale owuma mitima kotero kuti sitikukuopaninso? Bwererani chifukwa cha atumiki anu; mafuko a anthu amene ali cholowa chanu.
Why? do you make wander us O Yahweh from ways your do you harden? heart our from fear of you return for [the] sake of servants your [the] tribes of inheritance your.
18 Anthu anu atangokhala pa malo anu opatulika pa kanthawi kochepa, adani athu anasakaza malo anu opatulika.
For little while they possessed [the] people of holiness your opponents our they have trodden down sanctuary your.
19 Ife tili ngati anthu amene simunawalamulirepo ngati iwo amene sanakhalepo anthu anu.
We have been from long ago not you ruled over them not it was called name your on them