< Yesaya 6 >

1 Chaka chimene mfumu Uziya anamwalira, ndinaona Ambuye atakhala pa mpando waufumu, wautali ndi wokwezedwa, ndipo mkanjo wawo unali wautali; kotero kuti unadzaza mʼNyumba ya Yehova.
Ke yac se Tokosra Uzziah el misa, nga liye LEUM GOD. El muta fin tron lal, loangyak ac akfulatyeyuk, ac nuknuk loeloes lal nwakla in Tempul uh nufon.
2 Pamwamba pawo panayimirira Aserafi, aliyense anali ndi mapiko asanu ndi limodzi: awiri anaphimba nkhope zawo, awiri anaphimba mapazi awo, ndipo awiri ankawulukira.
Oasr seraph apnulla, ac kais sie selos oasr posohksok onkosr kac. Kais sie seraph afinya mutal ke luo pao ah, ac afinya manol ke luo, ac el sohksok ke ma luo lula.
3 Ndipo Aserafiwo amafuwulirana kuti “Woyera, woyera, woyera Yehova Wamphamvuzonse. Dziko lonse lapansi ladzaza ndi ulemerero wake.”
Elos apangoni sie nu sin sie, ac fahk: “Mutal, mutal, mutal! LEUM GOD Kulana El mutal! Wolana lal nwakla faclu.”
4 Chifukwa cha kufuwulako maziko a zitseko ndi ziwundo anagwedezeka ndipo mʼNyumba ya Yehova munadzaza utsi.
Pusraclos mokleak pwelung ke sru in mutunoa ke Tempul uh, ac in Tempul uh sessesla ke kulasr.
5 Tsono ine ndinafuwula kuti, “Tsoka langa ine! Ndatayika! Pakuti ndine munthu wapakamwa poyipa, ndipo ndimakhala pakati pa anthu a pakamwa poyipa, ndipo ndi maso anga ndaona mfumu Yehova Wamphamvuzonse.”
Na nga fahk, “Wanginla finsrak luk! Nga ac sun ongoiya lulap, mweyen kas nukewa ma fahla liki ngoasrok uh fohkfok, ac nga muta inmasrlon mwet ma kas nukewa la uh fohkfok. Ne ouinge, a nga liye Tokosra, LEUM GOD Kulana, ke mutuk sifacna.”
6 Pomwepo mmodzi mwa Aserafi aja anawulukira kwa ine ali ndi khala lamoto mʼdzanja lake, khala limene analichotsa ndi mbaniro pa guwa lansembe.
Na sie sin seraph inge sohkma nu yuruk. El us ipin mulut firir se ma el tuh sang sruhf se srukak liki loang uh.
7 Ndipo anandikhudza pakamwa panga ndi khala lamotolo nati, “Taona ndakhudza pa milomo yako ndi khalali; kulakwa kwako kwachotsedwa, machimo ako akhululukidwa.”
El sang mulut firir sac pusralla ngoasrok ac fahk, “Ma se inge pusralla ngoasrom, ac inge ma sufal lom wanginla, ac ma koluk lom nunak munas nu sum.”
8 Kenaka ndinamva mawu a Ambuye akuti, “Kodi ndidzatuma yani? Ndipo ndani adzapite mʼmalo mwathu?” Ndipo ine ndinati, “Ndilipo. Tumeni!”
Na nga lohng Leum El fahk, “Su nga ac supwala uh? Su ac som kacsr uh?” Na nga topuk, “Nga inge! Supweyula!”
9 Yehova anati, “Pita ndipo ukawawuze anthu awa: “‘Kumva muzimva, koma osamvetsetsa; kupenya muzipenya koma osaona kanthu.’
Ouinge El fahk nu sik, “Som ac tafweang kas inge nu sin mwet uh: Kowos finne sikalani in lohng, kowos ac tia kalem. Kowos finne suiya na, kowos ac tia etu kalmac.”
10 Tsono anthu amenewa uwaphe mtima; uwagonthetse makutu, ndipo uwatseke mʼmaso. Mwina angaone ndi maso awo, angamve ndi makutu awo, angamvetse ndi mitima yawo, kenaka ndi kutembenuka mtima ndi kuchiritsidwa.”
Na El fahk nu sik, “Orala nunak lun mwet inge in afon, insraclos in sulohngkas, ac mutalos in kun, tuh elos fah tia ku in liye ku lohng ku kalem. Mweyen elos funu ku, elos lukun forma nu sik ac akkeyeyukla.”
11 Pamenepo ine ndinati, “Zimenezo ndi mpaka liti Inu Ambuye?” Ndipo Iyeyo anandiyankha kuti, “Mpaka mizinda itasanduka mabwinja nʼkusowa wokhalamo, mpaka nyumba zitasowa anthu okhalamo, mpaka dziko litasanduka chipululu ndithu,
Ac nga siyuk, “Leum, ac ouingan putaka?” Ac El topuk, “Nwe ke na siti nukewa musalla, ac wanginla ma we — nwe ke wanginna mwet muta in lohm inge — nwe ke facl sac oan mwesisla.
12 mpaka Yehova atasamutsira aliyense kutali, dziko nʼkusiyidwa kwathunthu.
Nga fah supwala mwet uh nu yen loessula, ac oru facl sac nufon in pisala.
13 Ndipo ngakhale chigawo chakhumi cha anthu chitatsala mʼdziko, nachonso chidzawonongedwa. Koma monga momwe mitengo ya muwanga ndi thundu imasiyira chitsa pamene ayidula, chonchonso mbewu yoyera idzatsalira ngati chitsa chotsala mʼdziko.”
Finne mwet se inmasrlon mwet singoul pa lula muta in facl se inge, el ac fah kunausyukla pac. El ac fah oana sie sruen sak oak ma pakpuki.” (Kalmen sruen sak sac pa sie mutawauk sasu nu sin mwet lun God.)

< Yesaya 6 >