< Yesaya 54 >

1 “Sangalala, iwe mayi wosabala, iwe amene sunabalepo mwana; imba nyimbo, ndi kufuwula mwachimwemwe, iwe amene sunamvepo ululu wa pobereka; chifukwa mkazi wosiyidwa adzakhala ndi ana ambiri kuposa mkazi wokwatiwa,” akutero Yehova.
Caya nu loh tamhoe laeh, aka cun noek pawt long khaw tamlung neh rhong saeh, aka vawn pawt khaw hlampan saeh. BOEIPA loh, “Rhukom kah a ca rhoek lakah aka pong kah a ca ping ngai coeng,” a ti.
2 Kulitsa malo omangapo tenti yako, tambasula kwambiri nsalu zake, usaleke; talikitsa zingwe zako, limbitsa zikhomo zako.
Na dap hmuen te aek lamtah na dungtlungim kah himbaiyan khaw yueng dae. Na liva hlawt ham khaw tuemsoem boel lamtah na hlingcong te caang sak.
3 Pakuti udzasendeza malire ako kumanja ndi kumanzere; ndipo zidzukulu zako zidzalanda dziko la anthu a mitundu ina ndipo zidzakhala mʼmizinda yawo yosiyidwa.
Banvoei bantang la na pungtai vetih na tiingan loh namtom te a pang. Te vaengah khopuei aka pong ah khaw kho a sak uh ni.
4 “Usachite mantha; sadzakunyozanso. Usakhumudwe; sudzapeputsidwanso. Udzayiwala za manyazi zimene zinakuchitikira nthawi ya unyamata wako ndipo za manyazi zimene zinakuchitikira pa nthawi ya umasiye wako sudzazikumbukanso.
Rhih boeh, yah na pok mahpawh. Hmaithae na lo pawt vetih na hmai tal mahpawh. Na cacawn vaengkah yahpohnah na hnilh bitni. Na nuhmai vaengkah kokhahnah khaw na poek voel mahpawh.
5 Pakuti Mlengi wako ali ngati mwamuna wako, dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse. Woyerayo wa Israeli ndiye Mpulumutsi wanu; dzina lake ndi Mulungu wa dziko lonse lapansi.
Nang aka yuu nah tih nang aka saii kah a ming tah caempuei BOEIPA ni. Nang aka tlan, Israel kah a cim tah diklai pum kah Pathen la a khue.
6 Yehova wakuyitananso, uli ngati mkazi wosiyidwa ndi wodzaza ndi chisoni mu mtima, mkazi amene anakwatiwa pa unyamata wake kenaka nʼkukanidwa,” akutero Mulungu wako.
A hnoo uh dongah mueihla ngaihlih nu bangla nang te BOEIPA loh ng'khue ni. Te dongah na camoe kah na Pathen loh, “Na yuu te khaw a hnawt,” a ti.
7 “Kwa kanthawi kochepa, Ine ndinakusiya, koma ndidzakutenganso chifukwa ndimakukonda kwambiri.
Mikhaptok ca nang kan hnoo dae haidamnah neh a tanglue la nang kan coi bitni.
8 Ndinakufulatira kwa kanthawi kochepa ndili wokwiya kwambiri. Koma ndi kukoma mtima kwanga kwa muyaya, ndidzakuchitira chifundo,” akutero Yehova Mpulumutsi wako.
“Thinhul tuiphul vaengah tah ka maelhmai he nang taeng lamloh mikhaptok ah ka thuh coeng dae kumhal kah sitlohnah neh nang kan haidam,” tila nang aka tlan Yahovah loh a thui.
9 “Kwa ine zimenezi zili ngati mmene zinalili mʼnthawi ya Nowa. Monga ndinalumbira nthawi imeneyo kuti sindidzawononganso dziko lapansi ndi madzi. Kotero tsopano ndalumbira kuti sindidzakupseraninso mtima, sindidzakudzudzulaninso.
Kai ham tah tahae kah he Noah kah tui van pawn ni. Noah tui loh a khuk vaengah diklai ham ka toemngam te nang taengkah ka thintoek ah ni ka toemngam tih nang kan tluung.
10 Ngakhale mapiri atagwedezeka ndi zitunda kusunthidwa, koma chikondi changa chosasinthika pa iwe sichidzatha. Pangano langa lamtendere silidzasintha,” akutero Yehova amene amakuchitira chifundo.
“Tlang rhoek te nong uh tih som rhoek ke tuen uh cakhaw kai kah sitlohnah he nang taeng lamloh nong mahpawh. Kai kah rhoepnah paipi tah tuen mahpawh,” tila nang aka haidam BOEIPA loh a thui.
11 “Iwe mzinda wozunzika, wokunthidwa ndi namondwe ndiponso wopanda wokutonthoza, Ine ndidzakongoletsa miyala yako. Maziko ako ndidzamanga ndi miyala ya safiro.
Mangdaeng loh a thikthuek khaw damti pawh. Kai loh namah kah canglung lungto neh kan kol sak dongah minhum dongah nang kan hol bitni.
12 Ndidzamanga nsanja zako zankhondo ndi miyala yokongola ya rubi. Ndidzamanga zipata zako ndi miyala yonyezimira ngati moto, ndipo linga lako lonse lidzakhala la miyala yamtengowapatali.
Na puthue te aithilung, na vongka te hmaihli lungto neh, na khorhi boeih te danngaih lungto neh kan saii ni.
13 Yehova adzaphunzitsa ana ako onse, ndipo ana ako adzakhala ndi mtendere wochuluka.
Na ca rhoek te BOEIPA loh boeih a lolmang thil vetih na ca rhoek kah rhoepnah khaw ping ni.
14 Udzakhazikika mʼchilungamo chenicheni: Sudzakhalanso wopanikizika, chifukwa sudzaopa kanthu kalikonse. Sudzakhalanso ndi mantha chifukwa manthawo sadzafika pafupi ndi iwe.
Duengnah dongah n'cikngae sak vetih, hnaemtaeknah lamloh na lakhla pawn ni. Na rhih voel pawt vetih porhaknah khaw nang taengla ha pawk voel mahpawh.
15 Ngati wina adzakuthirani nkhondo, si ndine amene ndachititsa; aliyense amene adzalimbana nanu adzagonja chifukwa cha iwe.
A mae la aka mae te khaw kai lamkah moenih he. Nang aka mae te khaw namah taengah cungku bitni.
16 “Taona, ndi Ine amene ndinalenga munthu wosula zitsulo amene amakoleza moto wamakala ndi kusula zida zoti azigwiritse ntchito. Ndipo ndine amene ndinalenga munthu wosakaza kuti awononge;
Hmaisa-aek hmai aka hmut kutthai khaw kamah long ni ka suen ne. A bisai te hnopai la a poeh sak akhaw laikoi sak ham kutcaihnah khaw kai loh ka suen pah coeng.
17 palibe chida chopangidwa ndi mdani chimene chidzakupweteke, ndipo onse okuneneza pa mlandu udzawatsutsa. Umu ndimo adzapezekere atumiki a Yehova. Chipambano chawo chichokera kwa Ine,” akutero Yehova.
Hnopai tom te nang taengah hlinsai cakhaw thaihtak mahpawh. Laitloeknah dongah ol cungkuem loh nang n'tlai thil cakhaw na boe mahpawh. BOEIPA kah olphong dongah tah tahae kah he BOEIPA sal rhoek kah rho neh kamah taeng lamkah duengnah la om.

< Yesaya 54 >

A Dove is Sent Forth from the Ark
A Dove is Sent Forth from the Ark