< Yesaya 54 >
1 “Sangalala, iwe mayi wosabala, iwe amene sunabalepo mwana; imba nyimbo, ndi kufuwula mwachimwemwe, iwe amene sunamvepo ululu wa pobereka; chifukwa mkazi wosiyidwa adzakhala ndi ana ambiri kuposa mkazi wokwatiwa,” akutero Yehova.
Yelusaleme! Di da aligime uda defele esalebe ba: i. Be wali di da gesami hea: musa: , amola hahawaneba: le wele sia: musa: dawa: Wali dia mano lalelegemu ili idi da uda amo egoa hame fisi ea mano ilia idi bagadewane baligimu.
2 Kulitsa malo omangapo tenti yako, tambasula kwambiri nsalu zake, usaleke; talikitsa zingwe zako, limbitsa zikhomo zako.
Dia abula diasu amo bu bagade hamoma. Ea efe amo sedagimu amola ea ifa goge bugi amo bu gasa bagade hahamoma.
3 Pakuti udzasendeza malire ako kumanja ndi kumanzere; ndipo zidzukulu zako zidzalanda dziko la anthu a mitundu ina ndipo zidzakhala mʼmizinda yawo yosiyidwa.
Dia alalo defei la: ididili huluane amo mugululi bu bagade hamoma. Wali ga fi da dia sogega esala. Be dilia amo soge bu samogemu. Moilai wali amo ganodini dunu da hamedafa gala, amo da bu dunuga nabai dagoi ba: mu.
4 “Usachite mantha; sadzakunyozanso. Usakhumudwe; sudzapeputsidwanso. Udzayiwala za manyazi zimene zinakuchitikira nthawi ya unyamata wako ndipo za manyazi zimene zinakuchitikira pa nthawi ya umasiye wako sudzazikumbukanso.
Mae beda: ma! Di da gogosiasu bu hame ba: mu. Di da gaheabolo gawa fili baligi fa: su hamoi amo gogolemu. Amola di da didalo agoane esalebeba: le se bagade nabi, amo amola di da gogolemu.
5 Pakuti Mlengi wako ali ngati mwamuna wako, dzina lake ndi Yehova Wamphamvuzonse. Woyerayo wa Israeli ndiye Mpulumutsi wanu; dzina lake ndi Mulungu wa dziko lonse lapansi.
Dia Hahamosu dunu da dima digua agoane ba: mu. Ea dio da Hina Gode Bagadedafa. Isala: ili fi ilia Hadigi Gode da di gaga: mu. Bai E da osobo bagade amoma Hina bagade.
6 Yehova wakuyitananso, uli ngati mkazi wosiyidwa ndi wodzaza ndi chisoni mu mtima, mkazi amene anakwatiwa pa unyamata wake kenaka nʼkukanidwa,” akutero Mulungu wako.
Isala: ili! Di da gaheabolo lai uda amo egoa da e fisiagaiba: le, se bagade naba, amo defele ba: sa. Be Hina Gode da Ema bu misa: ne, dima wele sia: sa.
7 “Kwa kanthawi kochepa, Ine ndinakusiya, koma ndidzakutenganso chifukwa ndimakukonda kwambiri.
E da amane sia: sa, “Na da fonobahadidafa wadofamusu di fisiagai. Be Na da bagade asigiwane di bu lamu.
8 Ndinakufulatira kwa kanthawi kochepa ndili wokwiya kwambiri. Koma ndi kukoma mtima kwanga kwa muyaya, ndidzakuchitira chifundo,” akutero Yehova Mpulumutsi wako.
Na da ougiba: le, fonobahadidafa dima Na baligi olelei. Be wali Na da Na asigidafa hou mae fisili, dima olelelalumu.” Hina Gode, dia gaga: su dunu, da amane sia: sa.
9 “Kwa ine zimenezi zili ngati mmene zinalili mʼnthawi ya Nowa. Monga ndinalumbira nthawi imeneyo kuti sindidzawononganso dziko lapansi ndi madzi. Kotero tsopano ndalumbira kuti sindidzakupseraninso mtima, sindidzakudzudzulaninso.
“Nowa: ea esoga Na da osobo bagade amo hano bagadega bu hame dedeboma: ne ilegele sia: i. Amola wali Na da dima bu hame ougimu amo Na da ilegele sia: sa. Na da dima bu gagabole hame sia: mu, amola dima se hame imunu.
10 Ngakhale mapiri atagwedezeka ndi zitunda kusunthidwa, koma chikondi changa chosasinthika pa iwe sichidzatha. Pangano langa lamtendere silidzasintha,” akutero Yehova amene amakuchitira chifundo.
Goumi ilia da ugugusia amola agolo da mugululi hamedafa ba: sea, be Na dima asigidafa hou da mae mugululi, dialalalumu. Na dima olofosu ima: ne ilegei, amo Na da hame gogolemu.” Hina Gode da amane sia: sa. E da dima asigidafa gala.
11 “Iwe mzinda wozunzika, wokunthidwa ndi namondwe ndiponso wopanda wokutonthoza, Ine ndidzakongoletsa miyala yako. Maziko ako ndidzamanga ndi miyala ya safiro.
Hina Gode da amane sia: sa, “Yelusaleme! Di da se bagade naba. Disu di gaga: mu da hame dawa: , amola eno dunu ilia dia dogo hame denesisa. Na da igi ida: iwane amoga dia bai bu gagumu.
12 Ndidzamanga nsanja zako zankhondo ndi miyala yokongola ya rubi. Ndidzamanga zipata zako ndi miyala yonyezimira ngati moto, ndipo linga lako lonse lidzakhala la miyala yamtengowapatali.
Na da dia diasu gado gagagula heda: i amo ‘lubi’ igi amoga gagumu. Dia logo ga: su, Na da igi amo da lalu agoane hadigi gala, amoga gagumu. Amola gagoi dobea da di sisiga: sa, amo Na da igi ida: iwanedafa amoga gagumu.
13 Yehova adzaphunzitsa ana ako onse, ndipo ana ako adzakhala ndi mtendere wochuluka.
Na Nisu da dia fi dunuma olelemu. Amola Na da ilima olofosu amola bagade gagui hou imunu.
14 Udzakhazikika mʼchilungamo chenicheni: Sudzakhalanso wopanikizika, chifukwa sudzaopa kanthu kalikonse. Sudzakhalanso ndi mantha chifukwa manthawo sadzafika pafupi ndi iwe.
Dilia da moloidafa hou lalegaguiba: le, gasawane lelumu. Dilia da gaga: i dagoi ba: beba: le, eno dunu da dilima se hame imunu amola dilia da beda: su hame ba: mu.
15 Ngati wina adzakuthirani nkhondo, si ndine amene ndachititsa; aliyense amene adzalimbana nanu adzagonja chifukwa cha iwe.
Nowa da dilima doagala: sea, ilia da Na hanaiga hame hamomu. Be nowa da dilima gegesea da dafamu.
16 “Taona, ndi Ine amene ndinalenga munthu wosula zitsulo amene amakoleza moto wamakala ndi kusula zida zoti azigwiritse ntchito. Ndipo ndine amene ndinalenga munthu wosakaza kuti awononge;
Na da ouli hahamosu dunu amo da lalu didili ouli gegesu liligi hamosa, Na da amo dunu hahamosa. Amola Na da dadi gagui dunu e da amo gegesu liligiga gegenana, Na da amo amola hahamosa.
17 palibe chida chopangidwa ndi mdani chimene chidzakupweteke, ndipo onse okuneneza pa mlandu udzawatsutsa. Umu ndimo adzapezekere atumiki a Yehova. Chipambano chawo chichokera kwa Ine,” akutero Yehova.
Be gegesu liligi afae da dilima se imunu hamedei ba: mu. Nowa da dilima diwaneya udidisia, dilia da ilima ilia sia: hedofamusa: bu adole imunu dawa: mu. Na da Na hawa: hamosu dunu gaga: mu amola hasalasu hou ilima imunu,” Hina Gode da amane sia: i dagoi.