< Yesaya 50 >

1 Yehova akuti, “Kalata imene ndinasudzulira amayi anu ili kuti? Kapena mwa anthu amene ndili nawo ngongole, ndinakugulitsani kwa ati? Inu munagulitsidwa ku ukapolo chifukwa cha machimo anu; amayi anu anachotsedwa chifukwa cha kulakwa kwanu.
LEUM GOD El fahk, “Ya kowos nunku mu nga supwala mwet luk in som likiyu Oana sie mukul su sisla mutan kial? Na, pia pwepu in fahsrelik an? Ya kowos nunku mu nga tuh kukakin kowos in akfalye soemoul luk, Oana sie mwet su kukakin tulik natul tuh elos in mwet kohs? Mo, kowos tuh som nu in sruoh ke sripen ma koluk lowos; Nga supwekowosla ke sripen orekma koluk lowos.
2 Nʼchifukwa chiyani pamene ndinabwera kudzakupulumutsani panalibe munthu? Pamene ndinayitana, nʼchifukwa chiyani panalibe wondiyankha? Kodi dzanja langa ndi lalifupi kuti nʼkulephera kukuwombolani? Kodi ndilibe mphamvu zokupulumutsirani? Ndi kudzudzula kokha ndinawumitsa nyanja yayikulu, mitsinje ndinayisandutsa chipululu; nsomba za mʼmenemo zinawola chifukwa chosowa madzi; ndipo zinafa ndi ludzu.
“Efu ku mwet luk uh tia porongeyu Ke nga som nu yorolos in molelos? Efu elos ku tia topuk pacl se nga pang? Mea, nga arulana munas in molelosla? Nga ku in akpaoyela meoa ke sap na luk, Ac oru tuh infacl uh in ekla nu ke acn mwesis, Na ik loac fah misa mweyen lisr kof.
3 Ndinaphimba thambo ndi mdima ndipo chiguduli chinakhala chofunda chake.”
Nga ku in oru yen engyeng uh in lohsrla, In oana elan asor ke sie mwet misa.”
4 Ambuye Yehova anandiphunzitsa mawu oyenera kuyankhula kudziwa mawu olimbitsa mtima anthu ofowoka. Mmawa mulimonse amandidzutsa, amathwetsa khutu langa kuti ndimve monga amachitira munthu amene akuphunzira.
LEUM GOD Fulatlana El lutiyu ma nga in fahk, Tuh nga in ku in akkeye mwet munas. Lotutang nukewa El oru nga in kena Tari lohng ma El ac lutiyu kac.
5 Ambuye Yehova wanditsekula makutu anga, ndipo sindinakhale munthu wowukira ndipo sindinabwerere mʼmbuyo.
LEUM GOD El ase etauk nu sik, Ac nga tiana lainul Ku forla lukel.
6 Ndinapereka msana wanga kwa ondimenya masaya anga ndinawapereka kwa anthu ondizula ndevu; sindinawabisire nkhope yanga anthu ondinyoza ndi ondilavulira.
Nga fuhlelana elos in sringil fintukuk. Nga tia kutongolos ke elos fahk kas in akkolukyeyu Ac fis unen alut luk Ac ani nu in mutuk.
7 Popeza Ambuye Yehova amandithandiza, sindidzachita manyazi. Tsono ndalimba mtima ngati msangalabwi, chifukwa ndikudziwa kuti sindidzachita manyazi.
Tusruktu kas in akkoluk lalos koflana akmunasyeyu Mweyen LEUM GOD Fulatlana El kasreyu. Nga sikulyuwi na ku, tuh nga in muteng ma elos oru. Nga etu lah nga ac tia akmwekinyeyuk,
8 Wondikhalira kumbuyo ali pafupi, ndaninso amene adzandiyimba mlandu? Abwere kuti tionane maso ndi maso! Mdani wanga ndi ndani? Abweretu kuti tilimbane!
Mweyen God El apkuran nu sik, Ac El fah akpwayei lah wangin ma koluk luk. Ya oasr mwet ac pulaik in orek tukak keik? Lela nga el in tukeni som nu ke nununku! Lela elan fahk tukak lal an we!
9 Ambuye Yehova ndiye amene amandithandiza. Ndaninso amene adzanditsutsa? Onse adzatha ngati chovala chodyedwa ndi njenjete.
LEUM GOD Fulatlana El ac loangeyu, Na su ku in akpwayei lah oasr ma koluk luk? Mwet nukewa ma orek tukak keik ac wanginla, Elos ac wanginla oana sie ipin nuknuk ma watilla uh.
10 Ndani mwa inu amaopa Yehova ndi kumvera mawu a mtumiki wake? Aliyense woyenda mu mdima, popanda chomuwunikira, iye akhulupirire dzina la Yehova ndi kudalira Mulungu wake.
Kowos nukewa su akfulatye LEUM GOD Ac akos kas lun mwet kulansap lal, Sahp ac ku in lohsr inkanek ma kowos fahsr kac, Tusruktu lulalfongina in LEUM GOD, ac fungyang nu sel.
11 Koma tsopano inu nonse amene mumasonkha moto ndi kuyatsa sakali za moto kufuna kuwononga anzanu, lowani mʼmoto wanu womwewo. Pitani mu sakali za moto zimene mwayatsa. Ndipo ine Yehova ndiye amene ndidzakugwetsereni mazunzowo.
Kowos nukewa su oru pwapa koluk in kunausla mwet saya Ac fah kunausyukla ke pwapa koluk lowos. LEUM GOD El ac fah oru tuh in ouinge. Ke saflaiya uh kowos ac fah keok ke mwe ongoiya na koluk.

< Yesaya 50 >