< Yesaya 46 >

1 Beli wagwada pansi, Nebo wawerama; nyama zonyamula katundu za nyamula milungu yawo. Mafano awo asanduka katundu wolemera pa msana pa ngʼombe. Asandukadi ngati katundu pa msana pa nyama zotopa.
Klesl Bél, padl Nébo, modly jejich octnou se na hovadech a na dobytku. Tím zajisté, což vy nosíváte, budou náramně obtížena až do ustání.
2 Nyamazo zikuwerama ndi kufuna kugwa ndi milunguyo; sizikutha kupulumutsa katunduyo, izo zomwe zikupita ku ukapolo.
Klesly, padly spolu, aniž budou moci retovati břemene, nýbrž i oni sami v zajetí odejdou.
3 Mverani Ine, Inu nyumba ya Yakobo, inu nonse otsala a mʼnyumba ya Israeli, Ine ndakhala ndi kukusamalirani kuyambira mʼmimba ya amayi anu, ndakhala ndikukunyamulani chibadwire chanu.
Slyšte mne, dome Jákobův, a všickni ostatkové domu Izraelova, kteréž pěstuji hned od života, kteréž nosím hned od narození:
4 Mpaka pamene mudzakalambe ndi kumera imvi ndidzakusamalirani ndithu. Ndinakulengani ndipo ndidzakunyamulani, ndidzakusamalirani ndi kukulanditsani.
Až i do starosti já sám, nýbrž až do šedin já ponesu; já jsem vás učinil, a já nositi budu, já, pravím, ponesu a vysvobodím.
5 “Kodi inu mudzandifanizira ndi yani, kapena mufananitsa ndi yani? Kodi mudzandiyerekeza kapena kundifanizitsa ndi yani?
K komu mne připodobníte a přirovnáte, aneb podobna učiníte, abychom sobě podobní byli?
6 Anthu ena amakhuthula golide mʼzikwama zawo ndipo amayeza siliva pa masikelo; amalemba ntchito mʼmisiri wosula kuti awapangire mulungu, kenaka iwo amagwada pansi ndikupembedza kamulunguko.
Ti, kteříž marně vynakládají zlato z měšce, a stříbro na vážkách váží, najímají ze mzdy zlatníka, aby udělal z něho boha, před nímž padají a sklánějí se.
7 Amanyamula nʼkumayenda nayo milunguyo pa mapewa awo; amayikhazika pa malo pake ndipo imakhala pomwepo. Singathe kusuntha pamalo pakepo. Ngakhale wina apemphere kwa milunguyo singathe kuyankha; kapena kumupulumutsa ku mavuto ake.
Nosí jej na rameni, pěstují se s ním, a stavějí ho na místě jeho, i stojí, z místa svého se nehýbaje. Volá-li kdo k němu, neozývá se, aniž jej z úzkosti jeho vysvobozuje.
8 “Kumbukirani zimenezi ndipo muchite manyazi, Muzilingalire mu mtima, inu anthu owukira.
Pamatujtež na to, a zastyďte se; připusťte to, ó zpronevěřilí, k srdci.
9 Kumbukirani zinthu zakale zinthu zamakedzana; chifukwa Ine ndine Mulungu ndipo palibe wina ofanana nane.
Rozpomeňte se na první věci od věků stalé, nebo já jsem Bůh silný, a není žádného více Boha, aniž jest mně podobného.
10 Ndinaneneratu zakumathero kuchokera pachiyambi pomwe. Kuyambira nthawi yamakedzana ndinaloseratu zoti zidzachitike. Ndikanena zimene ndifuna kuchita ndipo zimachitikadi. Chilichonse chimene ndafuna ndimachichita.
Kterýž oznamuji při počátku dokonání, a hned zdaleka to, což se ještě nestalo; řeknu-li co, rada má se koná, a vše, což mi se líbí, činím.
11 Ndikuyitana chiwombankhanga kuchokera kummawa. Ndikuyitana kuchokera ku dziko lakutali munthu amene adzakwaniritsa cholinga changa. Zimene ndanena ndidzazikwaniritsadi; zimene ndafuna ndidzazichitadi.
Kterýž zavolám od východu ptáka, z země daleké toho, kterýž by vykonal uložení mé. Řekl jsem, a dovedu toho, umínil jsem, a vykonám to.
12 Ndimvereni, inu anthu owuma mtima, inu amene muli kutali ndi chipulumutso.
Slyšte mne, vy urputného srdce, kteříž jste dalecí od spravedlnosti.
13 Ndikubweretsa pafupi tsiku la chipulumutso changa; sichili kutali. Tsikulo layandikira ndipo sindidzachedwa kukupulumutsani ndi kupereka ulemerero wanga kwa Israeli.
Jáť způsobím, aby se přiblížila spravedlnost má. Nebudeť prodlévati, aniž spasení mé bude meškati; nebo složím v Sionu spasení, a v Izraeli slávu svou.

< Yesaya 46 >