< Yesaya 37 >

1 Mfumu Hezekiya atamva zimenezi, anangʼamba zovala zake navala chiguduli ndipo analowa mʼNyumba ya Yehova.
Ke na pacl se Tokosra Hezekiah el lohng ma elos fahk nu sel, el asor ac seya nuknuk lal, ac nokomang nuknuk yohk eoa, ac som nu in Tempul lun LEUM GOD.
2 Iye anatuma Eliyakimu woyangʼanira nyumba ya mfumu, Sebina mlembi wa bwalo, ndi ansembe akuluakulu, onse atavala ziguduli, kwa mneneri Yesaya mwana wa Amozi.
El supwalla Eliakim, mwet liyaung inkul sin tokosra; Shebna, mwet sim lun inkul fulat; ac mwet matu inmasrlon mwet tol nu yorol mwet palu Isaiah wen natul Amoz. Elos wi pac nukum nuknuk yohk eoa.
3 Iwo anamuwuza kuti, “Hezekiya akunena kuti, ‘Lero ndi tsiku lamavuto, lachilango ndi lamanyazi. Ife lero tili ngati mayi woyembekezera amene pofika nthawi yoti achire akupezeka kuti alibe mphamvu zoberekera.’
Pa inge kas ma el sap elos in tuh fahk nu sel Isaiah: “Misenge sie len in keok. Kalyeiyuk ac akmwekinyeyuk kut. Kut oana sie mutan su akola in isus tuh arulana munas in oswela.
4 Mwina Yehova Mulungu wanu adzamva mawu onse a kazembe amene mbuye wake, mfumu ya ku Asiriya anamutuma kudzanyoza Mulungu wamoyo, ndipo Mulunguyo adzamulanga chifukwa cha mawu amene Yehova Mulungu wanu wamva. Choncho pemphererani anthu otsala amene akanali ndi moyo.”
Tokosra Fulat lun Assyria el supwama sie mwet kol fulat lal in tuh fahk kas in akkolukye God moul. Lela LEUM GOD lom in lohng kas in akkoluk inge, ac kaelos su fahk kas inge. Ke ma inge, pre nu sin God ke mwet lasr su painmoulla.”
5 Akuluakulu a mfumu Hezekiya atafika kwa Yesaya,
Ke Isaiah el eis kas sel Tokosra Hezekiah inge,
6 Yesaya anawawuza kuti, “Kawuzeni mbuye wanu kuti ‘Yehova akunena kuti: Usachite mantha ndi zimene wamva, mawu amene nthumwi za mfumu ya ku Asiriya zandinyoza nawo Ine.
el folokunulosla ke top se inge: “Fahkang nu sel tokosra lah LEUM GOD El fahk mu elan tia lela mwet Assyria in aksangengyal ke kas in akkoluk ma elos fahk.
7 Tamverani! Ine ndidzayika mwa mfumuyo mzimu wina kotero kuti akadzamva mphekesera ya nkhondo, adzabwerera ku dziko lake, ndipo Ine ndidzachititsa kuti aphedwe ndi lupanga kwawo komweko.’”
LEUM GOD El ac oru Tokosra Fulat lun Assyria elan lohngak sie sramsram ma ac oru elan folokla nu in facl sel sifacna, na LEUM GOD El ac oru elan anwuki we.”
8 Kazembe wa ankhondo uja atamva kuti mfumu ya ku Asiriya yachoka ku Lakisi, iye anabwerera mʼmbuyo ndipo anakapeza mfumu ikuchita nkhondo ndi mzinda wa Libina.
Mwet kol fulat lun Assyria el lohngak lah Tokosra Fulat el som liki acn Lachish ac mweuni siti Libnah, su oan apkuran nu Lachish. Ouinge el som nu we in lolngok yorol.
9 Nthawi imeneyi Senakeribu analandira uthenga wakuti Tirihaka, mfumu ya ku Kusi akubwera kudzachita naye nkhondo. Atamva zimenezi, anatumiza amithenga kwa Hezekiya ndi mawu awa:
Kas se sun mwet Assyria lah un mwet mweun lun Egypt, ye kolyuk lun Tokosra Tirhakah lun Ethiopia, ac tuku in mweunelos. Ke Tokosra Fulat sac lohngak ma inge el supwala leta se nu sel Tokosra Hezekiah
10 “Kawuzeni Hezekiya mfumu ya ku Yuda kuti: Usalole kuti Mulungu amene ukumudalira akupusitse ponena kuti, ‘Yerusalemu sadzaperekedwa mʼmanja mwa mfumu ya ku Asiriya.’
lun Judah in tuh fahk nu sel, “God se ma kom lulalfongi kac el fahk nu sum mu kom ac tia sruhu sik, tusruktu nimet kom lela kas ingan in kiapwekomla.
11 Ndithudi iwe unamva zimene mafumu a ku Asiriya akhala akuchitira mayiko onse. Iwo anawawononga kotheratu. Tsono iwe ndiye ndi kupulumuka?
Kom lohng tari ma kutena tokosra fulat lun Assyria elos oru nu sin mutunfacl se elos sulela in kunausla. Ya kom nunku mu kom ku in kaingla?
12 Makolo anga anawononga mizinda ya Gozani, Harani, Rezefi ndi anthu a ku Edeni amene ankakhala ku Telasara. Kodi milungu inayi ija anawapulumutsa anthu a mizindayi?
Mwet matu luk somla elos kunausla siti lun Gozan, Haran, ac Rezeph, ac onela pac mwet Betheden su muta Telassar, a wangin god lalos tuh ku in molelosla.
13 Kodi mafumu a ku Hamati, Aripadi, Safaravaimu, Hena ndi Iva ali kuti?”
Pia tokosra lun siti Hamath, Arpad, Sepharvaim, Hena, ac Ivvah?”
14 Hezekiya analandira kalata kwa amithenga nayiwerenga pomwepo. Hezekiya anapita ku Nyumba ya Yehova ndipo anayika kalatayo pamaso pa Yehova.
Tokosra Hezekiah el eisla leta sac sin mwet se ma use ah, ac riti. Na el som nu in Tempul, ac filiya leta sac ye mutun LEUM GOD,
15 Ndipo Hezekiya anapemphera kwa Yehova:
ac pre,
16 “Inu Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, amene mumakhala pa mpando wanu waufumu pakati pa akerubi, Inu nokha ndiye Mulungu wolamulira maufumu onse a dziko lapansi. Munalenga kumwamba ndi dziko lapansi.
“O LEUM GOD Kulana, God lun Israel, su muta lucng liki cherub luo, kom mukena pa God su leumi tokosrai nukewa fin faclu. Kom orala kusrao ac faclu.
17 Inu Yehova tcherani khutu ndipo mumve. Inu Yehova, tsekulani maso anu ndipo muone. Imvani mawu onse amene Senakeribu watumiza, kunyoza Mulungu wamoyo.
Inge, LEUM GOD, lohng kut ac liye ma sikyak nu sesr. Porongo ma nukewa ma Sennacherib el fahk in akkolukye kom, God moul.
18 “Yehova, nʼzoonadi kuti mafumu a Asiriya anawononga mitundu yonse ya anthu ndi mayiko awo.
O LEUM GOD, kut nukewa etu lah tokosra fulat lun acn Assyria elos tuh kunausla mutunfacl puspis, sukela acn selos,
19 Iwo anaponyera pa moto milungu yawo ndi kuyiwononga pakuti sinali milungu koma mafano a mitengo ndi miyala, yopangidwa ndi manja a anthu.
ac esukak god lalos — su tia god pwaye, a ma sruloala ma poun mwet taflela ke eot ac sak.
20 Tsono Inu Yehova Mulungu wathu, tipulumutseni mʼdzanja lake kuti maufumu onse a dziko lapansi adziwe kuti Inu nokha, Inu Yehova, ndiye Mulungu.”
Ke ma inge, LEUM GOD lasr, molikutla liki poun mwet Assyria, tuh mutunfacl nukewa fin faclu fah etu lah kom mukena pa God.”
21 Tsono Yesaya mwana wa Amozi anatumiza uthenga wochokera kwa Yehova kwa Hezekiya poyankha pemphero lake lokhudza Senakeribu mfumu ya ku Asiriya.
Na Isaiah el supwala kas nu sel Tokosra Hezekiah in fahk lah lohngyuk pre lal kacl Sennacherib, tokosra lun Assyria,
22 Mawu amene Yehova wayankhula motsutsana naye ndi awa: “Mwana wamkazi wa Ziyoni akukunyoza ndi kukuseka. Mwana wamkazi wa Yerusalemu, akupukusa mutu wake pamene iwe ukuthawa.
ac LEUM GOD El fahk ouinge, “Siti Jerusalem isrun kom, Sennacherib, ac orek tafunkas keim.
23 Kodi iwe wanyoza ndi kulalatira ndani? Kodi iwe wafuwulira ndi kumuyangʼana monyada ndani? Watsutsana ndi Woyerayo wa Israeli!
Su kom nunku mu kom kaskou nu se, ku akkolukye uh? Kom arulana akpusiselyeyu, God Mutal lun Israel!
24 Kudzera mwa amithenga ako iwe wanyoza Ambuye. Ndipo wanena kuti, ‘Ndi magaleta anga ochuluka ndafika pamwamba pa mapiri, pamwamba penipeni pa mapiri a Lebanoni. Ndagwetsa mitengo yamkungudza yayitali kwambiri, ndi mitengo yabwino kwambiri ya payini. Ndafika pa msonga pake penipeni, nkhalango yake yowirira kwambiri.
Kom supwama mwet tafweyom in tungak nu sik mu chariot puspis nutum oru kom fanukya fineol ma fulat liki nukewa in acn Lebanon. Kom konkin pac mu kom pakiya sak cedar ma fulat emeet ac sak cypress ma wo emeet we, ac kom som loallana nu insak uh.
25 Ndakumba zitsime ku mayiko achilendo ndi kumva madzi akumeneko ndi mapazi anga ndawumitsa mitsinje yonse ya ku Igupto.’
Kom konkin pac mu kom pukanak lufin kof in acn sin mwetsac ac nim kof kac, oayapa falken mwet mweun lom lolongya Infacl Nile pulamlamla.
26 “Kodi sunamvepo kuti zimenezi ndinazikonzeratu kalekale? Ndinazikonzeratu masiku amakedzana; tsopano ndazichitadi, kuti iwe kwako nʼkusandutsa mizinda yotetezedwa kukhala milu ya miyala.
“Ya kom soenna lohng lah nga nuna akoo ma inge ke pacl loeloes somla? Ac inge nga orala tari. Nga pa sot nu sum ku in ekulla siti potyak nu ke yol in kutkut.
27 Anthu amene ankakhala kumeneko analibenso mphamvu, ankada nkhawa ndi kuchititsidwa manyazi. Anali ngati mbewu za mʼmunda, ngati udzu wanthete, ali ngati udzu omera pa denga, umene mphepo imawumitsa usanakule nʼkomwe.
Mwet ma muta in acn ingo wangin ma elos ku in oru; elos sangeng ac fohsak. Elos oana mah inimae, ku mah ma kapak fin lohm uh ke pacl eng fol kutulap me tuhyak ac okla.
28 “Koma Ine ndimadziwa zonse za iwe; ndimadziwa pamene ukuyima ndi pamene ukukhala; ndimadziwa pamene ukutuluka ndi pamene ukulowa, ndiponso momwe umandikwiyira Ine.
“Tusruktu nga etu ma nukewa keim, ma kom oru ac yen kom ac som nu we. Nga etu lupan mongsa lom lainyu.
29 Chifukwa umandikwiyira Ine ndi kuti mwano wako wamveka mʼmakutu anga, ndidzakola mphuno yako ndi mbedza ndikuyika chitsulo mʼkamwa mwako, ndipo ndidzakubweza pokuyendetsa njira yomwe unadzera pobwera.
Nga lohng tari pungen kasrkusrak lom ac inse fulat lom, ac inge nga ac sang sie ring srumasrla infwem ac soko osra nu inwalum, ac amakin kom folokla ke innek soko na kom tuku kac.”
30 “Iwe Hezekiya, chizindikiro chako cha zimene zidzachitike ndi ichi: “Chaka chino mudzadya zimene zamera zokha, ndipo chaka chachiwiri zimene zaphukira pa zomera zokha, koma chaka chachitatu mudzafesa ndi kukolola, mudzawoka mitengo yamphesa ndi kudya zipatso zake.
Na Isaiah el fahk nu sel Tokosra Hezekiah, “Pa inge sie akul ke ma ac fah sikyak. Yac se inge ac yac fahsru uh kom ac fah mongo wheat inima mukena, tusruktu ke yac se toko an kom ac fah ku in yukwiya wheat sunom ac kosrani pac kac, ac yukwiya oa in grape ac mongo grape kac.
31 Anthu a nyumba ya Yuda amene adzatsalire adzazika mizu yawo pansi ndipo adzabereka zipatso poyera.
Elos su painmoulla in acn Judah elos ac kapak oana sak ma okah kac kapla loal nu infohk uh ac rukruk fahko.
32 Pakuti ku Yerusalemu kudzachokera anthu otsala, ndi ku phiri la Ziyoni gulu la anthu opulumuka. Changu cha Yehova Wamphamvuzonse chidzachita zimenezi.
Ac fah oasr mwet in Jerusalem ac fin Eol Zion su ac fah painmoulla, mweyen LEUM GOD Kulana El wotela tari sel mu ac ouinge.
33 “Choncho Yehova akunena izi za mfumu ya ku Asiriya: “Iye sadzalowa mu mzinda umenewu kapena kuponyamo muvi uliwonse. Sadzafika pafupi ndi mzindawu ndi ankhondo ake a zishango kapena kuwuzinga ndi mitumbira yankhondo.
“Ac pa inge ma LEUM GOD El fahk ke Tokosra Fulat lun Assyria: ‘El ac fah tia utyak nu in siti se inge ku pisrikya sokofanna osra in pisr natul nu kac. Wangin mwet mweun su us mwe loeyuk ac fah tuku apkuran nu ke siti uh, oayapa ac fah wangin ma ac etoatyak elos in fanyak kac nu in siti uh.
34 Adzabwerera potsata njira yomwe anadzera pobwera; sadzalowa mu mzinda umenewu,” akutero Yehova.
El ac fah folokla ke inkanek soko na el tuku kac, ac tia utyak nu in siti se inge. Nga, LEUM GOD, pa fahk ma inge.
35 “Ine ndidzawuteteza ndi kuwupulumutsa mzindawu, chifukwa cha Ine mwini ndiponso chifukwa cha pangano ndi mtumiki wanga Davide!”
Nga fah loango siti se inge ac liyaung ke sripen Inek sifacna, ac ke sripen wuleang su nga tuh orala nu sel David, mwet kulansap luk.’”
36 Tsopano mngelo wa Yehova anapita ku misasa ya nkhondo ya ku Asiriya ndikukapha asilikali 185,000. Podzuka mmawa mwake anthu anangoona mitembo ponseponse!
Sie lipufan lun LEUM GOD som nu nien aktuktuk lun mwet mweun Assyria ac onela mwet mweun tausin siofok oalngoul limekosr. Toangna in len tok ah elos nukewa alapelik misa!
37 Choncho Senakeribu mfumu ya ku Asiriya anasasula misasa nʼkuchoka kubwerera kukakhala ku Ninive.
Na Sennacherib, Tokosra Fulat lun Assyria, el tila mweun a el folokla nu Nineveh, yen sel.
38 Tsiku lina, pamene ankapembedza mʼnyumba ya mulungu wake, Nisiroki, ana ake awiri, Adirameleki ndi Sarezeri anamupha ndi lupanga, ndipo anathawira mʼdziko la Ararati. Ndipo mwana wake Esrahadoni analowa ufumu mʼmalo mwake.
Sie len ah ke el alu in tempul lun Nisroch, god lal, luo sin wen natul ah, Adrammelech ac Sharezer, unilya ke cutlass natultal, ac kaingla nu in facl Ararat. Esarhaddon, sie pac sin wen natul, el aolulla in tokosra fulat.

< Yesaya 37 >