< Yesaya 28 >

1 Tsoka ufumu wonyada wa zidakwa za ku Efereimu. Tsoka kwa ulemerero wake wokongola umene ukufota ngati duwa limene lili pa mutu pa anthu oledzera a mʼchigwa chachonde.
Вай де кунуна ынгымфатэ а бецивилор луй Ефраим, де флоаря вештежитэ, каре есте стрэлучиря подоабей сале, пе кулмя вэий мэноасе а челор че се ымбатэ!
2 Taonani, ambuye ali naye wina wamphamvu ndi nyonga. Iye adzabwera ngati mkuntho wamatalala ndi namondwe wowononga, ngati madzi amphamvu osefukira a mvula yamkuntho; ndipo adzawagwetsa pansi mwankhanza.
Ятэ кэ вине де ла Домнул ун ом таре ши путерник, ка о фуртунэ де пятрэ, ка о вижелие нимичитоаре, ка о рупере де норь ку марь шувоае де апе, каре о добоарэ ку путере ла пэмынт.
3 Ulamuliro wa atsogoleri oledzera a ku Efereimu adzawuthetsa.
Ва фи кэлкатэ ын пичоаре кунуна ынгымфатэ а бецивилор луй Ефраим;
4 Ndipo ulemerero wokongola wa mzinda umene uli ngati duwa lofota pamutu pa anthu oledzera a mʼchigwa chachonde uja, udzakhala ngati nkhuyu yoyambirira kupsa imene munthu akangoyiona amayithyola nthawi yokolola isanakwane.
ши флоаря вештежитэ, каре есте стрэлучиря подоабей ей пе кулмя вэий мэноасе, ва фи ка о смокинэ тимпурие, каре се веде ынаинте де кулесул роаделор ши пе каре абя о ей ын мынэ ши ындатэ о ши ынгиць.
5 Tsiku limenelo Yehova Wamphamvuzonse adzakhala ngati nkhata yaufumu, chipewa chokongola kwa anthu ake otsala.
Ын зиуа ачея, Домнул оштирилор ва фи о кунунэ стрэлучитоаре ши о подоабэ мэряцэ пентру рэмэшица попорулуй
6 Iye adzapereka mtima wachilungamo kwa oweruza, adzakhala chilimbikitso kwa amene amabweza adani pa zipata za mzinda.
сау ун дух де дрептате пентру чел че шаде пе скаунул де жудекатэ ши о путере пентру чей че дау пе врэжмаш ынапой пынэ ла порциле луй.
7 Nawonso awa ali dzandidzandi chifukwa cha vinyo ndipo akusochera chifukwa cha mowa: ansembe ndi aneneri akudzandira chifukwa cha mowa ndipo akusokonezeka chifukwa cha vinyo; akusochera chifukwa cha mowa, akudzandira pamene akuona masomphenya, kupunthwa pamene akupereka chigamulo.
Дар ши ей се клатинэ де вин ши бэутуриле тарь ый амецеск; преоць ши пророчь сунт ымбэтаць де бэутурь тарь, сунт стэпыниць де вин, ау амецель дин причина бэутурилор тарь; се клатинэ кынд пророческ, се потикнеск кынд жудекэ.
8 Pa matebulo onse pali masanzi okhaokha ndipo palibenso malo wopanda zonyansa.
Тоате меселе сунт плине де вэрсэтурь мурдаре ши ну май есте ничун лок курат.
9 Iwo akuti, “Kodi munthu ameneyu akufuna aphunzitse ndani? Uthengawu akufuna kufotokozera yani? Ndi kwa ana amene aleka kuyamwa, kwa makanda ongowachotsa kumene ku bere?
Ей зик: „Пе чине вря ел сэ ынвеце ынцелепчуня? Куй вря сэ дя ынвэцэтурь? Унор копий ынцэркаць де курынд, луаць де ла цыцэ?
10 Akuyesa kumatiphunzitsa pangʼonopangʼono lemba ndi lemba, mzere ndi mzere, phunziro ndi phunziro. Zonsezi akungoti apa pangʼono apa pangʼono.”
Кэч дэ ынвэцэтурэ песте ынвэцэтурэ, ынвэцэтурэ песте ынвэцэтурэ, порункэ песте порункэ, порункэ песте порункэ, пуцин аич, пуцин аколо.”
11 Mulungu adzayankhula kwa anthu ake kudzera mwa anthu aziyankhulo zachilendo, ziyankhulo zosamveka bwino. Mulungu adzayankhula kwa anthu awa, amene
Ей бине! Прин ниште оамень ку бузе былбыитоаре ши ку ворбиря стрэинэ ва ворби попорулуй ачестуя Домнул.
12 anakuwuzani kuti, “Malo opumulira ndi ano, otopa apumule, malo owusira ndi ano.” Koma inu simunamvere.
Ел ый зичя: „Ятэ одихна! Лэсаць пе чел остенит сэ се одихняскэ! Ятэ локул де одихнэ!” Дар ей н-ау врут сэ аскулте,
13 Choncho Yehova adzakuphunzitsani pangʼonopangʼono lemba ndi lemba, mzere ndi mzere, phunziro ndi phunziro. Kotero mudzayenda ndi kugwa chambuyo, adzapweteka ndi kukodwa mu msampha ndipo adzakutengani ku ukapolo.
ши пентру ей Кувынтул Домнулуй ва фи: „Ынвэцэтурэ песте ынвэцэтурэ, ынвэцэтурэ песте ынвэцэтурэ, порункэ песте порункэ, порункэ песте порункэ, пуцин аич, пуцин аколо”, ка, мергынд, сэ кадэ пе спате ши сэ се здробяскэ, сэ дя ын лац ши сэ фие приншь.
14 Nʼchifukwa chake imvani mawu a Yehova, inu anthu achipongwe amene mumalamulira anthu awa mu Yerusalemu.
Де ачея, аскултаць Кувынтул Домнулуй, батжокориторилор, каре стэпыниць песте попорул ачеста дин Иерусалим!
15 Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol h7585)
Пентру кэ зичець: „Ной ам фэкут ун легэмынт ку моартя, ам фэкут о ынвоялэ ку Локуинца морцилор: кынд ва трече урӂия апелор нэвэлитоаре, ну не ва атинӂе, кэч авем ка лок де скэпаре неадевэрул ши ка адэпост, минчуна!” (Sheol h7585)
16 Tsono zimene Ambuye Yehova akunena ndi izi: “Taonani, ndikuyika mwala wovomerezeka ndi amisiri ngati maziko mu Ziyoni, mwala wapangodya, wamtengowapatali wopanga maziko amphamvu; munthu amene awukhulupirira sadzagwedezeka.
Де ачея, аша ворбеште Домнул Думнезеу: „Ятэ, пун ка темелие ын Сион о пятрэ, о пятрэ ынчеркатэ, о пятрэ де прец, пятрэ дин капул унгюлуй клэдирий, темелие путерникэ; чел че о ва луа ка сприжин ну се ва грэби сэ фугэ.
17 Ntchito zolungama zidzakhala ngati chingwe choyezera maziko ake, ndipo chilungamo chidzakhala chowongolera mzere; matalala adzawononga malo anu othawirapo, amene ndi mabodza, ndipo madzi adzamiza malo anu obisalako.
Вой фаче дин неприхэнире о леӂе ши дин дрептате, о кумпэнэ, ши гриндина ва сурпа локул де скэпаре ал неадевэрулуй ши апеле вор ынека адэпостул минчуний.
18 Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol h7585)
Аша кэ легэмынтул востру ку моартя ва фи нимичит ши ынвояла воастрэ ку Локуинца морцилор ну ва дэйнуи. Кынд ва трече урӂия апелор нэвэлитоаре, вець фи стривиць де еа. (Sheol h7585)
19 Ndipo ukadzangofika udzakutengani. Udzafika mmawa uliwonse, usiku ndi usana.” Anthu akadzamvetsetsa uthenga umenewu adzaopsedwa kwambiri.
Орь де кыте орь ва трече, вэ ва апука; кэч ва трече ын тоате диминециле, зи ши ноапте, ши нумай вуетул ей вэ ва ынгрози.”
20 Mudzakhala ngati munthu wogona pa bedi lalifupi kwambiri kuti sangathe kutambalitsapo miyendo; ndiponso mudzakhala ngati munthu amene wafunda bulangeti lochepa kwambiri kuti sangathe nʼkufunda komwe.
Патул ва фи пря скурт ка сэ те ынтинзь ын ел ши ынвелитоаря, пря ынгустэ ка сэ те ынвелешть ку еа.
21 Yehova adzamenya nkhondo monga anachitira ku phiri la Perazimu adzakalipa monga anachitira ku chigwa cha Gibiyoni; adzagwira ntchito yake yooneka ngati yachilendo, ndipo zimene ati adzachite zidzakhala ngati zodabwitsa.
Кэч Домнул Се ва скула ка ла мунтеле Перацим ши Се ва мыния ка ын валя Габаонулуй, ка сэ-Шь факэ лукраря, лукраря Луй чудатэ, ка сэ-Шь ымплиняскэ лукрул, лукрул Луй немайаузит.
22 Tsopano lekani kunyoza, mukapanda kutero maunyolo anu adzakuthinani kwambiri; Ambuye, Yehova Wamphamvuzonse wandiwuza kuti, “Ndagamula kuti ndidzawononga dziko lapansi.”
Акум, ну батжокориць, ка ну кумва сэ ви се стрынгэ май таре легэтуриле, кэч ам афлат де ла Домнул Думнезеул оштирилор кэ нимичиря ынтреӂий цэрь есте хотэрытэ.
23 Tcherani khutu ndipo mumve mawu anga; mvetserani ndipo mumve zimene ndikunena.
Плекаци-вэ урекя ши аскултаць гласул меу! Фиць ку луаре аминте ши аскултаць кувынтул меу!
24 Kodi mlimi wofuna kudzala mbewu amangokhalira kutipula kokhakokha? Kodi amangokhalira kugawula ndi kugalawuza kokhakokha?
Чел че арэ пентру семэнэтурэ арэ оаре неконтенит? Неконтенит ышь брэздязэ ши ышь грэпязэ ел пэмынтул?
25 Pamene iye wasalaza mundawo, kodi samafesa mawere ndi chitowe? Kodi suja samadzala tirigu ndi barele mʼmizere yake, nadzala mchewere mʼphepete mwa mundawo?
Оаре, дупэ че а нетезит фаца пэмынтулуй, ну арункэ ел мэзэрике ши сямэнэ кимен? Ну пуне ел грыул ын рындурь, орзул, ынтр-ун лок деосебит ши алакул, пе марӂинь?
26 Mulungu wake amamulangiza ndi kumuphunzitsa njira yabwino.
Думнезеул луй л-а ынвэцат сэ факэ аша, Ел й-а дат ачесте ынвэцэтурь.
27 Mawere sapunthira chopunthira cha galeta lopanda mikombero, kapena chitowe sapuntha popondetsapo mikombero ya galeta; mawere amapuntha ndi ndodo ndipo chitowe amapuntha ndi kamtengo.
Мэзэрикя ну се треерэ ку ляса ши роата карулуй ну трече песте кимен, чи мэзэрикя се бате ку бэцул ши кименул, ку нуяуа.
28 Tirigu ayenera kusinjidwa kuti apangire buledi, komabe munthu samangokhalira kupuntha tiriguyo osalekeza, kuopa kuti angatekedzeke. Ngakhale kuti amapuntha tiriguyo poyendetsapo mikombero ya galeta, koma akavalo ake satekedza tiriguyo.
Грыул се бате, дар ну се бате неконтенит; ымпинӂь песте ел роата карулуй ши каий, дар ну-л сфэрымь.
29 Izinso zimachokera kwa Yehova Wamphamvuzonse, wa uphungu wodabwitsa ndi wa nzeru zopambana.
Ши лукрул ачеста вине де ла Домнул оштирилор; минунат есте планул Луй ши маре есте ынцелепчуня Луй.

< Yesaya 28 >