< Yesaya 28 >

1 Tsoka ufumu wonyada wa zidakwa za ku Efereimu. Tsoka kwa ulemerero wake wokongola umene ukufota ngati duwa limene lili pa mutu pa anthu oledzera a mʼchigwa chachonde.
We nu sin tokosrai lun Israel! Wolana lal efla oana losr ma oan fin sifen mwet kol sruhi lalos. Insuf filang lalos onola keng na, tusruktu elos sruhilana oan ac tia etalos.
2 Taonani, ambuye ali naye wina wamphamvu ndi nyonga. Iye adzabwera ngati mkuntho wamatalala ndi namondwe wowononga, ngati madzi amphamvu osefukira a mvula yamkuntho; ndipo adzawagwetsa pansi mwankhanza.
Leum El akoela tari sie su ku ac fokoko in mweun nu selos — sie su fah tuku oana sie paka in af na yohk kosra, oana sie af matol ma oana sie sronot fungme ac afunla acn uh.
3 Ulamuliro wa atsogoleri oledzera a ku Efereimu adzawuthetsa.
Filang lun mwet kol sruhi lalos ac fah lolongyuki.
4 Ndipo ulemerero wokongola wa mzinda umene uli ngati duwa lofota pamutu pa anthu oledzera a mʼchigwa chachonde uja, udzakhala ngati nkhuyu yoyambirira kupsa imene munthu akangoyiona amayithyola nthawi yokolola isanakwane.
Wolana lun mwet kol filang lalos fah wanginla, oana fahko se meet ke sak fig ke pacl la, sifeyukyak ac mongola ke tufahna mwesrla.
5 Tsiku limenelo Yehova Wamphamvuzonse adzakhala ngati nkhata yaufumu, chipewa chokongola kwa anthu ake otsala.
Sie len ac tuku ke LEUM GOD Kulana El ac fah oana sie losr wolana nu sin mwet lal su moulla.
6 Iye adzapereka mtima wachilungamo kwa oweruza, adzakhala chilimbikitso kwa amene amabweza adani pa zipata za mzinda.
El ac fah sang ngunin nununku suwohs nu sin mwet nununku, ac akpulaikyalos su liyaung mutunpot lun siti in lain mwet lokoalok.
7 Nawonso awa ali dzandidzandi chifukwa cha vinyo ndipo akusochera chifukwa cha mowa: ansembe ndi aneneri akudzandira chifukwa cha mowa ndipo akusokonezeka chifukwa cha vinyo; akusochera chifukwa cha mowa, akudzandira pamene akuona masomphenya, kupunthwa pamene akupereka chigamulo.
Finne mwet palu ac mwet tol, elos arulana sruhi, oru elos fahsr tukulkul. Yokla nim wain ac mwe nim ku, oru elos nukanulosla ac fahsr toptop. Mwet palu elos arulana sruhi ac tia kalem ke aruruma ma God El supu, ac mwet tol elos arulana sruhi ac tia ku in oru nununku suwohs nu ke mwe elya lun mwet uh.
8 Pa matebulo onse pali masanzi okhaokha ndipo palibenso malo wopanda zonyansa.
Tepu ma elos muta kac afla ke woht, ac wangin acn nasnas lula fac.
9 Iwo akuti, “Kodi munthu ameneyu akufuna aphunzitse ndani? Uthengawu akufuna kufotokozera yani? Ndi kwa ana amene aleka kuyamwa, kwa makanda ongowachotsa kumene ku bere?
Elos torkaskas keik ac fahk, “Ku El nunku mu su El luti uh? Su enenu kas lal? Ma na nu sin tulik fusr ma tufahna liktitla!
10 Akuyesa kumatiphunzitsa pangʼonopangʼono lemba ndi lemba, mzere ndi mzere, phunziro ndi phunziro. Zonsezi akungoti apa pangʼono apa pangʼono.”
Ma na fisrasr pa El luti nu sesr: El kalweni kais sie leta, lain nu ke lain, mwe luti nu ke mwe luti.”
11 Mulungu adzayankhula kwa anthu ake kudzera mwa anthu aziyankhulo zachilendo, ziyankhulo zosamveka bwino. Mulungu adzayankhula kwa anthu awa, amene
Kowos fin tia porongeyu, na God El ac supwaot kutu mwetsac su orekmakin kas sakirik ma kowos tia kalem kac in luti kowos.
12 anakuwuzani kuti, “Malo opumulira ndi ano, otopa apumule, malo owusira ndi ano.” Koma inu simunamvere.
El kena akwoye kowos ac sot mongla nu suwos nukewa, a kowos srunga porongal.
13 Choncho Yehova adzakuphunzitsani pangʼonopangʼono lemba ndi lemba, mzere ndi mzere, phunziro ndi phunziro. Kotero mudzayenda ndi kugwa chambuyo, adzapweteka ndi kukodwa mu msampha ndipo adzakutengani ku ukapolo.
Pa pwanang LEUM GOD El ac kalweni kais sie leta, lain nu ke lain, ac mwe luti nu ke mwe luti. Na kowos fah tukulkul yen nukewa kowos fahsr we. Kowos ac fah kinkineta, sremla ke kwasrip, ac utukla nu in sruoh.
14 Nʼchifukwa chake imvani mawu a Yehova, inu anthu achipongwe amene mumalamulira anthu awa mu Yerusalemu.
Inge, kowos mwet enum su leum fin mwet inge in acn Jerusalem, porongo ma LEUM GOD El fahk.
15 Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol h7585)
Kowos konkin mu kowos orala sie wuleang yurin misa, ac kowos insesela yurin mwet in facl sin mwet misa. Kowos nunku mu mwe ongoiya ac fah aliki kowos ke pacl se ac tuku, mweyen kowos lulalfongi ke kikiap ac kutasrik lowos in loangekowos. (Sheol h7585)
16 Tsono zimene Ambuye Yehova akunena ndi izi: “Taonani, ndikuyika mwala wovomerezeka ndi amisiri ngati maziko mu Ziyoni, mwala wapangodya, wamtengowapatali wopanga maziko amphamvu; munthu amene awukhulupirira sadzagwedezeka.
Pa inge ma LEUM GOD Fulatlana El fahk: “Nga likiya sie pwelung in Zion ma oakwuki ku. Nga filiya sie eot insruwasrik saok ac ku kac, ac kas inge simla fac: ‘Lulalfongi se su ku el oayapa mongfisrasr.’
17 Ntchito zolungama zidzakhala ngati chingwe choyezera maziko ake, ndipo chilungamo chidzakhala chowongolera mzere; matalala adzawononga malo anu othawirapo, amene ndi mabodza, ndipo madzi adzamiza malo anu obisalako.
Nununku suwohs pa mwe srikasrak nu fin pwelung uh, ac pwaya pa mwe srikasrak nu ke siska ah, tenyak nu lucng.” Af yohk kosra fah pokla kikiap nukewa ma kowos lulalfongi, ac sronot ac fah kunausla acn kowos lulalfongi in wikla we.
18 Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol h7585)
Wuleang ma kowos orala yurin misa ac fah sisila, ac insesela lowos yurin mwet in facl lun misa fah ikilyukla wanginla ku la. Ke mwe ongoiya lulap ac tuhme, ac fah afinkowosi ac kunauskowosla. (Sheol h7585)
19 Ndipo ukadzangofika udzakutengani. Udzafika mmawa uliwonse, usiku ndi usana.” Anthu akadzamvetsetsa uthenga umenewu adzaopsedwa kwambiri.
Ac fah kalkalwen in pokkowosla ke lotutang nukewa. Kowos ac fah keokkin ke len ac fong. Kais sie kas sin God me ac fah mwe aksangeng yohk nu suwos!
20 Mudzakhala ngati munthu wogona pa bedi lalifupi kwambiri kuti sangathe kutambalitsapo miyendo; ndiponso mudzakhala ngati munthu amene wafunda bulangeti lochepa kwambiri kuti sangathe nʼkufunda komwe.
Kowos ac fah oana mukul se in soakas se inge: mwe oan kial fototola elan asrosrelik fac, ac kaot lal oasriksrikla elan afinilya kac.
21 Yehova adzamenya nkhondo monga anachitira ku phiri la Perazimu adzakalipa monga anachitira ku chigwa cha Gibiyoni; adzagwira ntchito yake yooneka ngati yachilendo, ndipo zimene ati adzachite zidzakhala ngati zodabwitsa.
LEUM GOD El ac fah mweun in oana El tuh oru Fineol Perazim ac infahlfal lun Gibeon, Elan ku in orala ma El nunku in oru, finne mukuikui lal uh sie liki na ma mwet uh tawi. El fah aksafye orekma lal su mwet uh tia ku in kalem kac.
22 Tsopano lekani kunyoza, mukapanda kutero maunyolo anu adzakuthinani kwambiri; Ambuye, Yehova Wamphamvuzonse wandiwuza kuti, “Ndagamula kuti ndidzawononga dziko lapansi.”
Nimet isrun kas in sensenkakin nga sot nu suwos! Kowos fin isrun, ac fah upala nu suwos in kaingkunla. Nga lohng pwapa lun LEUM GOD Kulana in kunausla mutunfacl nufon se inge.
23 Tcherani khutu ndipo mumve mawu anga; mvetserani ndipo mumve zimene ndikunena.
Porongo ma nga fahk uh, ac lohang nu ke ma nga fahk nu suwos.
24 Kodi mlimi wofuna kudzala mbewu amangokhalira kutipula kokhakokha? Kodi amangokhalira kugawula ndi kugalawuza kokhakokha?
Wangin mwet ima kalwenina in akfisrasrye acn in ima lal ac tia yukwiya.
25 Pamene iye wasalaza mundawo, kodi samafesa mawere ndi chitowe? Kodi suja samadzala tirigu ndi barele mʼmizere yake, nadzala mchewere mʼphepete mwa mundawo?
Ke pacl se el akoela fohk uh wo, na el yukwiya fiten mahsrik oana dill ac cumin. El yukwi tah in wheat ac barley, ac ke sisken ima lal el yukwi kutu pac kain fita.
26 Mulungu wake amamulangiza ndi kumuphunzitsa njira yabwino.
El etu lah el ac oru orekma lal fuka, mweyen God El lotel.
27 Mawere sapunthira chopunthira cha galeta lopanda mikombero, kapena chitowe sapuntha popondetsapo mikombero ya galeta; mawere amapuntha ndi ndodo ndipo chitowe amapuntha ndi kamtengo.
El tia orekmakin sak toasr in puokla fiten dill ku fiten cumin; a el orekmakin sak mulala ac fal lupa.
28 Tirigu ayenera kusinjidwa kuti apangire buledi, komabe munthu samangokhalira kupuntha tiriguyo osalekeza, kuopa kuti angatekedzeke. Ngakhale kuti amapuntha tiriguyo poyendetsapo mikombero ya galeta, koma akavalo ake satekedza tiriguyo.
El ac tia puok na puok wheat uh nwe ke na mukutkuti, a el etu lah el ac srungulla kolo uh ke el patok sie mwe wiwa fac in mau tia itungya wheat uh.
29 Izinso zimachokera kwa Yehova Wamphamvuzonse, wa uphungu wodabwitsa ndi wa nzeru zopambana.
Lalmwetmet inge nukewa tuku sin LEUM GOD Kulana. Lemlem ma God El oru uh lalmwetmet, ac pacl nukewa safla tuh na wo.

< Yesaya 28 >